MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo....

65
MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU W OYERA Ndipo utatha usiku watha ife tonse tangodzazidwa. Ine ndamva nkhani zabwino lero za ambiri omwe alandira Mzimu Woyera. Ndipo ndife okondwa chifukwa cha izo. 2 Wokondwa kukhala kuti M’bale Graham ali ndi ife usikuuno, mmodzi wa oyanjana nafe kuno ochokera ku kachisi, m’busa wa mpingo wa chiyero uko ku Utica. Ndipo M’bale Jackson, iye anali kuno usiku watha, ine ndikukhulupirira ilo linali; kapena iye ali mmbuyo umo mwa omvetsera penapake tsopano, wina anatero. Inde, ine ndikumuwona M’bale Jackson mmbuyo mwa omvetsera tsopano. Ndi—ndi M’bale Ruddell, kodi iye ali muno usikuuno? Uyo ndi mmodzi wina wa oyanjana nafe kuno ku “62.” Ndife okondwa kukhala ndi iwo muno. Ndi athu…O, M’bale Pat, ndi abale ena onse awa, ndife—ndi uko mwa omvetsera. Ndife okondwa kukhala nanu nonse inu muno usikuuno. 3 Tsopano, ngati ine ndikanati ndichilungamitse chinthucho, ine ndikanawabweretsa ena a alaliki abwinowa pano kuti adzayankhule kwa inu, chifukwa ine ndasasa mawu basi chifukwa chokhala ndi nthawi yaikulu usiku watha. 4 Tsopano, mkazi wanga, iye ndi wondikonza wanga; inu mukudziwa, abale, chimene ine ndikuchikamba. Iye anati anthu mmbuyomo usiku watha samakhoza kundimva ine, chifukwa ine ndimayankhulira mu chinthu ichi. Ndipo tsopano, ine ndisanati ndiyambe, ine ndiyesera chinachake. Tsopano, ine ndikudabwa ngati apo ziri bwino. Kodi ziri bwino mwanjira iyo mmbuyomo? Kapena kodi chonchi ziri bwino? Kodi chonchi ziri bwino? Tsopano, Wokondedwa, ndiyo nthawi imodzi ndapeza chimodzi chokutsutsa iwe. Tsopano, iwo akuti umo ndiye ziri bwino. Chabwino. O, mai! Uyo ndi mkazi. Icho ndi chabwino, chifukwa yakhala ili nthawi yaitali kuchokera pomwe ine ndinakhala nacho china. Iye nthawizonse amakhala wolondola. 5 Chabwino, ife ndithudi tinali ndi—takhala tiri ndi nthawi yaikulu pa msonkhano wa mausiku atatu awo; ine ndinali. Ndipo tsopano, matepi, onse kupatula usiku watha… Ine ndinamuimbira M’bale Goad ndipo ndinamuuza iye kuti abwere kudzajambula tepi ya pa kachisi. Koma izo zinachitika kuti ine ndamva kuti Billy Paul anali atatenga galimoto yake ndipo atapita, chotero tepiyo siinajambulidwe momwe ine ndikudziwira. Chotero ife tiuphonya umenewo. Ine ndikanakonda ndikanadzaisunga iyo mu tchalitchi

Transcript of MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo....

Page 1: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO

PAMZIMU WOYERA

Ndipo utatha usiku watha ife tonse tangodzazidwa. Inendamva nkhani zabwino lero za ambiri omwe alandira

MzimuWoyera. Ndipo ndife okondwa chifukwa cha izo.

2 Wokondwa kukhala kutiM’baleGrahamali ndi ife usikuuno,mmodzi wa oyanjana nafe kuno ochokera ku kachisi, m’busawa mpingo wa chiyero uko ku Utica. Ndipo M’bale Jackson, iyeanali kuno usiku watha, ine ndikukhulupirira ilo linali; kapenaiye ali mmbuyo umo mwa omvetsera penapake tsopano, winaanatero. Inde, ine ndikumuwona M’bale Jackson mmbuyo mwaomvetsera tsopano. Ndi—ndi M’bale Ruddell, kodi iye ali munousikuuno? Uyo ndimmodzi winawa oyanjana nafe kuno ku “62.”Ndife okondwa kukhala ndi iwo muno. Ndi athu…O, M’balePat, ndi abale ena onse awa, ndife—ndi uko mwa omvetsera.Ndife okondwa kukhala nanu nonse inumuno usikuuno.

3 Tsopano, ngati ine ndikanati ndichilungamitse chinthucho,ine ndikanawabweretsa ena a alaliki abwinowa pano kutiadzayankhule kwa inu, chifukwa ine ndasasa mawu basichifukwa chokhala ndi nthawi yaikulu usikuwatha.

4 Tsopano, mkazi wanga, iye ndi wondikonza wanga; inumukudziwa, abale, chimene ine ndikuchikamba. Iye anati anthummbuyomo usikuwatha samakhoza kundimva ine, chifukwa inendimayankhulira mu chinthu ichi. Ndipo tsopano, ine ndisanatindiyambe, ine ndiyesera chinachake. Tsopano, ine ndikudabwangati apo ziri bwino. Kodi ziri bwino mwanjira iyo mmbuyomo?Kapena kodi chonchi ziri bwino? Kodi chonchi ziri bwino?Tsopano, Wokondedwa, ndiyo nthawi imodzi ndapeza chimodzichokutsutsa iwe. Tsopano, iwo akuti umo ndiye ziri bwino.Chabwino. O, mai! Uyo ndi mkazi. Icho ndi chabwino, chifukwayakhala ili nthawi yaitali kuchokera pomwe ine ndinakhalanacho china. Iye nthawizonse amakhala wolondola.

5 Chabwino, ife ndithudi tinali ndi—takhala tiri ndi nthawiyaikulu pa msonkhano wa mausiku atatu awo; ine ndinali.Ndipo tsopano, matepi, onse kupatula usiku watha…Ine ndinamuimbira M’bale Goad ndipo ndinamuuza iyekuti abwere kudzajambula tepi ya pa kachisi. Koma izozinachitika kuti ine ndamva kuti Billy Paul anali atatengagalimoto yake ndipo atapita, chotero tepiyo siinajambulidwemomwe ine ndikudziwira. Chotero ife tiuphonya umenewo.Ine ndikanakonda ndikanadzaisunga iyo mu tchalitchi

Page 2: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

428 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

chifukwa cha mpingowu—kwa wina atati—chomwe ifetimachikhulupirira.

6 Tsopano, usikuuno ine ndikuti ndiyankhule pa MsonkhanoWaukulu, ngati ine ndingakhoze kutsiriza mafunsowamu nthawi. Ndiyeno, mawa mmawa ndi msonkhano wamachiritso. Ndipo ife tikuti tiwapempherere odwala. Chotero,ife sitingakhoze kupereka—kapena kungopita ndi kukati,“Tsopano, ine ndati ndikutengeni inu, ndi inu, ndi inu.” Izosizikanati zikhale zabwino. Koma ife tiperekamuluwamakhadi,ndipo penapake potsatira makhadi amenewo, ine ndidzaitaniraangapo pa nsanja. Ndiyeno, ngati Mzimu Woyera uyambakuwulula, ndiye Iwo umapita uko kudutsa mwa omvetsera ndikukawapeza anthu mwa omvetsera kwa utumiki wa machiritso.Ndiyeno, mawa mmawa, ine ndidzakhala ndikuyankhula,Ambuye akalola, basi tisanayambemsonkhanowamachiritso.

7 Ine ndikumuwona mkazi wanga akuseka. Wokondedwa,kodi iwe sukukhoza kundimva ine nkomwe? O, iwe ukundimvaine. Chabwino, ziri bwino. Iye amakhala kumbuyo mmbuyondipo ngati nkuti—sakukhoza kundimva ine, iye amagwedezamutu wake, “Iwe…Sindikukhoza kukumva iwe, sindikukhozakukumva iwe.”

8 Ndiyeno mawa—mawa usiku ndi utumiki wa ulaliki limodzindi utumikiwa ubatizowamadzi. Ndiyeno,mwamsanga pameneine ndidzatsiriza kulalikira mawa usiku, ife tidzakokera pansimakatani ndi kudzakhala ndi ubatizo wa madzi muno mawausiku. Ngati Ambuye alola, ngati Ambuye alola, mmawa inendikufuna—kapena mawa usiku ine ndikufuna ndidzayankhulepa phunziro: C—Chizindikiro Chinaperekedwa. Ndiyeno, ngatiife tidzakhala pano Lachitatu usiku, ngati Ambuye adzandilolaine kuti ndidzakhale pano Lachitatu usiku, ine ndikufunakuti ndidzayankhule pa phunziro: Ife Taiwona Nyenyezi YakeKummawa ndipo Tabwera Kudzampembedza Iye. Tsopano,ndizo basi usanafike usiku wa Khrisimasi.

9 Ndiyeno, mwamsanga ikatha Khrisimasi ndi sabata latchuthi cha Khrisimasi. Apo ndi pamene ife titi tidzatengemakalata onse…M’bale Mercier ndi iwo kawirikawiriamawatulutsa onsewo. Ndipo ife tidzawayala iwo onse apo,ndipo ife tidzawapempherera makalata awa ndi kuwapemphaAmbuye kuti atitsogolere ife komwe kuli koyenera kudutsamdziko komwe ife titi tidzapiteko.

10 Tsopano, Amuna Amalonda Achikhristu ali ndimndandanda waukulu, tiyenera kukakhala mu Floridamwamsanga ku msonkhano wao. Tidzapita kuchokera ukoku Kingston, ndiye mpaka ku Haiti, ndipo kutsika mpaka kuPuerto Rico, kulowa mu South America, kubwererako podzeramu Mexico.

Page 3: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 429

11 Koma Ambuye akuwoneka kuti akunditsogolera ine kuNorway. Ine sindikudziwa chifukwa chake. Inu mukulidziwabukhu laling’ono lotchedwa Mwamuna Wotumidwa KuchokeraKwa Mulungu? Ndi bukhu lalikulu kwambiri lachipembedzomu Norway. Taganizani za zimenezo, chimene Ambuye achitauko. Ndipo pamene ine ndinali uko, iwo samandilola ine kuyikamanja pa odwala. Ine ndinali uko kwamausiku atatu. Ndipo iwosamandilola ine kuika manja pa odwala. Chotero inu mukuonachimene Mulungu akhoza kuchita. Unyinji unali waukulukwambiri iwo anachita kutenga apolisi okwera, akavalo, ndikumawayendetsa anthu achoke mmisewu kuti ine ndikhozekukafika ku maloko. Ndipo ine sindinayike manja pa odwala.Ine ndimangowapempherera iwo basi; nkuwasiya iwo ayikanemanja wina ndi mzake.12 Chotero…[Winawake akuyankhula ndi M’baleBranham—Mkonzi.] Eya, ine ndithudi ndidzatero, ndiyeTsopano, mawa mmawa…Tsopano, usikuuno, mwina ifetingolowa mu mafunso awa, chifukwa ife tiri nawo ena abwinokwenikweni. Ndipo ine sindikudziwa utali wake womweAmbuye ati atisunge ife pa izo. Ndiyeno, mawa mmawa mwinaBilly Paul, Gene, kapena Leo, wina, adzakhala pano kutiazidzapereka makadi a pemphero pa eyiti koloko mpaka hafupasiti eyiti. Tsopano, anthu a kunja kwa tawoni, mundiloleine ndichinenenso icho kuti inu musati muiwale. Ngati inumukufuna kuti mudzabwere mu mzere, ife ndibwino tidzakhalendi anthu a kunja kwamzinda ngati nkotheka.13 Tsopano, nthawizina kuno mu tchalitchi ife timafika pamalo amene iwo amati, “Chabwino…” Ife timawatengaanthu a kunja kwa tawoni, kuwabweretsa iwo…Wina amati,“Chabwino, ine sindimadziwa chomwe chinali cholakwika ndiiwo. Iwo mwina amanena chinachake cholakwika.” Ndiyeiwe ukatenga anthu mu tawoni; iwo amati, “O, inu mwinamumawadziwa iwo.” Kotero…Ndiye iwo amati—izo zakhalazikunenedwa, “Chabwino, ine ndikukuuzani inu, ndi makadia pempherowo.” Chabwino, nanga bwanji awo amene alibemakadi a pemphero. Ndipo zakhala ziri tsiku ndi tsikupamene izo…

Mukuti chiani? [M’bale Branham akufunsidwa kuti aimemmbuyo kuchoka ku choyankhulira—Mkonzi.] Ndiime patalindi choyankhulirapochi? Chabwino, inu mukudziwa, inenthawizonse ndimalalikira pakati pa msewu. Chotero mwinaine ndingozitenga izo monga choncho. Kodi ziri bwino apo?Ziri bwino. Ndizo zabwino. Ine ndikuuzeni inu chomwe chiri.Zoyankhulira kugulu zathu—zathu nzosauka muno, zosaukakwambiri. Ndipo ife sitiri kuyesera kuti tikhale mwabwinokomulimonse tsopano, chifukwa ife tikufuna kachisi watsopanoamangidwe pompano. Ndipo apo ndi pamene ife titi tidzakhalenawo malo ochuluka (mukuona?), ngati ife tingakhoze kubwera

Page 4: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

430 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

pano ndi kudzawatambasula malo ano mokulitsa pang’ono,ndi kudzayikamo malo ena owonjezera, ndi kukonzekeramisonkhano pamene ife titi tidzakhale nayo kuno.14 Ndipo tsopano, kumbukirani, mmawa anyamata, mmodzikapena atatu a iwo adzakhala akupereka makadi pakati pa8:30—kapena 8:00 ndi 8:30. Izo zikupereka mwayi kwa aliyensekuti adzakhazikike. Ndipo ine ndinali kuyankhula pa za momweiwo amaperekera makadi, chifukwa chomwe ife timachitira izo.Nkuti tizisunga dongosolo. Mwaona? Tsopano, nanga bwanji inendikanabwera muno, basi monga pakali pano nkuti, “Mulolemkazi uyu, mkazi uyu, ndi bambo uyo, ndi mkazi uyu…?” Inumukuona, izo zikanakhala ngati—izo zikanakhala ngati zovuta.Mwaona? Ndiyeno, ngati inu…Nthawi zambiri ine ndachitapoizi. Ndipo ngati iwo sali ochuluka kwambiri mmawawu, inemwina ndikhoza kuchita chinthu chomwecho. Ine ndimati, “Ndianthu angati muno ali ochokera kunja kwa mzinda omwe ali ndichinachake cholakwika ndi inu, inumuiimirire.”15 M’bale Mercier, inu mubwere kudzandipulumutsa. Inumudzandithandiza ine? [M’bale Mercier akuyankha—Mkonzi.]O, inu mubwera…Iye abwera kudzadzipulumutsa yekha. Inendinayankhula kwa bwenzi wanu wamkazi lero. Tsopano,inu muyenera kuti muzikhala wabwino kwenikweni kwa ine.Mwaona? Chabwino. Izo nzabwino. Ine—ine ndikuyamikirakulimbamtima uko M’bale Leo. Pamene izo siziri bwino, tiyeni—tiyeni tizikonze izo bwino monga ife tikudziwira kuzifikitsiraizo, mopambana momwe ife tingakhozere.16 Chotero tsopano ndiye, timangowafunsa anthu a kunjakwa mzinda kuti akweze mmwamba manja awo omwe alinacho chinachake cholakwika nawo. Ndiyeno iwe umaima apo,nkukhazikika pa munthu mmodzi mpaka Mzimu Woyera ufikepoyamba, ndipo nkuwatenga omvetsera onsewo. Ndi angatiakhalapo ali muno pamene iwo anaziwona izo zikuchitidwamunomo? Zedi! Mwaona, mukuona? Chotero ziribe kanthu kutiziri mbali iti. Ndi basi…17 Ine ndikufuna kuti inu mukumbukire izi, ndipo inendiyesera kuti ndidutse mu izo mmawa kachiwiri. Amitundu,Uthenga umene waperekedwa kwa iwo ndi Uthenga wachikhulupiriro, osati wa zintchito konse. Mukuona? Ndipomonga ine ndinanenera usiku watha. Pamene Mzimu Woyeraunagwa pa Pentekoste, pamene iwo anapita uko kwa Ayuda(Machitidwe 19:5), iwo ankachita kuyika manja pa iwo kutiiwo aulandire Iwo. Ndipo pamene iwo anapita ku Samaria, iwoankachita kukaika manja pa iwo. Koma pamene iwo anabwerakwa Amitundu ku nyumba ya Kornerio, “Pamene Petro analiakuyankhulamawu awa…”Osati kuyika kwamanja.18 Pamene msungwana wamng’ono anafa, mwana wamkaziwa Yairo, wansembe, anati, “Bwerani mudzaike manja pa iye,

Page 5: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 431

ndipo iye akhala moyo.” Koma pamene kenturio wachi Roma,Wamitundu, anati, “Ine sindiri woyenera kuti Inu mubwerepansi pa denga langa, yankhulani mawu.” Ndi zomwezo.Mwaona?19 Mkazi wachi Surofonisia, Mherene kwenikweni chimeneiye anali, pamene iye—pamene Yesu anati kwa iye, anati,“Sizoyenera kwa Ine kuti nditenge mkate wa ana ndi kuuperekakwa agaru.”

Iye anati, “Izo nzoona, Ambuye; koma agaru pansi pa gomeamadya nyenyetswa za ana.”

Iye anati, “Chifukwa cha kuyankhula uku, mdierekeziwamusiya mwana wako wamkazi.” Muzinena zinthu zabwinondiye. Muzinena zinazake zabwino zokhudza winawake.Muziyankhula za Yesu. Muzinena chinachake chomvera,chinachake chenicheni. Ndiyo njira yochotsera adierekezi. Iyesananene konse—Iye sanampempherere konsemsungwanayo. Iyesananene konse kanthu kamodzi zokhudzana ndi kuchiritsidwakwake; Iye anangoti, “Chifukwa cha kuyankhula uku, chifukwacha kuyankhula uku…”20 Hattie Wright, tsiku lina, iye sanapemphe kalikonse. Iyeanali atangokhala pamenepo, koma iye ananena chinthuchoyenera, chimene chinaukondweretsa Mzimu Woyera. NdipoMzimu Woyera unayankhula moyankha nkuti, “Hattie, pemphachirichonse chimene iwe ungafune, chirichonse chimene iweuli nacho ndipo ukuchifuna. Kafufuze ngati izi ziri zenizenikapena ayi. Pempha chirichonse (machiritso a mchemwaliwake wamng’ono wolumala atakhala apo yense atawunjikikapamodzi; madola zikwi khumi kuti iye asiye kumakakumbapa mapiri awo kumeneko; unyamata ubwezeretsedwe kwathupi lake logujumulidwa kwambirilo); chirichonse chimene iweukufuna kuti upemphe, iwe uchipemphe icho pakali pano. NgatiIwo subwera ndi kudzakupatsa iwe icho pomwe pano, ndiyendine mneneri wabodza.” Ndicho—ndicho—ndicho chinachake,sichoncho izo?21 Yesu anati, “Nenani kwa phiri ili…” Ndipo inumwamvapo—zokhudza zomwe zakhala zikuchitika; umenewondiwo utumiki umene ife tiri kulowamo. Ife tiri patali munjirayi tsopano. Posachedwa Kudza kwa Ambuye Yesu. Ndipoife tiyenera kuti tikhale nacho chikhulupiriro chokwatulitsamu Mpingo umene ungakhoze kusinthidwa mu kamphindi mukuthwanima kwa diso kuti tizipita, kapena ife sitidzapita. Komamusati mudandaule, iwo udzakakhala ulipo. Iwo udzakakhalaulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera,iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu ya mpingo uwoikakwera, udzawabweretsa abale ake; mphamvu ya mpingo uwoudzawabweretsa abale enawo; ndiye kudzakhala chiukitsiro chaaliyense. Ndipo ife tikuyang’anira ku zimenezo.

Page 6: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

432 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

22 Tsopano, musati muiwale, makadi apemphero mmawapa 8 koloko mpaka 8:30. Ndiye ine ndidzawafunsa iwoaliwonse omwe alimo, ndiye adzangosiya kupereka makadi, ndikupitirira kumka mmbuyo, ndi kukakhala pansi (mwaona?),chifukwa iwo adzakhala atapereka onse mwina pofika nthawiimeneyo mulimonse, kapena ochuluka monga omwe ife tititidzawatenge kuchokera uko penapake. Anyamata adzabwera,kudzawasakaniza makadi onsewo pamaso panu pomwe, ndiyengati inu mukufuna imodzi, inu mukufuna imodzi, kapenachoonjezera china chirichonse monga choncho…Ndiye pameneine ndibwera umo, ine basi…Paliponse pamene Ambuyeati itana kuchokerapo…Ndipo ngati Iye ati, “Usawaitanekonse,” Ine sindiwaitana iwo konse (mwaona?), basi chirichonsechomwe chiri.23 Ndipo ine ndiri…Utumiki umenewo wangotsala pang’onokuti uzimirire mulimonse; pali chinachake chachikulupochikubweramo. Kumbukirani, ndi pomwe nthawi iliyonsezakhala zikunenedwa kuchokera pa nsanja ino kapena paguwa lino, ndipo izo sizinayambe zalepherapo panobe. Inumukukumbukira utumiki wa dzanja? Mukuona chimeneiwo unachita? Malingaliro a mtima, mukuona chimene iwounachita? Tsopano penyani ichi: kuyankhula Mawu, ndipomuwone chimene Iwo akuchita. Mukuona? Ine ndinakuuzaniinu kuno zaka zapitazo—mpingo (ine ndikuyankhula kwaa pa kachisiyu)—zaka zapitazo, zaka zitatu kapena zinaizapitazo, chinachake chinali kukonzekera kuti chiwonekere;icho chikukonzekera kuti chichitike. Ndipo ndi ichi tsopanokulowa mkati momwemu…Icho chiri kudziumba chokha apa.Tsopano, ndife oyamikira chifukwa cha izo. O, momwe ife tiriothokozera. Okondwa basi.24 Tsopano, ife tiri ndi mafunso ena olimba kwambiri pano,ndipo ife tikufuna kuti tilowe kumene mwa iwo. Winawakeanayang’ana pa mabuku onse awa omwe ine ndiri nawo. Inendinati, “Chabwino, munthu wanzeru amangosowa limodzi.”Koma ine sindine munthu wanzeru. Ine ndimayenera kutindikhale nawo ochuluka a iwo oti ndiziyang’anamo. Chabwino,ili ndi Diaglott, ndipo ili ndi Baibulo, ndipo ili ndi lolongosola.Chotero ziri…Ife tati tingowapempha Ambuye kuti atithandizeife ndi kutilondolera ife kuti tiwayankhe mafunso awa basimolingana ndi chifuniro ChakeChaumulungu ndiMawuAke.25 Chotero tsopano, tiyeni ife tiweramitse mitu yathu kwamphindi yokha ya pemphero. Ambuye, ife tiri oyamikira kwaInu kuchokera mu kuya komwe kwamtima wathu pa zomwe Inumwatichitira ife mu masiku atatu athawa. O, kuwaona atumikiakusonkhana kumbuyo uko mu chipinda ndi kumagwiranamanja, ndi chikhulupiriro chotsitsimutsidwa, ndi—ndi sitepeyatsopano yoti aitenge. Kuitana pa foni…Ndipo mitima yathuikusangalala, ndi anthu akulandira Mzimu Woyera iwo atatha—

Page 7: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 433

kuwaona Mawu Anu, momwe Iwo akufotokozera ndendendesitepe ndi sitepe momwe angalandirire MzimuWanuWoyera. Ifetiri othokoza kwambiri chifukwa cha izo, Ambuye.26 Inu mukuzipanga zinthu kuphweka kwambiri kwa ife,chifukwa ndife anthu ophweka. Ndipo ife tikupemphera,Mulungu, ku—kuti Inu mutilola ife kwathunthu tizidzipangatokha nthawizonse kukhala ophweka. Pakuti ndiwo…Ndiwo mtundu umene umadzichepetsa wokha umene utiudzakwezedwe. Ndipo nzeru ya mdziko ndiyo kupusa kwaMulungu; kuti zinamukondweretsa Mulungu kupyolera mukupusa kwa kulalikira kuti aziwapulumutsa iwo amene aliotaika.27 Ndipo tsopano, Atate, alipo pano omwe ndiri nawomafunso angapo omwe afunsidwa ochokera mu mitimayodzipereka yomwe yakhudzidwa. Ndipo limodzi la iwolitayankhidwa molakwika zikhoza kumuponyera munthuyonjira yolakwika, kuti uponyere kuwala kolakwika pa funsolawo limene likuwasautsa iwo. Chotero Ambuye Mulungu, inendikupemphera kuti Mzimu Wanu Woyera usunthire pa ifendipo uwulule zinthu izi, pakuti zinalembedwa mu Malemba,“Pemphani ndipo inu mudzalandira; ndi funani ndipo inumudzapeza; gogodani ndipo zidzatsegulidwira kwa inu.” Ndipondi chimene ife tikuchita tsopano, Ambuye, kugogoda pakhomo Lanu la chifundo. Titaima mu mthunzi wa chilungamoChanu Chaumulungu, ife tikuchonderera Magazi a Khristu waMulungu ndi kwaMzimuWoyera.28 Ndipo ife sitikubwera usikuuno kungoti chifukwa ifetachokera ku usiku utatu uja wa kulalikira paMzimuWoyera, ifetikubwera ndi kuya kwa kulemekeza kwambiri ndi kuonamtima.Ife tikubwera ngati kuti uwu ndi usiku wotsiriza womwe ifetiti tidzakhale nawo konse pa dziko lapansi. Ife tikubweratikukhulupirira kuti Inu muyankha mapemphero athu. NdipoAmbuye, ife tikukupemphani Inu tsopano kuti mutikhutitse ifendi Moyo Wanu Wamuyaya. Ndi pa kuyankha kwa Mawu Anu,mulole Mzimu Woyera…O Mulungu, monga ife tinapeza kutindi Inumwini pakati pathu, ife tikupemphera kuti Iye aululirekwa ife usikuuno zinthu zomwe ife tikuzikhumba. Ndipoife tikukhumba kokha kuti miyoyo yathu ikhoze kukhala pampumulo, ndi malingaliro athu pa mtendere, ndi kukhala nachochikhulupiriro mwa Mulungu kuti tiziyenda chamtsogolo kutitiwatenge madalitso omwe Iye anawalonjeza. Ife tikupempha izimu Dzina la Yesu. Ameni.29 Tsopano, ine ndiri nawo mafunso onse omwe anaperekedwakwa ine, kupatula limodzi. Ndipo ine ndinamuyankha M’balewamng’ono Martin yemwe anandifunsa ine funso usikuwadzana, limodzi lokha. Analipo ambiri muno usiku watha,koma awo anali opempha pemphero. Ndipo M’bale Martinanandifunsa ine funso lokhudza Yohane 3:16—kapena Yohane 3,

Page 8: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

434 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

ine ndikukhulupirira, la, “Kupatula ngati munthu abadwa mwamadzi ndi mwaMzimu, iye sangakhoze kuwuona Ufumu,” ndipoamafanizitsa izo ndi tepi yomwe ine ndinaitumiza ya Ahebri.Ndipo ine ndinakomana naye iye mu chipinda cha kumbuyokuno usiku watha, ndipo—ine ndisanakhale nawo mwayi wotindimuyankhe iye, ndiyeno ine ndinazichita apo, pa phunzirolo.

30 Tsopano, kodi alipo wina pano yemwe sanali pano usikuwatha, tiyeni tiwone manja anu, omwe sanali pano usiku watha.O, ife zedi timakhumba inu mukadakhala ndi ife. Ife tinali ndinthawi yaulemerero chotero. MzimuWoyera…

31 Ine mwina, kwa miniti yokha…Izi sizipweteka. Izizikujambulidwa. Ndipo ngati mtumiki aliyense apezekakuti—kapena munthu yemwe ati apezeke kuti sakugwirizanapa zomwe ine ndikukonzekera kuti ndinene tsopano,kapena ngakhale mu mafunso, ine ndikupempha, m’bale,inu musaganize kuti icho ndi chachilendo, koma kuti—kumbukirani kuti tepi iyi ikupangidwa mu kachisi mwathumuno. Ife tikuphunzitsa kwa anthu athu. Atumiki ochuluka azikhulupiriro zosiyana akhala pano. Ndipo ine ndikufuna kutindilowe mu phunzirolo kachiwiri, pakuti alipo ena a anthuathu omwe sakanakhoza kulowa muno usiku watha ameneine ndikuwawona ali muno usikuuno. Ndipo ine ndikanafunakuti ndidutsemo mphindi yokha, ngati inu mungandiloleze izo,pa zomwe ine ndinayankhula usiku watha; ndipo izo zinali paPentekoste, pa kulandira MzimuWoyera.

Tsopano, powerenga kuchokera mu Emphatic Diaglott yakumasulira kwa Chigriki, pamene ine ndinali usiku watha,lomwe liri chitsegulire patsogolo panga tsopano. Ndikokumasulira kwa pachiyambi kuchokera ku Chgriki kupitaku Chingelezi. Ilo silimadzera mwa omasulira ena, ndi—ndikumasulira kwina, ndi lolunjika basi kuchokera ku Chigrikikupita ku Chingelezi. Tsopano, mawu Achingelezi, nthawizambiri ali ndi matanthauzo otero kwa iwo, monga ngati inendikanati tsopano, board.Mukawatenga mawu awo a board. Inumukanati, “Chabwino, iye amatanthauza kuti ife timamutopetsaiye.” Ayi! “Iye—iye analipira gulu lake.” Ayi! Chabwino, iye…“Ndi bolodi ili ku mbali ya nyumba.” Chabwino, mukuona?Kapena chirichonse cha izo…Alipo mawu anai kapena asanuosiyana angakhoze kugwiritsidwa ntchito; iwe umayenerakuti umvetse chiganizocho. Mawu oti see. See amatanthauza“kumvetsa,” mu Chingelezi. Sea amatanthauza “chikhamu chamadzi.” See amatanthauza “kuyang’anapo.” Mwaona? Koma pakumasulira uku, mawu amene agwiritsidwa ntchito apa, omweine ndinawayankhula usiku watha mu Machitidwe mutu wa 2,pamene amati. “Malirime amoto anakhala pa iwo…” Tsopano,ine ndikukhumba ndikanangobwerera mmbuyo mphindi yokha.Kodi inu mungakonde kutero, mphindi yokha, ndi kukhala

Page 9: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 435

ngati kuzibwereza izo kwa mphindi ife tisanapite patsogolopaliponse?32 Tsopano, tembenuzirani, inu mu King James lanukapena kumasulira kulikonse kumene inu mukuwerengakuchokeramo…Ndipo ine ndikufuna kuti ndiwerenge izo.Ndipo mumvetsere mwatcheru kwenikweni tsopano. Musatimumvetse molakwika. Ochuluka lero, ngakhale mlongo wanga,ambiri a iwo anaimba, anati…Akazi a Morgan…Ambiri a iwoanalimo usiku watha. Akazi a Morgan ndi mmodzi wa alongoathu yemwe analepheredwa; ndipo iye anali pa mndandandawa okufa mu Louisville kwa sikisitini, zaka seventini zapitazondi khansara. Ine ndikuganiza iye wakhala kumbuyo munousiku unonso. Iye sanali kukhoza kumva, iye anati, chifukwaine ndinali kuyankhula molunjika mu choyankhulira. Ndipochifukwa cha iwo ine ndikufuna ndidutsenso mu izi kwamphindi.33 Tsopano, ine ndikuwerenga kuchokera ku Lemba ili laMachitidwe 2:

…pamene Tsiku la Pentekoste Linadza Kwathunthu,anali onse mu lingaliro limodzi…(Tsopano, inendikuzikonda izo bwinoko kuposa “chigwirizanochimodzi,” chifukwa inu mukhoza kukhala achigwirizano chimodzi pafupifupi pa phunziro lirilonse,koma pano malingaliro awo anali ofanana.)…alingaliro limodzi ndi pa malo omwewo.Ndipo mwadzidzidzi apo panadza Phokoso lochokera

Kumwamba, longa Mphepo ya nkokomo yachiwawa;ndipo iyo inadzaza Nyumba Yonseyo momwe iwo analiatakhala. (Osati atagwada, osati akupemphera, komaatakhala.)…Malirime ogawanika… (M-a-l-i-r-i-m-e—

malirime. Ogawanika kutanthauza “opatukana.”) …Malirime anawonekera kwa iwo, onga Moto, ndipolimodzi…(“Limodzi,” palokha.)…linadzakhala paaliyense wa iwo.)Ndipo iwo onse anadzazidwa…(“Ndipo,”

cholumikizira)…onse anadzazidwa ndi Mzimuwoyera, ndipo anayamba kuyankhula ndi malirimeEna, momwe Mzimu unkawapatsira iwo zoyankhula.Tsopano iwo anali akukhala mu Yerusalemu, Ayuda,

Amuna odzipereka, ochokera ku Fuko Lirilonse la pansipa Kumwamba.Pamene ichi—ndipo Umboni uwu pamene

unafalitsidwa, Unyinji unadza palimodzi, ndipoanadodometsedwa, Chifukwa aliyense anamumva—iye akuyankhula mu Chinenero chake Chomwe.

Page 10: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

436 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

34 Tsopano zindikirani! Pamene moto unadza, iwo unalimalirime; pamene iwo anali akuyankhula, icho chinalichinenero. Tsopano, pali kusiyana kwakukulu pakati pamalirime ndi zinenero. Kwa ife zonsezo ndi zofanana.Koma, mu Chigriki “lirime” zimatanthauza ili [M’baleBranham akufotokozera—Mkonzi.] Khutu ndi ili. Mukuona?Ilo silimatanthauza chinenero; ilo limatanthauza gawo lathupi lako ilo ndilo lirime. Ngati inu mungazindikire, izozinamasuliridwa kuti malirime a moto chomwe chikutanthauza“monga malirime,” monga ngati chidutswa cha moto, lawilalitali la moto. Tsopano, penyani kutsimikizirako tsopano.Ndipo aliwonse amalo amenewo tsopano,musatimuiwale izo.35 Tsopano, ife tikuti tipereke kasewero kakang’ono usikuuno.Ndipo ine ndikuti ndizisiyire izo kwa inu. Tsopano kumbukirani,ngati chirichonse chiri mosiyana, izo ziri kwa inu. Komanjira yokha yomwe wina aliyense angakhoze kupeza konsechirichonse kuchokera kwa Mulungu ndi mwa chikhulupiriro.Ndipo inu musanati…36 Ine ndiyenera kuti ndizidziwa chimene ine ndikuchita inendisanakhale ndi chikhulupiriro mu zomwe ine ndikuzichita.Nchifukwa chiani inu munamukwatira mkazi wanu? Inumunali ndi chikhulupiriro mwa iye. Inu munamuyesa iye,munamupenya iye, munawona komwe iye ankachokera, yemweiye anali. Ndi momwe liriri Lemba, kwa Mulungu. Ndi zomwezimapangitsa masomphenya awa, a—Lawi la Moto ili, zinthuzonse izi, chifukwa Mulungu analonjeza izo. Mulungu ananenachomwecho. Ine ndamuyesapo Iye ndi Mawu Ake ndipo inendikudziwa kuti Ichi ndi Choonadi. Ndipo inu muzitsatiraMawu Ake. Ndiye ngati pali kusokonezeka penapake, ndiyepali chinachake cholakwika penapake. Chifukwa Mulungu(mvetserani!)—Mulungu sanachite konse kapena sadzagwirakonse ntchito mochoka kwa Iyeyekha—kapena motsutsanandi malamulo Ake omwe. Dzinja silingabwere mu chilimwe,ndipo chilimwe sichingabwere mu dzinja. Masamba sangakhozekumagwa mu nthawi ya kuphukira ndi kubwereranso kachiwirimu kugwa. Inu simungakhoze basi kuzipangitsa izo.37 Monga ine ndinanenera usiku wathawu za chitsime chakasupe, kutsirira mbewu zanu. Kapena ngati inu mutaimapano pakati pa tchire, ndipo imo ndi mwakuda bii, ndipoinu mukanati, “O, magetsi opambana, ine ndikudziwa inumuli mmundamu. Tsopano, ine ndataika, sindikudziwa kumeneine ndikupita. Ndipatse kuwala, kuti ine ndikhoze kumawonamomwe ndingayendere! Alipo magetsi okwanira kuti uwalitsiremmundawu.” Izo nzoona. Inde, bwana! Alipo magetsi okwaniramu chipinda chino kuti achiwalitse icho popanda ngakhale nyaliizo, popanda izo. Koma inu muyenera kuti muwalamulire iwo.Tsopano, inu mukhoza kufuulira kwa iwo mpaka inu osathakufuulanso, iwo sangakhoze konse kuwalitsa. Koma ngati inu

Page 11: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 437

mutagwira ntchitomolingana ndi malamulo amagetsi, ndiye inumupeza kuwala.38 Chabwino, ndi mofanana momwe ziriri ndi Mulungu.Mulungu ndiye Mlengi wamkulu wa miyamba ndi dziko lapansi,yemweyo dzulo, lero, ndi kwanthawizonse. Iye akadali Mulungu.Koma Iye amagwira ntchito pamene inu mukutsatira malamuloAke ndi malangizo basi. Abwenzi, ine ndikunena izi: Inesindinayambe ndaziwonapo izo zitalephera, ndipo sizingatero.39 Tsopano, tiyeni tizindikire. Yesu mu Luka 24:49 analiatawatuma atumwi iwo atapulumutsidwa kale ndi kuyeretsedwamalingana ndi Mawu; kulungamitsidwa pa kukhulupirira paAmbuye Yesu; kuyeretsedwa paYohane 17:17 pamene Yesu anati,“Ayeretseni iwo, Atate, kupyolera mu Choonadi. Mawu Anundiwo Choonadi.” Ndipo Iye anali Mawu.40 Tsopano, anawapatsa iwo mphamvu kuti azichiza odwala,kutulutsa ziwanda, kuukitsa akufa; ndipo iwo anabwereraakusangalala. Ndipo maina awo anali pa Bukhu la Moyo waMwanawankhosa. Inu mukukumbukira momwe ife takhalatikudutsira mu izo tsopano. Koma iwo anali asanatembenukeapabe. Yesu anamuuza Petro usiku wa kupachikidwa Kwakeuja; Iye anati, “Iwe ukadzakhala utatembenuka, ndiyeudzawalimbikitse abale ako.”41 Mzimu Woyera ndi womwe…Inu mukukhulupirirakuloza ku Moyo Wamuyaya, koma pamene Mzimu Woyeraubwera Iwo ndiwo Moyo Wamuyaya. Inu mukukhulupirirakuloza ku…Ndinu obalidwa ndi Mzimu pa kuyeretsedwa,koma simunabadwe konse ndi Mzimu mpaka Mzimu Woyerautabwera umo. Ndiko kukhoza. Mwana amakhala ndi moyo muchiberekero cha amake, akatumba aang’ono amadziwongola; ndimoyo. Koma ndi moyo wosiyana pamene iko kapumila mpweyawa moyo mu mphuno zake. Ndi zosiyana. Nchomwe icho chiri,ndi…42 M’bale wanga wokondedwa wa Methodisti, ndi PilgrimHoliness, ndi Nazarene, ubatizo wa Mzimu Woyera ndiwosiyana ndi kuyeretsedwa. Kuyeretsedwa ndi kutsuka, komwekuli kukonzekera kwa Moyo. Koma pamene Mzimu Woyeraubwera, Iwo ndiwo Moyo. Kukonzekera ndi kutsuka chidacho;Mzimu Woyera ndi kuchidzazitsa chidacho. Kuyeretsedwakumatanthauza “kutsukidwa ndi kuikidwira pambali kwautumiki.” Mzimu Woyera ndi kuchiyika icho mu kutumikira.Ndinu chida chimeneMulungu wachitsuka.43 Ndipo ife tikupeza kuti Mzimu Woyera ndi MulunguMwiniwake mwa inu, Mulungu anali pamwamba pa inu muLawi la Moto ndi Mose. Mulungu anali ndi inu mwa YesuKhristu. Tsopano Mulungu ali mwa inu mwa Mzimu Woyera.Osati amulungu atatu, Mulungu mmodzi akugwira ntchito mumaudindo atatu.

Page 12: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

438 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

44 Mulungu kudzichepetsa, kubwera pansi kuchokerapamwamba pa munthu. Iye sankakhoza kumukhudza Iye,chifukwa iye anali atachimwa mmunda wa Edeni ndipoanadzilekanitsa yekha ku chiyanjano Chake. Ndiye nchianichinachitika? Iye ankachita kumakhala pamwamba pa iye.Magazi a ng’ombe zamphongo ndi mbuzi sakanakhoza kumulolaIye kuti akhale ndi chiyanjano ndi munthu kachiwiri; komakupyolera mmalamulo ndi malangizo, kuwonetseratu nthawiino ikudza, pa kupereka nsembe ng’ombe, ndi zina zotero, ndinkhosa…Ndiye pamene Mulungu anabwera pansi nadzakhalamu thupi loyeretsedwa, lobadwa mwa namwali kwa mkazi,kuti Mulungu Mwiniwake…Inu mukudziwa zomwe Mulunguanachita? Iye—Iye sankachita kanthu koma basi…Iye anazikaHema Wake pakati pa athu. Mulungu ankakhala mu Hemawotchedwa Yesu Khristu. Iye anadzangomanga Hema Wakelimodzi nafe, anadzakhala…(Ine—ndidzalalikira pa izommawa, kotero ndibwino kuti ine ndizisiye izo zokha.) Tsopano,kuti—momwe hema wa Mulungu—kapena anadzakhala ndiife…45 Ndipo tsopano Mulungu ali mwa ife. Yesu ananena muYohane 14, “Mu tsiku limenelo inu mudzadziwa kuti ine ndirimwa Atate, Atate ali mwa Ine, ndi Ine mwa inu, ndi inu mwaIne.” Mulungu mwa ife. Cholinga chake chinali chiani? Kutiadzachite dongosolo Lake.46 Mulungu anali ndi dongosolo. Iye ankafuna kuti azidzagwirantchito pakati pa anthu, ndipo Iye anazibweretsa izomu Lawi la Moto, umene unali Moto wachinsinsi umeneunkapachikika pamwamba pa ana a Israeli. Ndiye Motowomwewo unadzawonetseredwa mu thupi la Yesu. Ndipo Iyeanati Iye anali Moto umenewo, “Asanakhalepo Abrahamu,INE NDINE.” Iye anali Moto umenewo. Iye anati, “Inendinabwera kuchokera kwa Mulungu, ndipo ine ndikubwererakwa Mulungu.” Ndipo itachitika imfa Yake, kuikidwa, ndichiukitsiro, PauloWoyera anakomana naye Iye pa njira—pamenedzina lake linali likadali Sauli—pa njira yaku Damasiko, ndipoIye anali aponso atabwereranso ku Lawi la Moto ilo. Kuwalakunathimitsa maso ake. Ndiko kulondola.47 Ndipo pano Iye ali lero, Lawi la Moto lomwelo, Mulunguyemweyo akuchita zizindikiro zomwezo, ntchito zomwezo.Bwanji? Iye akugwira ntchito pakati pa anthu Ake. Iye alimwa ife. Ine…Iye ali ndi inu tsopano, “koma ine ndidzakhalamkati mwanu. Ine ndidzakhala ndi inu, ngakhale mkati mwanu,mpaka ku mapeto a chimaliziro,” mapeto a dziko. Iye adzakhalaali nafe.48 Tsopano, zindikirani. Yesu anali atawatuma iwo kutiapite uko ku Yerusalemu ndi kukadikira. Mawu oti tarryamatanthauza “kudikirira,” samatanthauza kupemphera,amatanthauza “kudikirira.” Iwo sanali otsatira oyenera apabe

Page 13: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 439

kuti azilalikira, chifukwa iwo ankangodziwa chiukitsiroChake mwa Umunthu Wake, pa kumuwona Iye kunja. Iye—Iyeanawalamulira iwo kuti asati azikalalikiranso, kuti asamachitekalikonse mpaka poyamba iwo atadzazidwa ndi Mphamvuyochokera kumwamba.

Ine sindikukhulupirira kuti mlaliki aliyense ali wotumidwandi Mulungu kapena kuti akhoza kukhala wodzozedwamolondola…Chifukwa Mulungu ndi wopandamalire. Ndipochimene Mulungu amachita kamodzi, Iye amachichitanthawizonse. Tsopano, ngati Mulungu sakanati awalole iwo kutiazilalikira mpaka iwo atapita ku Pentekoste ndipo atalandirachowachitikira cha Chipentekoste, palibe munthu, kupatulachikhumbo china chakuya chakechake kapena bungwe linalitamutuma iye, ali ndi ufulu wolowa mu guwa mpaka iyeatadzazidwa kaye ndi Mzimu Woyera. Ndizo ndendendekulondola. Chifukwa iye akuwatsogolera iwo mwa lingalirolaluntha la bungwe lina mpaka iye atadzazidwa ndi MzimuWoyera; ndiyeno, iye akuwapatsa iwo chakudya cha nkhunda;Mwanawankhosa ndi Nkhunda,monga ife tinaziyankhula usikuwatha.49 Tsopano zindikirani. Iye anati, “Pitani uko ku Yerusalemundipo mukakhale komweko; muzikangodikirira kumenekompaka ine nditatumiza lonjezo la Atate.” Ndiyeno, kodi iwoanachita chiani? Iwo analipo wani handiredi ndi twente a iwo,amuna ndi akazi. Iwo anapita mu chipinda chapamwamba kukachisi.

Tsopano, linali kuyandikira tsiku la Phwando la Pentekoste,kuchokera ku kuyeretsa kwa malo opatulika, kupha kwamwanawankhosa wa paskha mpaka—kudza kwa Pentekoste,zomwe zinali zipatso zoyamba za zokolola, chisangalalo,chisangalalo cha Pentekoste. Ndi pamanyumba…50 Tsopano, ine ndakhala ndiri mmaiko. Maiko akummawa sikawirikawiri kuti amakhala ndi makwerero opita mmwambamkati. Makwererowo anali kunja. Kunja kwa kachisi, ifetimauzidwa, uko kunali makwerero ankalondolera mpakammwamba ku kachipinda kakang’ono patali pomwe, opitammwamba, ndi mmwamba, ndi mmwamba, mpaka iwe umafikaku kachipinda kakang’ono mmwamba umo, monga chipindachosungira zinthu pamwamba pa kachisi, mtundu winawa chipinda chaching’ono, chipinda chapamwamba. NdipoBaibulo linati iwo anali mkati mmenemo ndipo zitseko zinalizitatsekedwa, chifukwa iwo ankachita mantha ndi Ayuda,chifukwa iwo akanawakhadzula iwo chifukwa chomupembedzaAmbuye Yesu, Kayafa wansembe wamkulu, ndi Pontiasi Pilato,ndi iwo atamuika kale Iye ku imfa. Chotero iwo ankatiathane nawo onse otchedwa Akhristu. Ndipo zitseko zinalizitatsekedwa, ndipo iwo anali akudikirira.

Page 14: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

440 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

51 Tsopano, mu zipinda izo monga icho, munali mopandamazenera. Mazenera anali zinthu zazing’ono zotchingidwazokhala ndi zonga zitseko, iwe unkazikoka kuti utsegule. Muzipinda zimenezo munkakhala nyali zazing’ono za chikoloboizomwe zinkapachikidwa chozondotsa ndi kumayaka…Ngati inu mungadzafike konse mu California ku Cafeteriaya Clifton, mudzapite ku chipinda cha pansi, ndipo inumudzakapeza china cha mtundu wofanana, ndi chipindachapamwambacho. Kodi inu munayamba mwapitamo uko?Ndi angati muno anayamba apitamo uko? Ine ndikuwawonaanthu mukugwedeza mitu yanu. Chabwino, inu mukudziwachimene ine ndikuchikamba. Chabwino. Mudzapite pansipamenepo, ndipo inumudzakawuonaMundawaGetsemane; inumusanatero, inu mudzakalowe mu zipinda zina zachikale izo.Izo ziri ndendende moona. Uko inu mukapeza nyali yaing’onoya mafuta a azitona ili ndi chingwe chaching’ono cha ubweyamkati mwake, chikuyaka.52 Tsopano, tiyeni tinene kuti iwo anali mmwamba umo,atakwera chozungulira kunja uku. Iwo anakwera umo ndipoanakadzibisa okha, chifukwa iwo ankachita mantha ndi Ayuda.Yesu sanawauze iwo kuti adzapite mu chipinda chapamwamba.Iye anangoti, “Mukadikirire ku Yerusalemu.” Iwo akanakhalapansi apa mu nyumba, nzovuta kuti udziwe zomwe zikanatizichitike. Iwo akanabwera ndi kudzawatenga iwo. Chotero iwoanapita ku kanyumba kachikale mu chipinda cha mmwamba,mmwamba momwe umo mu chipinda cha mdenga, ndipommenemo, iwo anatseka chipindacho kuti Ayuda sakanakhozakufika kwa iwo. Ndipo iwo anakhala mmenemo akudikira kwamasiku khumi.53 Tsopano, tsopano, ife tiri mu Machitidwe 1. Tsopano,mvetserani mwatcheru tsopano. Inumwachigwira chithunzicho?Kunja kwa nyumba makwerero aang’ono anapita mmwamba,ndipo iwo anakalowa mu chipinda chaching’ono ichi. Pansimu kachisi mkati iwo ali ndi Phwando la Pentekoste. O, ukokunali kukuchitika nthawi yaikulu. Tsopano, pamene tsiku laPentekoste linadza kwathunthu, iwo anali onse ndi lingalirolimodzi, lingaliro limodzi, akukhulupirira kuti Mulungu analiwoti atumiza lonjezo limenelo. Ndipo mulole munthu aliyensemuno alowe mu lingaliro lomwelo usikuuno ndipo awonezomwe ziti zichitike. Izo ziyenera kubwereza. Ilo ndi lonjezochimodzimodzi basi monga iwo anali nalo. Mukuona?54 Kodi iwo anali kuchita chiani? Ankatsatira malangizo,ankatsatira m—m—malamulo a Mulungu: “Dikiranimpakana…”55 Tsopano, iwo ankachita mantha ndi Ayuda. Tsopano,zikumbukirani izo. Iwo anali kuwaopa Ayuda. Tsopano,zonse mwadzidzidzi uko kunadza phokoso longa mphepo yankokomo. Iyo siinali mphepo yankokomo; iyo inali ngati mphepo

Page 15: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 441

yankokomo. Ine ndiwerenga ndemanga mu maminiti pang’onookha ya womasulira. Ilo linali longa mphepo yankokomo.Mwa kuyankhula kwina, iyo inali mphepo yauzimu (o!),chinachake chimene iwo amakhoza kuchimverera. Mphepoyoinali mkati mwa iwo. Pamenepo panadza—mphepo yankokomo,yonga mphepo yankokomo. Mphepoyo siinali kukukuma,koma inkangomveka monga mphepo ya nkokomo, yongachinachake chikuti [M’bale Branham akupanga phokoso lamphepo—Mkonzi.] Kodi inu munayamba mwaimverera iyo? O,mai! Yonga nkokomo wa mphepo. Tsopano penyani. Ndipo iyoinadzaza…Tsopano, umu anati “onse,” komamu Chigriki anati“Yonse (wankulu Y-o-n-s-e), Nyumba Yonse,” paliponse mkatiumo. Mng’alu uliwonse, ngodya, ndi pamphanga pankangakuti panali podzaza nayo. Osati kuti, “Nkuti, Abale, kodiinu mukumverera zomwe ine ndikumverera?” Ayi! Iyo inalipaliponse, monga mphepo yankokomo. Tsopano penyani. “Apopanadza phokoso longa nkokomowamphepo yamphamvu ndipo(cholumikizira. Tsopano muziwapenya “ma ndipo” amenewo.Ngati inu simutero, inu muwapangitsa Iwo kunena chinachimene Iwo ali kunena. Mwaona?)—ndipo monga (ndichochimene chinachitika choyamba chinali phokoso, chinachakechonga n—nkokomo wa mphepo unadza pa iwo)—ndipo (inumukukumbukira, usiku watha ine ndinapita ku golosale ndipondinakagula mtanda wa mkate ndi nyama ina. Ndi chinachakechomwe chinapita limodzi nacho. Mkate ndi chinthu chimodzi,nyama ndi chinanso. Ndipo nkokomo unali chinthu chinachimene chinawakhudza iwo)—ndipo pamenepo panawonekerakwa iwo, (pamaso pawo)malirime—malirime ogawanika.”56 Kodi aliyense muno anayamba waonapo MalamuloKhumi a Cecil DeMille’? Kodi inu munazindikira pameneMalamulowo anali kulembedwa? Momwe iye anazigwirira izo,ine sindimadziwa. Zinalipo zinthu ziwiri kapena zitatu zomweine ndinaziwona umo zomwe ine ndinazikonda kwenikweni.Chinthu choyamba ndi kuwala kwa ambara kuja, umo ndindendende momwe Iko kumawonekera. Mukuona? Chinthuchina chinali pamene Malamulo anali atalembedwa, ndipoizo zitatha, kodi inu munazindikira kuulukira kwina kwaLawi la Moto lalikulu lija, apo panali malawi aang’ono amoto akuwulukira kwina? Kodi inu munazizindikira izo?Tsopano, ndicho chimene ine ndikuganiza kuti ichi chinalipa Pentekoste. Apo panawonekera kwa iwo…Kotero iwoankakhoza kukuwona Iko. Iwo sanati, “Apo anagwera mkatimwao.” Koma pamenepo panawonekera kwa iwo malawi (ifetizitcha izo), malirime, ngati lirime monga lirime ili apa, [M’baleBranham akuwonetsera—Mkonzi.], mawonekedwe a lirime, lawila moto. Tsopano, khutu—monga ine ndinati, khutu ndi khutu;chala ndi chala. Chala sizikutanthauza kuti iwe unazimvereraizo; izo zikutanthauza kuti icho chinkawoneka monga chala.Ndipo ngati ilo likanakhala liri khutu, izo sizikanatanthauza

Page 16: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

442 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

kuti iwo analimva ilo; izo zinkawoneka monga khutu. Uwuunali moto umene unkawoneka monga lirime, osati winawakeakuyankhula, moto umene unkawonekamonga lirime.57 Tsopano mvetserani. Penyani momwe Chigrikichikuwerengekera pa izo apa:

Ndipo mwadzidzidzi apo panadza Phokoso…longaMphepo ya nkokomo wamphamvu…(Ya 3—ndime ya3.)Ndipo Malirime Ogawanika anawonekera kwa

iwo,…(Osati malirime ogawanika anali mkati mwawo,kapena iwo anali kuyankhula ndi lirime logawanika,awo anali malirime ogawanika omwe anawonekera kwaiwo. Tsopano penyani. Iwo sali pa iwo apabe. Ali muchipinda mmenemo, kuzungulira zungulira umo mongamu mphepo iyi.)…kwa iwo, monga Moto—MalirimeOgawanika anawonekera kwa iwo,…(Ndizo patsogolopawo.)…onga Moto,… (Malirime onga moto.)…ndipo limodzi… (Lalokha.) …linadzatera pa winaaliyense wa iwo. (Osati anapita mkati mwawo; komaanadzatera pa iwo.)

58 Tsopano, mukuona momwe King James akanati aziponyereizo kumbali: “Ndipo malirime ogawanika anabwera pa iwo,kapena anadzakhala (kodi zikuwerengeka motani mu KingJames umo?)—anadzakhala pa iwo.” Mukuona? Tsopano, iwosakanakhoza kupita mmwamba umo ndi kukakhala pansi. Ifetikudziwa izo. Koma mwapachiyambi anati, “Iwo anadzaterapa iwo,” ine ndikukhulupirira; si choncho izo? Mundiroleine ndizipeze izo ndendende moona. Eya! “…anadzatera paaliyense wa iwo.” Lirime limodzi la moto linadzatera pa aliyensewa iwo. Mukuona apo? Kodi inu mukuzimvetsa izo? Ndichochinthu chachiwiri chimene chinachitika. Choyamba chinalimphepo, kenako kuwonekera kwamalirime amoto.59 Munali mchipinda chaching’ono ichi umu muli nyalizazing’ono za mafuta zikuyaka. Taganizani za iwo atakhalammwamba umo. Ndipo wina nati, “O!” Iye anayang’anaponseponse mnyumbayo; iwo anali ponseponse mnyumbayo.Ndiye iwo anati, “Taonani!” Malirime a moto anayamba ku—kubwera kuzungulira mchipindamo. Tsopano penyani. Ndipopamenepo anawonekera malirime amoto awa.

Tsopano penyani chotsatira:Ndipo…(Cholumikizira china; chinachakenso

chinachitika.)…iwo onse anadzazidwa ndi MzimuWoyera,…(Chinthu chachiwiri chimene chinachitika.)

60 Tsopano taonani, ife tikufuna kuti tizisinthe izomozungulira nkuti, “Iwo anali ndi malirime a moto, ndipoapa akubwebweta pamenepo; ndiyeno anatuluka panja ndipoanayamba kuyankhula mu lirime losadziwika.” Mulibe chinthu

Page 17: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 443

chotero monga icho mu Malemba, mzanga. Aliyense yemweamayankhula ndi lirime losadziwika pa kulandira MzimuWoyera amachita izo mosiyana ndi Baibulo. Ndipo inendisonyeza kwa inu mu maminiti pang’ono ndi kutsimikizirakwa inu kuti ine ndimakhulupirira kuyankhula mu malirimeosadziwika, koma osati pakulandira Mzimu Woyera. Iyo ndimphatso yaMzimuWoyera.MzimuWoyera ndiMzimu.61 Tsopano penyani. Malirime awa anali mu chipinda mongamoto, ndipo iwo anaikidwa pa aliyense. Ndiye iwo anadzazidwandi Mzimu Woyera (chinthu chachiwiri), ndipo kenako,iwo atadzadzidwa kale ndi Mzimu Woyera, atayankhulandi malirime, osati ndi malirime, ndi zinenero. Kodi inumwazindikira izo? Iwo anayamba kuyankhula ndi zinenero zinamomwe Mzimu unkawapatsira iwo kuti ayankhule. Tsopano, izizinamveka konsekonse.62 Tsopano penyani. Tsopano, tiyeni titenge kalongosoledwekachiwiri kuti inu musati muziiwale izi tsopano. Malinganandi Lemba, mu chipinda chapamwamba akuyembekezera,mwadzidzidzi phokoso longa mphepo yankokomo, yomweinali pa iwo; umenewo unali Mzimu Woyera. Ndi angatiakukhulupirira kuti kumeneko kunali kuwonekerapo kwaMzimu Woyera? Monga mphepo, mphepo yauzimu. Ndiye iwoanazindikira. Ndipo kuchokera mmenemo munali malirimeaang’ono a moto, handiredi ndi twente a iwo, ndipo anayambakudzakhazikika pansi ndipo anadzakhala pa wina aliyense waiwo. Chinali chiani icho? Chinali chiani? Lawi la Moto, ameneanali Mulungu Mwiniwake akudzigawaniza Iyeyekha pakati paanthu Ake, kubweramkati mwa anthu. Yesu anali nacho chinthuchonsecho; Iye anali nao Mzimu Woyera wopanda muyezo;ife timaulandira Iwo mwa muyezo (Inu mukuona chimene inendikutanthauza?) chifukwa ndife ana okhazikitsidwa. MoyoWake—Moyo Wake Wamuyaya unali kubwera mkati. Tsopano,ndi chiani chinachitika? Ndiye iwo onse anadzazidwa ndiMzimuWoyera.63 Tsopano, ine ndikufuna kuti ndikufunseni inu chinachake.Ndi liti pamene mphekeserayo inayamba? Ngati iwo akanatiachite kubwera kuchokera mchipinda chapamwamba ichokuti atsike pansi ndi masitepe amenewo ndi kukafika mumabwalo a nyumba yachifumu—kapena uko mu—ku mabwaloa kachisi, kumene kunali mwinamwake mdadada wa mumzinda kuchokera, kumene iwo anali, chipinda chammwambandi kutsika, mu mabwalo kumene anthu onse anasonkhanapalimodzi…Ndipo iwo anabwera kuchokera umo okhalangati aledzera ndi Mzimu. Pakuti anthu anati, “Amuna awaaledzera vinyo watsopano.” Iwo anali asanawonepo chirichonsechonga izo.64 Ndipo aliyense ankayesera kunena kuti, “Mzimu Woyerawabwera. Lonjezo la Mulungu liri pa ine. Ine—ine ndadzazidwa

Page 18: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

444 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

ndi Mzimu.” Ndipo iye pokhala Mgalilea, mwamuna yemwe iyeanali kuyankhula naye, Mluya kapena Mperisi, ankamumva iyemu chinenero chake chomwe.65 “Ife tikuwamva bwanji (osati mu lirime losadziwika)—ife tikuwamva bwanji munthu aliyense mu lirime lomwe ifetinabadwira. Ndipo kodi onse awa omwe akuyankhulawasi Agalilea?” Ndipo anali mwinamwake akuyankhulaChigalilea…Koma pamene iwo ankawamva iwo, izo zinalimu chinenero chomwe iwo anabadwiramo. Ngati si choncho,ine ndikufuna kuti inu mundifunse ine—mundiyankhe inefunso ili: Zinali motani kuti Petro anaimirira pamenepo ndipoankayankhula mu Chigalilea, ndipo gulu lonselo linkamvachimene iye ankanena? Miyoyo zikwi zitatu inadza kwa Khristuapo pomwe ndipotu Petro akuyankhula mu chinenero chimodzi.Zedi! Uyo anali Mulungu akuchita chozizwitsa. Petro, kwaomvetsera omwewo omwe anapangidwa ndi a ku Mesopotamia,ndi alendo, ndi otembenuzidwa, ndi chirichonse ochokera kudziko lonse lapansi anali ataima pamenepo…Ndipo Petroanaima ndi kumalalikira mu chinenero chimodzi, ndipo munthualiyense ankamumva iye, pakuti zikwi zitatu analapa ndipoanabatizidwa mu Dzina la Yesu Khristu apo pomwe. Zinalimotani zimenezo?66 Taonani, abwenzi, ine sindingakhoze kuyembekeza m’balewanga wa chipembedzo, wa Chipentekoste kuti angazivomerezeizo pakali pano. Koma inu muzitsatire izo kudutsa mu Baibulondipo mundiuze ine nthawi iliyonse yomwe iwo analandirapokonse Mzimu Woyera nayankhula mu malirime omwe iwosanali kudziwa chimene iwo anali kuchiyankhula. Ndipo ngatinjira yake ili imeneyo yomwe anaulandirira Iwo uko, Mulunguwochita mwayekha…Izo ziyenera kumachitika nthawi iliyonsemwanjira yomweyo.67 Tsopano, ine sindingakhoze…Tsopano, kunyumba yaKorne-…Ife tikukumbukira, pamene ife tinapita ku Samariakuja, usiku watha, ife tinakapeza kuti uko kunalibe chinthuchimodzi chinanenedwa chokhudza iwo kumva mu lirime linalirilonse, panalibe zinanenedwa zokhudza izo. Koma pameneiwo anapita ku nyumba ya Kornelio, kumene kunali mafukoatatu osiyana a anthu, iwo anayankhula mu malirime. Ndipopamene iwo anatero, ngati iwo anatero, iwo anaulandiraIwo, Petro anati, mwanjira yomweyo imene anaulandiriraIwo pachiyambi. Ndipo iwo anadziwa kuti Amitundu analiatalandira chisomo kuchokera kwa Mulungu, chifukwa iwoanali atalandira Mzimu Woyera chimodzimodzi monga iwoanachitira pachiyambi. Ine ndiri nalo funso pano, chinachake paizo mu maminiti pang’ono. Ine ndikufuna kuti ndiyike maziko,chotero inumukhoze kuwona zomwe izo ziri.68 Tsopano, ine sindingakhoze kuyembekezera anthuomwe aphunzitsidwa mosiyana…Ndipo mvetserani kwa

Page 19: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 445

ine, abale anga okondedwa, ofunika, Achipentekoste. Inesindingakaphunzitse izi kunja. Izi ndi…Ine sindikanachitakanthu koti kayambitse kutsutsana. Koma ngati ife sititengaChoonadi, ndi liti pamene titi tidzayambe? Ife tiyenerakuti tikhale nacho chinachake choti chichitike pano chotichitiwongole ife. Ife tiyenera kuti tipeze chisomo chokwatulitsapano tsopano. Choonadi chiyenera kutulukirapo.69 Akanachita chiani munthu ngati iye akanakhala wogontha,ndi wosayankhula, ndipo akanakhala wosayankhula nkomwe?Kodi iye akanakhoza kulandira Mzimu Woyera? Bwanji ngatiiye akanakhala wopanda lirime pa kuyamba pomwe, ndipomunthu wosaukayo akufuna kuti apulumutsidwe? Mukuona?Ndi Mzimu Woyera, ndiwo ubatizo. Ndiyeno, mphatso zonse izimonga kuyankhula mu malirime, kutanthauzira kwa malirime,ziri pambuyo iwe utabwera mu Thupilo mwa ubatizo wa MzimuWoyera. Pakutimphatso zimenezo ziri muThupi laKhristu.70 Tsopano, chifukwa chimene ine ndikuti…Tsopano, penyanikuno. Kodi inu mukanayembekeza mpingo wa Katolika, umeneunali mpingo woyamba kupanga bungwe mu dziko pambuyopa atumwi…Ndiye mpingo wa Katolika unapanga bungwe, o,zaka mazana angapo pambuyo pa imfa ya mtumwi wotsiriza,mwina sikisi handiredi ndi—zaka pambuyo pa atumwi, pambuyopa Nicene Council pomwe, pamene makolo a Nicene anabwerapalimodzi ndipo anapanga bungwe; ndiye iwo anawuyikampingo wa konsekonse, umene unali mpingo wa Katolika.Mmenemo iwo anapanga mpingo wa kwa dziko. Ndipo mawu otikatolika amatanthauza “konsekonse”; ndiko kulikonse. Iwo…Roma—Roma wachikunja anatembenuzidwa kukhala Romawaupapa. Ndipo iwo anaikapo papa kuti akhale mutu kutiatenge malo a Petro, chimene iwo ankaganiza ndipo ankanenakuti Yesu anamupatsa mafungulo aku Ufumu. Ndi kuti Papaanali wosalephera, ndipo alipo panobe kwampingowaKatolika.Kuti…Mawu Ake ali lamulo ndi langizo. Iye ndi papawosalephera. Izo zinapitirira.71 Ndiyeno, chifukwa kuti iwo sanali kugwirizana ndichiphunzitso cha Chikatolika ichi, iwo anali kuikidwa kuimfa, kuwotchedwa pa nkhuni, ndi china chirichonse. Ife tonsetikuzidziwa izo kupyolera mu zolemba zopatulika za Josephus,ndi Bukhu la Fox la Ofera, ndi ochuluka ena opatulika…Two Babylons la Hislop, ndi—mbirizakale zazikulu. Ndiye,izo—zitatha zaka fifitini handiredi, momwe ife tikudziwira, zaMibadwo ya Mdima, Baibulo linachotsedwa kwa anthu. NdipoIlo linali—Ilo linabisidwa ndi ansembe aang’ono, ndi ena otero,ife timamva.72 Ndiye zitachitika izo panadza kukonzanso koyamba kumenekunali Marteni Lutera. Ndipo iye anabwera poyera nanenakuti mgonero umene Katolika umautcha thupi—thupi lenilenila Khristu, iwo unali kungoimira thupi la Khristu. Ndipo

Page 20: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

446 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

iye anaponyera mgonero pa chotchingira ku guwa, kapena pamasitepe, ndipo anakana kuti aziwutcha iwo thupi lenilenila Khristu, ndipo analalikira, “Olungama azikhala moyomwa chikhulupiriro.” Tsopano, inu simungakhoze kuyembekezampingo wa Katolika kuti uvomerezane ndi iye, ndithudi ayi,pamene mtsogoleri wawo wosalephera atawauza iwo kuti ayi.Chabwino.

73 Ndiye Marteni Lutera atatha, kulalikira Kulungamitsidwa,Joni Wesile anabwera motsatira akulalikira Kuyeretsedwa.Ndipo iye ankalalikira kuti munthu, akatha kulungamitsidwa(zonsezo ndi zabwino)—koma iwe umayenera kuti uyeretsedwe,kutsukidwa, muzu wa zoipa uchotsedwe mwa iwe ndi Magazia Yesu. Tsopano, inu simungakhoze kuwayembekeza Achiluterakuti azilalikiraKuyeretsedwa, chifukwa iwo sati azichita izo.

74 Wesile atatha kulalikira Kuyeretsedwa, ndi ena ochulukaatachoka kwa iwo, chimene chinadzakhala Methodisti ya chiWesile, ndi Nazerini, ndi ena otero, omwe ankasunga motochiyakire kupyola mu m’badwo wawo, ndiye potsatira kunadzaPentekoste ndipo anati, “Pakuti, Mzimu Woyera ndiwo ubatizo,ndipo ife timayankhula ndimalirime pamene timaulandira Iwo.”Zedi. Ndiye pamene izo zinabwera apo, inu simukanakhozakuwayembekeza a Nazareni, ndi Amethodisti Achiwesile, ndiena otero kuti azikhulupirire izo. Iwo sakanati achite izo. Iwoanazitcha izo mdierekezi. Chabwino. Chinachitika ndi chiani?Iwo anayamba kugwa; Pentekoste inayamba kuwuka. Tsopanoiyo yawuka mpaka pa malo pomwe Pentekoste yalandirakugwedezedwa kwake. Iyo yapanga bungwe ndipo yatuluka, salikulandira china chirichonse. Iwo ali nawo malamulo awo awondi malangizo, ndipo izo zikukhazikitsa icho.

75 Tsopano, pamene Mzimu Woyera ukubwera umo ndikudzaulula Choonadi cha chirichonse ndi kuzitsimikizira izondi Kukhalapo Kwake komwe ndi mwa Mawu Ake, inusimungakhoze kuwayembekeza anthu Achipentekoste kuti aziti,“Ine ndivomerezana nazo izo.” Iwe ukuyenera kuti uziyimawekha monga Lutera anachitira, monga Wesile anachitira, ndimonga ena onse a iwo ankachitira. Iwe uyenera kumaima paizo chifukwa oralo liri pano. Ndipo ndi chimene chikundipangaine kukhala bakha wonyansa. Ndi chimene chikundipanga inekukhala wosiyana.

76 Ndipo ine sindingakhoze kuyamba monga M’bale wangawofunika Oral Roberts, ndi Tommy Osborne, Tommy Hicks,ndi iwo, chifukwa mipingo siingagwirizane ndi ine. Iwo amati,“Iye amakhulupirira mu chitetezero chamuyaya. Iye ndi waBaptisti. Iye samakhulupirira mu kuyankhula mmalirime ngatiumboni woyamba wa Mzimu Woyera. Pitani kutali ndi munthuameneyo!” Mukuona?

Page 21: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 447

77 Koma bwerani maso ndi maso ndi izo. Yang’anizanani nazoizo. Iwo akhoza kuyang’anizana ndi Achilutera, a—Amethodistiakhoza. Apentekoste akhoza kuyang’anizana ndi Amethodisti.Ine ndikhoza kuyang’anizana ndi Apentekoste nazo. Ndikokulondola ndendende. Ndi zoona. Nchifukwa chiani zirichoncho? Ife tikuyenda mu Kuwala pamene Iye ali mu Kuwala.Mukuona? Ife tikuyenda chokwera mu Msewuwawukuluwa Mfumu, ndipo zikamafika patali, chisomo chochulukachikumaperekedwa, mphamvu yochuluka ikumaperekedwa,chauzimu chochuluka chikumaperekedwa. Ndipo ndife apo. Ilindi ora lomweMzimuWoyera wabwera pansi mu mawonekedwea Kuwala monga Iye analiri pachiyambi, Lawi la Moto, ndipowadziwonetsera Yekha, akuchita zinthu zomwe zomwezo zimeneIye ankazichita pamene Iye anali kuno pa dziko lapansi. NdipoYesu anati, “Inu mumawadziwa bwanji ngati iwo akulondolakapena ayi? Ndi zipatso zawo inu mudzawadziwa iwo. Iyeamene akhulupirira mwa Ine, ntchito zimene Ine ndichitanayenso azidzazichita. Zizindikiro izi zidzawatsatira iwo ameneakhulupirira.”78 Tsopano, abale anga Achipentekoste. Ine ndiri ndi inu.Ndine mmodzi wa inu. Ine ndiri nawo Mzimu Woyera.Ine ndayankhulapo mu malirime, koma ine sindinawalandireiwo pa kulandira Mzimu Woyera. Ine ndiri ndi ubatizo waMzimu Woyera. Ine ndinayankhula mu malirime, ndanenera,ndili nazo mphatso za chidziwitso, nzeru, kutanthauzira, ndichirichonse chikuchitika. Koma ndine womvera ku chirichonsecha zinthu zimenezo, chifukwa tsopano ndine mwana waMulungu. Mphamvu, Moto wa Mulungu uli mu moyo wanga;lirime lamoto lija limene linadzakhalapo—linabweramkati mwaine ndi kuwotchamo chirichonse chimene chinali chosiyana ndiMulungu, ndipo tsopano ine ndikutsogozedwa ndi Mzimu Wake.Iye angati, “Pita uko,” ndipo ine ndimapita. “Pita uku”; inendimapita. “Yankhula pano”; ine ndimayankhula. “Ndipo chitaichi, icho, ndi chinacho.” Ndi inu apo, monga choncho…Iweukutsogozedwa ndi Mzimu. Ameneyo ndi Mulungu mwa iwe,akuchita chifuniro Chake. Ziribe kanthu chimene icho chiri, Iyeakuchita chifuniro Chake.79 Tsopano,mverani.Mundilole ine ndiwone—ndiwerenge panoife tisanayambe mafunso pa lexicon pano. Tsopano, kuchokerakuKumasulira kwa ku Vatican, Volume 7, 190—1205:

“Ndi kovuta kuti udziwe ngati linali liwu laanthu awo omwe ankayankhula mu chinenerochachirendo; kapena zonenedwa kapena mphekeseraya kuchitika kwa mphepo yauzimu yankokomo yomweinalisangalatsa gulu.”

Iwo sankakhoza kuzimvetsa izo. Tsopano penyani. Kaya apoanali anthu…

Page 22: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

448 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

80 Ine ndingolongosola. Pano pali gulu la osauka, Agalileaolimba. Ndipo apa iwo ali uko mu msewu. Iwo analiasanawonepo chirichonse chonga izo: manja awo ali mumlengalenga, akuchokera ku chipinda chapamwambaicho, akutsika makwerero awo, kutuluka kumka uko,atangodzazidwa; iwo anali asanayankhule apobe. Mukuona?Apa iwo anabwera akutsika kudutsa apo. Ndipo tsopano, tiyenititi, iwo anali kunja uko akuzandima akuzungulira mwa izi.Ndipo anthu anati…Mgriki anathamangira kwa ine nati, Inendikuyankhula mu Chigalilea.

Iwe ukuthamangira kwa iye nkuti, “Ndipo chavuta nchianindi iwe, Mnyamata?”81 “Ine ndadzazidwa ndi Mzimu Woyera. Mphamvu yaMulungu inagwera uko mu chipinda icho. Chinachakechinachitika kwa ine. O, Ulemerero kwaMulungu!”

Ndipo mmodzi wina chakuno, iye anali kuyankhula kwaMluya, ndipo iye pokhala Mgalilea akunena Chiluya—chinenerocha Chiluya.82 Tsopano, iwo sangakhoze kunena, kodi inali mphepo yankokomo yomwe inawakokera anthuwo palimodzi pameneunyinji unabwera palimodzi, kapena kodi kunali kuyankhulamu chinenero chachirendo chimene iwo anali kuyankhula?Tsopano, Baibulo silimatero ndendende…Inu muli nazo zinthuziwiri zoti muzipenye. Izo zinali…A—akunja anati, “Zirimotani kuti ife tikumumva munthu aliyense mu lirime lathulomwe ife tinabadwa nalo?” Izo sizinanene kuti iwo analikuziyankhula izo, koma iwo anali kuzimva izo.83 Ndiye gulu lomwelo, anthu omwewo, analongosola ichi.Petro analumphira pa chinachake ndipo anati, “Inu amuna akuGalileya, ndi inu okhala mu Yerusalemu, lolani ichi chidziwikekwa inu (anthu amati iwo analibe chinenero cha Chigalilea)—lolani ichi chidziwike kwa inu ndipo mvetserani kwa mawuanga (chiani—kodi ndi chinenero chanji chimene iye analikuchiyankhula, kwa onse awo?); bwanji, awa sanaledzere mongainu mukulingalira, powona kuti ndi ora lachitatu la tsiku,koma ichi ndi chija chimene chinayankhulidwa ndi mneneriYoweli: ‘Ndipo zidzafika pochitika mu masiku otsiriza, ateroMulungu, Ine ndidzatsanulira Mzimu Wanga pa mnofu wonse.Ana anu aamuna ndi aakazi azidzanenera.’” Mopitiriza pitirizaiye anapita, ndipo anati, “Inu ndi manja oyipa munamupachikaMwana wa Mulungu wosalakwa. Davide anali atayankhula zaIye… ‘kusasiya moyo Wake mu gehena, ngakhale kuti Iyealole Woyera Wake Uyo kuti awone chivundi.’” Ndipo anati,“Lolani ichi chidziwike kwa inu kuti Mulungu anamupangaYesu yemweyu yemwe inu munamupachika zonse Ambuye ndiKhristu.” Ndipo pamene iwo anamva izi…Ameni! Ndani?Munthu aliyense pansi pa miyamba. Nchiani chinali kuchitika?

Page 23: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 449

Iye sanali kunena, “Tsopano, ine ndiyankhula mu Chigalilea; inendiyankhulamu ichi; ndipo ine ndiyankhulamu ichi…?…”84 Pamene Petro anali kuyankhula mawu awa, iwoanati, “Amuna ndi abale, kodi ife tingachite chiani kutitipulumutsidwe?” Ndipo Petro anawapatsa iwo kachitidweko.Ndimomwe izo nthawizonse zimachitikira. Mwaona?85 Ndi kusunthira mmwamba, kulimbikira kupitamwa Mulungu, kuyenda kwa pafupi. Inu mukudziwabwanji? Chabwino tsopano, pamene Lutera analandiraKulungamitsidwa, iye anazitcha izo Mzimu Woyera. Iwo unali.Mulungu anamiza pang’ono pa Iwo mmenemo. Ndiye Iyeananena chiani? Wesile analandira Kuyeretsedwa, ndipo anati,“Mnyamata, pamene iwe ufuula, iwe waulandira Iwo.” Komaambiri a iwo anafuula amene analibe Iwo. Pamene Pentekosteanayankhula mu malirime—malirime osadziwika, iwo anati,“Mnyamata, iwe uli nawo Iwo.”Koma ambiri a iwo analibe Iwo.

Palibe zinthu zotero zonga zizindikiro izo zodziwiraizo. “Njira yokha yomwe iwe umaudziwira mtengo,” Yesuanati, “ndi mwa chipatso chimene iwo umabala,” ntchito zaMzimu, chipatso cha Mzimu. Ndiye pamene inu mumuwonamunthu yemwe ali wodzazidwa ndi mphamvu, yemwe aliwodzazidwa ndi Mzimu Woyera, ndiye inu mumawonamoyo umene uli wosinthika. Inu mumawona zizindikiro izizikuwatsatira iwo amene akukhulupirirawo: “Mu Dzina Langaiwo azidzatulutsa ziwanda, azidzayankhula ndi malirimeatsopano. Ngati njoka idzawaluma iwo, iyo siidzawapwetekaiwo. Ngati iwo ati adzakhale ndi chinthu chokupha, nkuchimwa,icho sichikanadzawapha iwo. Iwo azidzaika manja paodwala, ndipo iwo azidzachira.” Mai! Zizindikiro za mtunduuwu zimawatsatira iwo amene amakhulupirira. Koma inumumalowamo chotani mmenemo? Mphatso zimenezo zirimu Thupi. Mumalowamo bwanji mu Thupi? Osati mwakuyankhula njira yako yoloweramo; koma pobatizidwa kulowamu Thupi limodzi (l Akorinto 12:13). Mzimu umodzi ife tonsetimabatizidwa kulowa mu Thupi limenelo ndipo timakhalaoyeneramphatso zonse. Ambuye akudalitseni inu.86 Tsopano, ngati wina ati ayimve tepi iyi kapena winawakemuno angati atsutse, kumbukirani, muzichite izo mwaubwenzi,m’bale, chifukwa ine ndimakukondani inu.93. Funso loyamba usikuuno:M’bale Branham, ine ndikuganiza

televizioni ndi themberero kwa dziko. Kodi inu mukuganizachiani za izi?

87 Chabwino, yense yemwe analemba ilo, ine ndatindivomerezane ndi inu. Iwo ayipanga iyo themberero kwadziko. Iyo ikanakhoza kukhala dalitso kwa dziko, koma iwoaipanga iyo themberero. Chirichonse monga izo, anthu angaokondedwa, ndi chimene iwe umayang’anapo iwemwini. Ngati

Page 24: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

450 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

televizioni ili themberero, ndiye nyuzipepala ili themberero,ndiye wailesi ili themberero, ndipo nthawi zambiri telefoni ili.Mwaona, mwaona, mwaona, mukuona? Ndi chomwe umapangakuchokera mwa iyo. Koma pokhala kuti m’bale ananena usikuwina, kuti palibe nkomwe programu iliyonse pa televizionipanonso; pali ndalama zochuluka zambiri. Alaliki osaukaomwe amalalikira Uthenga Wathunthu sangakhoze kukwanitsaprogramu pa televizioni. Chotero ndiye…M’bale ananena usikuwina, ine ndikukhulupirira, kapena kwinakwake, “Sasani fumbipa wailesi yanuyo,” kapena winawake, kapena, “Muibwezeretseiyo pa ngodya ndipo muzimvetsera ku maprogramu amenewo.”Ndiko kulondola.88 Koma, munthu wokondedwa, yense yemwe inu muli, inendithudi ndikuvomerezana ndi inu. Iyo yasanduka chimodzicha zinthu zotemberereka kwa mtundu wa anthu. Mmenemoiwo amatenga ndalama zonse izi zomwe zimayenera kuti zipiteku boma za misonkho, ndi kukaziika izo mu zolengeza pandudu zonse izi ndi maprogramu a mowa ndi zinthu zonga izo,ndi kuchotsera pa misonkho ya boma; ndiyeno iwo amabwerandi kudzawatenga alaliki ndi kuwakokera iwo kubwalo lamulandu kuti akapeze ndalama pang’ono kuchokera kwa iwo.Ine ndikuvomerezana ndi inu, ndi chinthu choyipisitsa. Tsopano,sindicho ayi…Inu mukudziwa, ndi chinachake basi chimeneiwe umapezamo. Zikomo inu, Mlongo, M’bale, yense yemwe inumuli yemwe munafunsa izo.

94. Tsopano, pano pali lina labwino. Funso: Alipo malo muBaibulo onga ngati l Samuele 18:10, amene amati mzimuwoipa wochokera kwa Mulungu unachita zinthu. Ine sindirikumvetsa “mzimuwoipawochokera kwaMulungu.” Chondetafotokozani izi.

89 Chabwino, mwina mwa thandizo la Ambuye, ine ndikhoza.Izi sizikutanthauza kuti Mulungu ndi Mzimu woipa. Komamzimu uliwonse wa chirichonse ndi womvera kwa Mulungu.Ndipo Iye amapangitsa chirichonse kugwira ntchito molinganandi zomwe Iye amafuna. Mwaona?90 Tsopano, pa funso lanu, inu mukuyankhula za mzimu woipaumene unapita kuchokera kwaMulungu kuti ukamuzunze Sauli.Iye anali molunda, mmawonekedwe osweka—chikhalidwe,chifukwa, malo oyamba, iye anali atabwerera mmbuyo. Ndipopamene iwe ubwerera mmbuyo, mzimu woipa—Mulunguamaloleza kuti mzimuwoipa uzikuzunza iwe.91 Ine ndikufuna kuti ndiwerenge kwa inu chinachake mu—mu mphindi. Ine ndiri ndi lingaliro lina pa izo pano. Mwaona?Mzimu uliwonse uyenera kukhala womvera kwa Mulungu. Kodiinu mukukumbukira pamene Yehosafati ndi Ahabu anali kupitaku nkhondo kuja? Ndipo chinthu choyamba inumukudziwa, apopanali—iwo anakhala ku zipata. Ndipo Yehosafati anali munthu

Page 25: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 451

wolungama, ndipo iye anati (mafumu awiri anakhala apo, ndipoiwo analumikizana mphamvu zawo limodzi)—ndipo chotero iyeanati, “Tiyeni tifunsire kwa Ambuye za ngati ife tingati tipiteuko kapena ayi.”92 Ndipo Ahabu anapita ndipo anakatenga anenerimazana anai omwe iye anali nawo, onse, ankawasunga iwonawadyetsa iwo ndi kuwanenepesa ndi chirichonse; iwo analimumawonekedwe abwino. Ndipo iwo anabwera pamenepo,ndipo iwo onse analosera ndi mtima umodzi, anati, “Pitaniuko, ndipo Mulungu akakupatsani inu chigonjetso. Pitani kuRamoti-gileadi uko ndipo kumeneko Mulungu akakutengeraniinu chinthucho.” Mmodzi wa iwo anadzipangira yekha nyangaziwiri ndipo anayamba kumazungulira ngati molongosolera,anati, “Ndi nyanga zachitsulo izi, inu mukawakankha iwompaka kuwachotsa mu dzikolo; ndi la inu.”93 Koma inu mukudziwa, pali chinachake chokhudza munthuwa Mulungu kuti samangopitira zonse izo. Mwaona? Ngati ichosichikumveka bwino ndi Lemba, pali chinachake cholakwika.Wokhulupirira woona aliyense…Kotero Yehosafati anati,“Chabwino, foro handiredi awo akuwoneka bwino. Iwoakuwoneka ngati anthu abwino.”

“O, iwo ali,” mwinamwake Ahabu anatero.Koma Yehosafati anati, “Kodi inu mulibe mmodzi wina?”

Bwanji mmodzi wina pamene inu muli nao foro handiredimchigwirizano chimodzi? Chifukwa iye ankadziwa kuti panalichinachake chimene sichinkamvekamwabwino basi.Mwaona?

Iye anati, “Inde, ife tiri naye mmodzi wina, mwana waImlah, kuntunda kuno,” anati, “koma ine ndimadana nayeiye.” Zedi. Inu mungatseke tchalitchi chake nthawi iliyonse inumungakhoze. Inu mungamthamangitse iye achoke mu dzikolo.Mwaona? Zedi. “ine ndimadana naye iye.”

“Nchifukwa chiani inumumadana naye iye?”“Iye nthawizonse amalosera zoipa motsutsana ndi ine.”

Ine ndikukhulupirira Yehosafati anadziwa apo pomwe panali—chinachake sichinali bwino.

Kotero iye anati, “Pitani ndipo kamutengeniMikaya.”Chotero iwo anapita kukamufuna iye, ndipo apa iye

anabwera uko…Kotero pamene iwo anapita uko, iwoanatumiza mthenga ndipo anati, “Tsopano, dikirani miniti.Tsopano, iwo ali ndi Madokotala Azauzimu mazana anaikumeneko. Iwo ndi opambana omwe alipo mu dzikolo, okhalandi Ph, ma LLD, ndi chirichonse.” Anati, “Tsopano, iweukudziwa, iwe munthu wamng’ono wosauka wosaphunzira, iwesuti ukatsutsane ndi alaliki onse awo.”94 Imlah ananena izi, kapena ine ndikutanthauza, Mikayaananena izi: “Ine sindinena kanthu mpaka Mulungu ataika icho

Page 26: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

452 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

mkamwa mwanga, ndiyeno ine ndinena ndendende chimeneIye wanena.” Ine ndikuzikonda izo. Ine ndikuzikonda izo. Mwakuyankhula kwina, “Ine ndikhala nawo Mawu.” Ziribe kanthuzomwe ena awo ananena. Iye anati, “Chabwino,” anati, “Inendikukuuza iwe. Ngati iwe sukufuna kuti utaidwe kunja, iwekulibwino unene chinthu chomwecho.”

Kotero iye anapita uko. Ndipo iye anati, “Kodi inendipite uko?”

Iye anati, “Zipitani.” Anati, “Ndipatseni ine usikuwu.Mundilole ine ndikambirane izo ndi Ambuye.” Ine ndikuzikondaizo. Chotero usiku umenewo Ambuye anawonekera kwa iye,ndipo tsiku lotsatira iye anapitako. Ndipo iye anati, pameneiye anali kupita uko, iye anati, “Zipitani; koma ine ndinawonaIsraeli ngati nkhosa zopanda m’busa, atamwazikana pa mapiri.”O, mai! Izo zinaphwesa mpweya mwa iye.

Ndipo iye anati, “Kodi ine sindinakuuzeni inu? Inendimadziwa izo. Umo ndi ndendende momwe iye amachitiranthawizonse, kunena chinachake choipamonditsutsa ine.”95 Bwanji? Iye anali kukhala ndi Mawu. Chifukwa? Mneneriasanadze iyeyu, Mawu a Mulungu ochokera kwa Eliya, mneneriweniweni, iye anati, “Chifukwa iwe wakhetsa magazi amunthu wosalakwa Naboti, agalu adzanyambita magazi akonawenso.” Ndipo anamuuza iye zoipa. Elisha anali atapita kaleKumwamba. Koma iye ankadziwa kuti Elisha anali ndi Mawua Mulungu, chotero iye ankakhala ndi Mawu. Ine ndikuzikondaizo. Kukhala ndi Mawu.96 Ngati Baibulo linati Yesu Khristu yemweyo dzulo, lero, ndikwanthawizonse; mphamvu Yake ikadali pano yofanana; MzimuWoyera ndi wa aliyense yemwe akufuna,mulole iye adze, khalanindi Mawu. Inde, bwana! Ziribe kanthu zomwe ena onsewoakunena. Kaya ndi odyetsedwa bwino bwanji ndi masukuluangati omwe iwo adutsamo, izo ziribe kanthu kochita ndi izo.

Chotero ndiye iye anati…Munthu wamkulu uyu ali ndinyanga pa mutu wake, mukazikankha izo—dzikolo kulilandakwa mfumu, iye anayenda mpaka anadzamumenya iye pakamwa (mlaliki wamng’ono uyu). Iye anazindikira kuti iyeanali woyera wodzigudubuza wamng’ono basi chotero palibekanthu kamene kakanati kanenedwe pa izo, chotero iyeanangomubwanyula iye pa kamwa. Iye anati, “Ine ndikufunakuti ndikufunse iwe chinachake.” Anati, “Ndi njira iti yomweMzimu wa Mulungu unapita pamene Iwo umachoka mwa inengati iwe uli nawo Iwo?”97 Iye anati, “Iwe ukamvetsa pamene iwe uti ukakhale mulinga kutali uko ngati wogwidwa.” Iye anati, “Ine ndinamuwonaMulungu atakhala pa mpandowachifumu (Ameni! Tsopanomvetserani!), ndipo khamu la Kumwamba linasonkhanamomuzungulira Iye.” Nchiani chinali chovuta? Mneneri

Page 27: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 453

wake anali atanena kale zomwe zikanati zidzachitike kwaAhabu. Mulungu…Uyo sanali Eliya yemwe ananena izo;uyo anali mneneri wodzozedwa. Amenewo anali Mawu aAmbuye, PAKUTI ATERO AMBUYE. Ndipo Mikaya anati,“Ine ndinaliwona khamu lonse la Kumwamba litasonkhanamomuzungulira Mulungu mu msonkhano waukulu. Ndipo iwoanali kuyankhulana wina ndi mzake. Ndipo Ambuye anati,‘Ndani yemwe Ife tingamutenge kuti apite uko—ndi ndaniwa inu yemwe angapite uko ndi kukamunyenga Ahabu, kutiakamutengere iye kunja uko kuti akakwaniritse Mawu aMulungu, kuti akamupangitse iye kulasidwa? Ndani yemwe Ifetingamupeze kuti apite kumeneko?’”98 Chabwino, mmodzi anali kunena uyu kapena mmodziuyo. Ndipo patapita kanthawi, mzimu woipa, mzimuwabodza unabwera kuchokera pansi ndipo unati, “Ngati Inumutangondilola ine. Ndine mzimu wabodza. Ine ndipita ukondi kukalowa mwa alaliki onse awo, chifukwa iwo alibeMzimu Woyera; ndipo ine ndiwapangitsa iwo (iwo angokhalaanyamata ophunzitsidwa ndi sukulu)—ndipo ine ndipita uko,ndi kukalowa mwa aliyense wa iwo, ndi kukawanyenga iwo,ndi kukawapangitsa iwo kunenera bodza.” Kodi iye ananenazimenezo? Ndipo iye anati, “Ndi momwe ife titi tiwanyengere.”Chotero iye anapita uko.

Iye anati—Mulungu anati, “Iwe uli ndi chilolezo Changakuti upite.”99 Ndipo iye anapita uko ndipo anakalowamwa aneneri abodzaawo, utumiki wophunzitsidwa ku sukulu, ndipo anawapangitsaiwo kunenera bodza. Uwo unali mzimu wabodza ukugwirantchito kwa chifuniro cha Mulungu. Mundirole ine…Basichinachake chimene inu mungati onani pano, miniti yokha.Penyani izi. Ine ndikufuna kuti inu mutembenuze ndi ineku l Akorinto mutu wa 5, ndime yoyamba, miniti yokha.l Akorinto…Ndipo penyani ichi ngati inu mukufuna kutimuwone chinachake, cha Mulungu akupanga chinachake—momwe kuti mizimu yoipa iyo, momwe kuti iyo ima—iyoimayendera…Chabwino, Paulo akuyankhula:

Ziri kunenedwa mwawamba kuti pali ziwerewerepakati panu, ndipo ziwerewere zotero zomwe ziri…siziri kutchulidwa pakati pa Amitundu,… (Kodi inumukuganiza chiani za izo pakati pa mpingo?)…kutiwina akumakhala ndi mkazi wa abambo ake.

Ndipo inu mukudzitukumula, ndipo mulibe…(Tiyenitiwone. Ine ndikukhulupirira ine ndinatembenuzamasamba awiri apa…)…Inu muli—Ndipo inumukudzitukumula, ndipo inu simunati makamuzilirire,izo…(Tsopano, dikirani miniti apa. Ine ndine…Eya,ndiko kulondola. Eya.)…kulira…(Ndi choncho.)…

Page 28: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

454 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

kudzitukumula, ndipo simunati…mulire, kuti uyoyemwe wachita ichi akhoze kuchotsedwa pakati panu.

100 Ndine—sindikudziwa. Ine sindikukhulupirira kutialiyense akanati anene kwa izi kapena kudulapo, koma inendikungotetezera pa chimene ine ndimakhulupirira: Ngatimunthu adzazidwapo kamodzi ndi Mzimu iye sangakhozekuwutaya Iwo. Mwaona, mukuona?

Pakuti Ine ndithudi, monga sindiripo mu thupi, komandiripo mu mzimu, ndaweruza kale, ngati kuti inendinalipo, za iye yemwe wachita izo chotere,Mu dzina la Ambuye wathu Yesu Khristu, pamene

inu musonkhana pamodzi, ndipo mzimu wanga, ndimphamvu ya Ambuye Yesu Khristu,Kuti mumupereke woteroyo kwa Satana kuti

thupi lake liwonongedwe, kuti mzimu udzakhozekupulumutsidwa mu tsiku la Ambuye Yesu.

101 Mulungu, akuwuuza Mpingo woyera, umene uli Thupi Lakekuno pa dziko lapansi, kuti (tsopano, izi ndi chitachitikaChipangano Chakale, mu Chatsopano)—akumuuza munthuyemwe anali woipa kwambiri ndi wauve pakati pa anthu kutiiye ankagona ndi mkazi wa abambo ake omwe. Anati, “Chinthuchoterocho mu Thupi la Khristu…Inu, Mpingo, mumperekeiye kwa mdierekezi ku chiwonongeko…” Mwaona? Mulunguamalola…Ndipo pamene Iye anali ndi chinachake chimeneIye amayenera kuwona kuti chachitidwa, kuti ayike chikwapupa winawake, Iye amamasulira mzimu woipa pa iwo choterokuti umuzunzemunthu ameneyo ndi—ndi kuwabweretsanso iwo.Tsopano, ife tikumupezamunthu uyu pambuyo…102 Ndi lomwe liri vuto ndi mipingo lero. Pamene munthuabwera mu Thupi la Khristu ndi kukhala mmodzi wa ziwalonayamba kuchita choipa, mmalo moti inu nonse mubwerelimodzi ndi kuchita chinthu chomwe chomwechi…Ndipo inu,Branham Tabernacle, muzichita izo. Chifukwa utali wonsewomwe inu mukumugwirizira iye, iye ali pansi pa Magazi.Ndipo iye amangopitiriza kumachita zinthu zakale zomwezomobwereza bwereza nthawi zonse. Inu muzibwera palimodzindi kumupereka iye kwa mdierekezi kuti awonongedwe thupi,kuti mzimu wake uli—monga—ukhoze kudzapulumutsidwa mutsiku la Ambuye. Ndipo muwone chikwapu cha Mulunguchikubweramo. Mumuwone mdierekezi atamugwira iye. Ndiwomzimu woyipa utamutenga iye.103 Ndipo mnyamata uyu apa anawongoledwa. Iye anabwerera.Ife tikuzipeza mu ll Akorinto pamene iye anadzitsukakwenikweni pamaso pa Mulungu.104 Tayang’anani pa Yobu, munthu wamngwiro, munthuwolungama. Ndipo Mulungu analoleza mdierekezi woipa kutiabwere pa iye, ndi kumukwapula iye, ndi china chirichonse kuti

Page 29: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 455

akaupange mzimu wake kukhala wangwiro. Mwaona? Koteromzimu woipa uli…Mulungu amagwiritsa ntchito mizimu yoipanthawi zambiri kuti achite dongosolo Lake ndi chifuniro Chake.

95. Tsopano, pano pali limodzi lomwe liri lomata kwenikweni.Funso (ine ndikuganiza ndi munthu yemweyo, chifukwaiko kukuwoneka ngati kulemba kofanana): Ngati munthuayenera kukhala nao Mzimu Woyera kuti akhale—akhalenao Mzimu Woyera kuti atembenuzidwe ndi kuti apite mumkwatulo, chidzakhala chotani chikhalidwe cha ana omweanafa asanafike zaka za kuzindikira? Ndipo ndi liti pameneiwo ati adzauke?

105 Tsopano, m’bale wanga, mlongo, ine sindingakhozekukuuzani inu zimenezo. Palibe Lemba pa izo mu Baibulolomwe ine ndingakhoze kulipeza paliponse. Koma ine ndikhozakufotokoza maganizo anga. Tsopano, izi zikulimbikitsaniinu amene mumakhulupirira mu chisomo cha Mulungu. Inumukuona, munthuyu akufuna kuti adziwe (lomwe liri funsolabwino kwambiri. Mwaona?)—munthuyu akufuna kuti adziwechiukitsiro chiti—nchiani chiti chidzachitike kwa mwana, kutingati zimatengera kuti ukhale nao Mzimu Woyera polingakuti udzapite mu mkwatulo…Monga ine ndanenera, ndikokulondola. Ndizo zolingana ndi Baibulo. Ndiko kuphunzitsakwa Lemba. Osati kuti—osati kuti upite Kumwamba…Chifukwa anthu odzazidwa ndi Mzimu Woyera ndi a chiukitsirochoyamba, Osankhidwa. Ndi otsalira a iwo…Akufa onsesadzakhalanso moyo kwa zaka chikwi. Zitatha Zakachikwi,kenako chiukitsiro chachiwiri, chiweruzo cha ku MpandoWoyera. Mwaona? Ndilo ndendende dongosolo la Baibulo. Komamunthu uyu akufuna kuti adziwe kuti nanga bwanji ana awa.Iwo…Mwa kuyankhula kwina, kodi iwo anali nao MzimuWoyera iwo asanabadwe? Kodi iwo anaulandira Iwo? Tsopano,izo ine sindingakhoze kukuuzani inu.106 Koma tsopano, tiyeni ife tinene monga chonchi: Ifetikudziwa kuti ana amene amafa, mosasamala za makoloawo, iwo ali opulumutsidwa. Tsopano, ine sindigwirizana nayosukulu ya aneneri pa izo. Iwo amati ngati izo zinali—anafaali ndi kholo lomwe linali lochimwa, kuti mwana ameneyoakanati apite ku gehena, kukavundako; sipakanadzakhalansokanthu kwa iye. Chabwino, Yesu…Yohane anati pameneYesu anadza, “Taonani Mwanawankhosa wa Mulungu ameneachotsa tchimo la mdziko.” Ndipo ngati mwana uyo analimunthu wokhalapo, yemwe akanati adzabwere pansi paziweruzo za Mulungu, ndipo Yesu anafa kuti achotse tchimo,tchimo lonse linachotsedwa pamaso pa Mulungu pamene Yesuanafera cholinga chimenecho. Machimo anu anakhululukidwa.Machimo anga anakhululukidwa. Ndipo njira yokha yomweiwe ungakhoze kukhululukidwa konse ndiyo pa kulandirachikhululukiro Chake. Tsopano, mwana sangakhoze kulandira

Page 30: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

456 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

chikhululukiro chake, chotero iye sanachite kalikonse. Iyesanachite nkomwe kalikonse. Chotero iye ali mwamtheradiwaufulu kuti apite Kumwamba.107 Koma inu mukuti, “Kodi iwowo adzapita mu mkwatulo?”Tsopano—tsopano, awa ndi mawu anga anga; ili ndi lingalirolanga tsopano. Musati…Ine sindingakhoze kutsimikizira izindi Baibulo. Koma yang’anani. Ngati Mulungu, asanaikidwemaziko a dziko, anamdziwa munthu wokhalapo aliyenseyemwe akanati adzakhale konse pa dziko lapansi…Kodi inumukukhulupirira izo? Iye anamdziwa tongole aliyense, utitiriuliwonse, ntchentche iliyonse, Iye anadziwa chirichonse chimenechikanati chidzakhalepo konse pa dziko lapansi. Ngati Iyeanazidziwa izo…108 Penyani. Tiyeni titenge mwa chitsanzo, Mose. PameneMose anabadwa, iye anali mneneri. Asanakhalepo Yeremia…Mulungu anamuuza Yeremia, “Iwe usanaumbidwe nkomwemu mimba ya amayi ako, iwe usanaumbidwe nkomwe mumimba yao, Ine ndinakudziwa iwe, ndipo ndinakuyeretsa iwe,ndipo ndinakudzozeratu iwe mneneri kwa mafuko.” YohaneM’batizi, zaka 712 iye asanabadwe, Yesaya anamuwona iyemu masomphenya, anati, “Iye ali liwu la wina wofuula muchipululu.”109 Kukonzeratu kapena kudziwiratu kwaMulungu kumadziwazonse za tiana tating’ono (mwaona?), zomwe iwo anali wotiadzachite. Ndipo Iye anadziwa kuti iwo akanati adzafe. Iyeanadziwa. Palibe kangakhoze kuchitika popanda Mulungukudziwa za iko. Palibe kanthu kangakhoze kuchitika…Chimodzimodzi monga M’busa Wabwino, momwe Iyeamaloweramo…Tsopano, kuti titenge izi mwa Lemba, inesindikanati Lemba limati zakuti-n-zakuti. Ine ndikungozitengaizo kuchokera ku malingaliro anga.96. Tsopano, funso lotsatira ndi lomwe ine ndikuganiza kuti

mwinamwake wina anali—chimene ine ndinanena usikuwina. Tafotokozani za mkazi kuti apulumutsidwe pa kubalaana.

110 Mkazi samapulumutsidwa pa kubala ana. Koma tiyenititembenuze tsopano ku l Timoteo 2:8 miniti yokha. Ndipotiyeni tingofufuza chomwe Baibulo limanena zokhudzamwana. Tsopano, ine ndikuzindikira icho ndi chiphunzitsocha Chikatolika, kuti Akatolika amati mkazi amapulumutsidwapa kubala kwa ana, pa kubala ana. Koma tiyeni tisati…Inesindimakhulupirira zimenezo. l Timoteo mutu wa 2, ndipotiyeni tiyambire pa ndime ya 8, ndi kuwerenga kamphindi kokhatsopano. Chabwino, mvetserani.

Mu kachitidwe kofanana aponso, kuti akazi anuazidzikometsera okha ndi zovala zaulemu…(Ifesitikusowa kufunsa zimenezo, si choncho ife?)

Page 31: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 457

Tamvetserani kwa izi.)…ndi nkhope yamanyazi…(Fyuuu!)…ndi kudekha; osati ndi kumanga tsitsilake ndi, kapena golide, kapena ngale, kapena zovalazodula; (Abale, ine ndikukuthandizani inu apa, inendikuyembekeza. Zibenenga zonse zatsopano izi tsikulirilonse kapena pa masiku atatu. Inu mukuona? Izo simonga amakhalira Akhristu.)Koma (zomwe ziri zoyenera akazi odzinenera

umulungu) ali ndi zintchito zabwino.Mulole akazi anu aziphunzira mwachete ndi kumvera

konse.Koma ine sindimalola kuti mkazi aziphunzitsa,

kapena kutenga ulamuliro pa…mwamuna, koma kutiazikhala…chete.Pakuti Adamu anapangidwa poyamba, ndipo kenako

Eva.…Adamu sananyengedwe, koma mkaziyo pokhala

atanyengedwa anali mu cholakwira.Popanda choletsa iye adzapulumutsidwa pa kubala

ana, ngati…(Tsopano, Iye sali kuyankhula kwa mkaziwa mdziko, pokhala ndi ana.)…ngati iye apitiriramu chikhulupiriro…(Mukuona? Ngati iye apitirira. Iyeali kale…Uyo ndi mkazi yemwe iye akumukamba,mkazi yemwe ali wopulumutsidwa kale. Mukuona?)…ndi chikondi ndi chiyero ndi kudekha konse.

111 Osati pa kukhala ndi ana zikumupanga iye kukhalawopulumutsidwa, koma chifukwa kuti iye akulera ana,akuchita ntchito yake, osati kulera amphaka, agalu, ndizina zoonjezera kuti zitenge malo a mwana, momwe iwoakuchitira lero, kuzipatsa izo chikondi cha mayi kuti iyeazikhoza kumapita ndi kumakathamanga paliponse usikuwonse. Anthu ena amachita zimenezo. Pepani, koma iwoamachita izo. Izo ndi zamwano kwambiri kuti ine ndizinene,koma choonadi ndi choonadi.Mwaona? Iwo samamufunamwanakuti azimangiriridwa pansi naye. Koma pa kubala ana, ngati iyeakupitirira mu chikhulupiriro, chiyero, ndi kudekha konse, iyeadzapulumutsidwa. Koma ngati uyo ali, iwe udzapulumutsidwanawenso, bola uli wobadwa mwatsopano. Iwe udza—iweukhoza kuchiritsidwa ngati iweyo ukukhulupirira. Iwe ukhozakulandira Mzimu Woyera ngati iweyo ukukhulupirira Iwo,kukonzekera Iwo, ngati inu mwaukonzekera Iwo. Ndipo iyeadzapulumutsidwa ngati iye apitiriza kumachita zinthu izi(mwaona?), koma osati chifukwa iye ndi mkazi. Chotero ukondi kulondola, m’bale, mlongo. Si chiphunzitso cha Chikatolikakonse. Tsopano, ine ndikufuna…Pano pali lina lomwe lirilomata kwambiri. Ndiye ife tiri nalo linanso. Ine ndikuganizamwina ife tiri nayo nthawi kwa ilo. Ine ndinangotenga nthawi

Page 32: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

458 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

yathu. Tsopano, izi zangokhala—izi zangokhala zotsatira zachitsitsimutso. Izi ndi zotsatira zamsonkhano,mafunso awa.97. Tsopano: M’bale Branham (ndi lotaipidwa), kodi ndi Lemba

kuti munthu aziyankhula mu malirime ndi kutanthauzirauthenga wake womwe? Ngati ziri choncho, chondetafotokozani l Akorinto—kapena Akorinto 14:19 ndiponsoAkorinto 14:27.

112 Chabwino, tiyeni tipite ku Lemba limenelo ndi kuonachomwe ilo likunena. Ndiyeno ife tiwona ngati ife tikuzisungaizi Mwamalemba. Ife tikufuna kuti nthawizonse tizikhalaMwamalemba. Ndi Akorinto 14. Tsopano, munthuyu akufunakuti adziwe ngati ziri Mwamalemba kuti munthu azitanthauzirauthenga wake womwe umene iye anauyankhula mu malirime.“Ngati ziri choncho, tafotokozani Akorinto 14:19.” Tiyeni tione,14 ndi 19. Chabwino, ife tiri apa.

Komabe mu mipingo ine…kulibwino ndiyankhulemawu asanu ndi kumvetsa kwanga, kuti ndi liwulanga ndikhoze kuphunzitsa ena akenso, kuposa zikwikhumi…mu… malirime osadziwika.Tsopano, yotsatira ina ndi ndime ya 27, iwo akufuna kuti

ayidziwe.Ngati munthu aliyense ayankhula mu lirime

losadziwika, mulole izo zikhale ndi awiri, kapenamwa…ochulukitsa mwa atatu, ndipo awomotsatizana; ndi kumulola wina atanthauzire.

113 Tsopano, ine ndikutenga zomwe munthuyu akuyeserakuti afikepo (chimene ine ndikufuna—ine ndikuti ndiwerengechinachake kwa inu kwamphindi yokha). Koma ine ndikuganizachimene m’bale kapena mlongo akuyesera kuti afikepo, “Kodindi choyenera kuti munthu yemwe akuyankhula mu malirimekutinso atanthauzire uthenga umene iye waunena?” Tsopano,mzanga wofunika wokondedwa, ngati inu mutangowerengandime ya 13mumutuwomwewo, iwo ukuuzani inu:

Chomwecho mulole iye amene ayankhula mulirime losadziwika apemphere kuti iyeyo akhozekutanthauzira.

114 Zedi. Iye akhoza kutanthauzira uthenga wake womwe.Tsopano, ngati ife titangoti…Tiyeni tingo…Chabwino,inu…Werengani zonse izo apa, ndipo inu mukhoza kuwonaZiri…Ingowerengani mutu wonsewo. Ndi zabwino kwambiri,kufotokoza izo.115 Tsopano, kuyankhula mu malirime…Tsopano, pamene ifetikadali pa izo, ndipo izi pokhala zikujambulidwa, ine ndikufunakunena kuti ine ndimakhulupirira mochuluka basi kuyankhulamu malirime monga ine ndimakhulupirira mu machiritsoAuzimu, ndi—ubatizo waMzimuWoyera, kudza kwachiwiri kwa

Page 33: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 459

Khristu, ndi mphamvu ya dziko likudzalo; ine ndimakhulupiriramochuluka basi mu izo momwe ine ndimakhulupirira, koma inendimakhulupirira kuyankhula mu malirime kuli ndi malo akebasi monga kudza kwa Khristu kuli ndi malo ake; machiritsoAuzimu ali ndimalo ake; chirichonse chiri ndimalo ake.116 Tsopano, kwa inu anthu, ine ndiri nawo mwayi woti ndineneizi tsopano, ndipo ine ndikanafuna kuti ndizifotokoze izi.Ndipo ngati ine ndimupweteka aliyense, ine sindikutanthauzakutero. Ine sindikutanthauza kuti ndiyambitse chisokonezo.Koma mvetserani. Chakhala chovuta ndi chiani ndi kuyankhulamu malirime osadziwika ndi anthu Achipentekoste (amene ndiriinemwini; Ine ndine Wachipentekoste. Mwaona?)…Tsopano,lomwe lakhala vuto ndi ili: kuti—iwo samazilemekeza izo. Ndipochinthu china, iwo amangozilola izo zizipita mwachisawawa.Iwo samabwerera ku Mawu.117 Tsopano mvetserani. Njira yake ndi iyi—mulole—umu ndimomwe mpingo wakhazikitsidwira. Tsopano, mu mpingo waChipentekoste, ngati ine ndikanamachita ubusa mpingo uno,ine ndikanakuuzani inu momwe ndikanati ndiukhazikitsireiwo (mwaona?), ngati ine ndikanakhala—ndikanati ndikhalepano nthawi yonse kuti ndizichita ubusa pa iwo. Inendikanamathandizira ku mphatso iliyonse ya mu Baibulo.Kuwauza okhulupirira choyamba kuti azibatizidwa mu MzimuWoyera. Ndiyeno, mphatso iliyonse ya l Akorinto 12 ikanatiizigwira ntchito mu mpingo wanga, ngati ine ndikanakhalanawo iwommenemo, thupi lonse likugwira ntchito.118 Tsopano, ngati inu mutazindikira…Osati kupangandemanga tsopano. Ndipo kumbukirani, ine sindikanati ndinenemawu amodzi mosiyana—ine ndikanati ndichitire mwanoMzimu Woyera. Ndipo Mulungu akudziwa ine sindikananenaizo molakwitsa. Mwaona? Koma ine ndikungonena izi kutindiyese kukupatsani inu momwe Lemba likuwonekera inenditaziphunzira izo tsopano kwa pafupi zaka twente. Inendakhala ndikulalikira kwa pafupi zaka sate. Ndipo inendadutsa kumene mu chirichonse, kumangokoka basi podutsa;inu mukhoza kulingalira momwe izo zakhalira ziri. Ndipomuyang’ana munthu aliyense, ndi chiphunzitso chake, kudziko lonse. Ndi kumazitenga izo chifukwa ndi chondisangalatsachanga. Ndi chosangalatsa kwa anthu okhalapo pambalipa inemwini. Ine ndiyenera kuchokako kuno. Inu muyenerakuchokako kuno. Ndipo ngati ine ndipita ngati mneneriwabodza, ine ndidzataya moyo wanga womwe ndi kutaya wanulimodzi nane. Chotero ndi zoposa—ndi zoposamkatewa pa tsiku;ndi zoposa kutchuka; ndi zoposa china chirichonse; ndi moyokwa ine. Mwaona? Ndipo ine ndikufuna nthawizonse kukhalamwa kuya kwambiri kwa kudzipereka.119 Tsopano, inu mukapita mu mpingo wa Chipentekoste,chinthu choyamba…(ine sindikutanthauza onse a iwo. Ena

Page 34: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

460 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

a iwo ali…) Nthawi zochuluka iwe ukalowa mu tchalitchindi kuyamba kulalikira; pamene iwe ukulalikira, wina amaukandi kuyankhula mu malirime. Tsopano, munthu wokondeka uyoakhoza kukhala ali mwangwiro wodzazidwa ndi MzimuWoyera,ndipo uwo ukhoza kukhala uli Mzimu Woyera ukuyankhulakupyolera mwa munthu ameneyo, koma chinthu chake ndichoti, iwo ali osaphunzitsidwa. Ngati utumiki uwu pa nsanja ulikuyankhula pansi pa kudzoza, mzimu wa aneneri umamumveramneneri. Mwaona? “Mulole zinthu zonse zizichitidwa…”Tsopano, fikani umu mwa Paulo chifukwa chimene iyeakunenera kuti “pamene wina ayankhula,” ndi zina zotero…“pamene iye anabwera, izo zinangokhala chisokonezo.”120 Tsopano, ine ndakhala ndikupanga kuitanira paguwa, ndipowina amaima ndipo amayankhula mu malirime. Izo basi…Chabwino, iwe kuli bwino ungosiya kupanga kuitanira pa guwa.Izo zimaletsa iko. Mwaona?121 Ndiyeno, chinthu china. Nthawi zambiri anthu amaukandipo amayankhula mu malirime, ndipo anthu amakhalandi kumatafula chingamu, akuyang’ana uku ndi uko. NgatiMulungu ali kuyankhula, khala bata, zimvetsera! Ngati ichochiri Choonadi, ngati umenewo uli Mzimu Woyera ukuyankhulamwa munthu ameneyo, iwe ukhale chete ndi kumamvetsera,khala molemekeza. Kutanthauzirako kukhoza kubwera kwaiwe. Mwaona? Khala bata; zimvetsera kutanthauzira kwake.Tsopano, ngati palibe wotanthauzira mu mpingo, ndiye iwoamayenera kuti azikhala bata mu Thupilo.122 Ndiyeno, pamene iwo ayankhula ndi lirime losadziwika,Baibulo linati, mulole iwo akayankhule kwa okha kwa iwondi Mulungu. Iye amene amayankhula mu malirime osadziwikaamadzilimbikitsa yekha. Tsopano, amenewo ndi malirimeosadziwika; ziyankhulo, zinenero ndipo zosiyana. “Izo sizirikanthu,” iye akutero…Koma chimene chimapanga phokosochiri ndi tanthauzo. Koma inu…Ngati lipenga liwomba, iweumayenera kudziwa momwe ilo likulirira (…kungoliwombailo) kapena iwe sungadziwemomwe ungadzikonzekerewekha kunkhondo. Ngati aliyense ayankhula mu malirime, ndi kungoti“tutu”; ndi zonse zomwe ziripo kwa ilo, ndani ati adziwechoti achite. Koma ngati ilo liyamba tetelite, izo zikutanthauza“ukani!” Ngati ilo liwomba mogunda, izo zikutanthauza“khalani pansi.” Mukuona? Ngati ilo liwomba mwaukali izozikutanthauza “pitani mwamphamvu.” Ilo liyenera kuperekatanthauzo, ndipo osati kungoyankhula kokha. Chotero mumpingo, ngati mulibe wotanthauzira, koma momwe muliwotanthauzira, ndiyemalirime ndi omwe ali amumpingo.123 Tsopano, ku funso lanu, mzanga wokondeka, lomwe likuti,“Ine kulibwino ndiziyankhula zikwi zisanu…mawu asanu mu,ndi chotero kuti anthu azikhoza kumandimvetsa ine kuposazikwi zisanu (kapena ena aliwonse ochuluka amene akuwanena)

Page 35: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 461

mu lirime losadziwika.” Izo nzoona. Koma werengani mpakapansi: “…kupatula ngati izo zikhala mwa vumbulutsokapena mwa kutanthauzira kuti zilimbikitse.” Mwaona? Kutiumangirize.124 Tsopano, ine ndingokhala ngati ndikupatseni inu kalingalirokakang’ono bwanji ngati—chiani…Ngati ine ndinali wotindichitire ubusa mpingo uno umene ukudzapo, ngati Mulunguakanandiyitana ine kuti ndichite ubusa pa iwo, umu ndimomwe ine ndikanauyendetsera iwo: ine ndikanayeserakuti ndimupeze munthu aliyense mmenemo yemwe ali nayomphatso. Ndipo ine ndikanati anthu amenewo kuti azikomanapafupi ora misonkhano isanayambe konse, mu chipindakwa okha. Kumawalola iwo kuti akhale pansi pa Mzimu.Ndipo chinthu choyamba inu mukudziwa, wina abwera apoyemwe ali nayo mphatso yoyankhula mu malirime. Ndipo iyeayankhula mu malirime. Aliyense atakhala chete. Ndiyeno winaaimirirapo ndi kutanthauzira zomwe iye wanena. Tsopano,izo zisanaperekedwe kwa mpingo, Baibulo limati izo ziyenerakuti ziweruzidwe pakati pa mboni ziwiri kapena zitatu.Tsopano awo ndi amuna omwe ali nako kuzindikira kwaMzimu (mwaona?), chifukwa nthawi zambiri mphamvu zoipazimalowa mmenemo. Paulo anayankhula za izo. Komano,mphamvu ya Mulungu ili mmenemonso. Ndiuzeni ine gulummene choipa sichimakhalamo. Ndiuzeni ine pamene ana aMulungu amasonkhana palimodzi kumene Satana samakhalapakati pa iwo. Ndi chirichonse. Chotero musamachitire tsinyapa izo. Mukuona? Satana ali paliponse. Tsopano, ndi ife pano.Wina akuyankhula mu malirime. Tsopano, alipo atatu ameneali apo omwe ali nao Mzimu wa kuzindikira. Ndipo winaanayankhula mu malirime napereka uthengawo. Tsopano, izosizingakhoze kukhala kubwereza Lemba, chifukwa Mulungusamagwiritsa ntchito kubwereza kwachabe, ndipo Iye anatiuzaife kuti tisamatero. Mwaona? Chotero si zimenezo. Ndi uthengawa kwa mpingo.125 Ife takhalapo nazo zinthu ziwiri mu chitsitsimutsoichi mpaka pano. Penyani chomwe chirichonse chaizo chinali—mwangwiro, mpaka pa dontho. Mwaona?Zinasunthira mkati. Mwamuna mmodzi anaimirira, ndipoanayankhula mu malirime, ndipo anapereka kutanthauzira,ndipo anatembenukira mmbuyo chozungulira, ndipoanadzautsimikizira uthenga umenewo umene unangopitapowo.Mmodzi wina anauka usiku wina, ndipo ananena mu—pansipa kudzoza kwa ulosi, ndipo ananena chinachake, asakudziwachimene iye anali akunena; ndiyeno pa mapeto iye anayankhulakuti, “Wodala ali iye yemwe adza mu Dzina la Ambuye.”Mwamsanga chinachake chinandigwira ine mofulumirakumene ndipo ndinati, “Mwinamwake wodala ali iye yemweakukhulupirira kuti awa ndi Ambuye amene abwera.”

Page 36: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

462 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

126 Mwaona kuma—ndiye Mzimu Woyera unagwa mu chipindausikuwatha.Mwaona? Izo ndi zolimbikitsa. Ine ndinali nditaimaapo ndikuyesera kuwauza anthu kuti iwo ayenera kulandiraMzimu Woyera. Ndipo mdierekezi anali atabweramo panalianthupo, kumati, “Musati mumvetsere; khalani duu.”

Mlongo wanga anati, “Bill, ine ndinali wokondwa kwambiripamene iwe unali kulalikira; ndinamverera ngati ine ndiimirirendi kulumpha kudutsa khoma.”

Ine ndinati, “Dzuka ndipo zilumpha.” Ndizo basi.Ndipo iye anati, “Koma pamene iwe unayamba kuchita

izo,” ndipo anati, “anthu anayamba kufuula,” nati, “ndiyeine ndinangomverera ngati kuti ine ndinali chakale chopandantchito.”127 Ine ndinati, “Ameneyo ndi mdierekezi. Ameneyo ndi Satana.Pamene iye anabwera umo kudzachita izo,” ine ndinati, “iweukanati ungoima basibe.” Ife ndife ansembe kwa Mulungu,tikupanga nsembe zauzimu—kupereka nsembe, zipatso zamilomo yathu poperekamatamando kwaDzinaLake.Mwaona?128 Tsopano, tsopano, izi ndi zomwe zinachitika. Ndiye MzimuWoyera unafalikira, chifukwa uko kunangokhala… “Wodalaali iye amene akhulupirira.” Mausiku awiri, atatu molunjikaine ndinayesera kuyala izo mmenemo; ndiyeno, Mzimu Woyeraunayankhula ndipo unati (pansi pa kudzoza)—unati, “Wodala aliiye amene adza mu Dzina la Ambuye.” Ndipo ine ndisananenechirichonse, ine ndinali nditazinena kale mobwereza. “Wodalaali iye amene akukhulupirira kuti Ambuye abwera muno.” Inumukuona? Ndipo ine ndangokhala ndikuyankhula izi, MzimuWoyera ndiMulunguMwiniwakemkati mwanu.Mwaona?Ndipoiwo anazigwira izo. Mwaona? Ndiyeno MzimuWoyera unagwerapakati pa anthu. Mukuona momwe Iwo—Iwo umalimbikitsira,ulosi?129 Tsopano, pali kusiyana pakati pa ulosi ndi mneneri. Ulosiumapita kuchokera kwa mmodzi kupita kwa wina, komamneneri amabadwa kuchokera mchikuta ali mneneri. Iwoamakhala ndi PAKUTI ATERO AMBUYE! Palibe kuwaweruzaiwo. Inu simukuwawona iwo pamaso pa Yesaya, kapenaYeremiya, aliyense wa aneneri awo, chifukwa iwo anali ndiPAKUTI ATERO AMBUYE! Koma mzimu wa ulosi pakati paanthu; iwe umayenera kuti uwupenyesetse iwo, chifukwa Satanaakhoza kuzembera mmenemo. Mwaona? Tsopano. Koma izoziyenera kumaweruzidwa.130 Tsopano, ndife—ife tikuti tikhale ndi chitsitsimutso.Tsopano, penyani izi mwatcheru kwambiri kwenikweni tsopano,inu atumiki. Ife tikukonzekera chitsitsimutso. Chabwino.Kapena mwina ife tangokhala ndi msonkhano wachizoloweziwa mpingo. Mpingo wayaka moto. Iwo umayenera uzikhala ulinthawizonse. Chabwino, mwinamwake ife tiri nawo anthu faifi

Page 37: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 463

kapena sikisi omwe ali anthu amphatso; mmodzi amayankhulandi malirime, awiri kapena mwina atatu amayankhula ndimalirime, anai kapena asanu ndi malirime, ali ndi mphatsoya malirime, amayankhula mu malirime osadziwika. Awirikapena atatu a iwo amakhoza kutanthauzira. Mwina alipommodzi—awiri, kapena atatu a iwo omwe ali nayo mphatsoya nzeru. Chabwino. Iwo onse amakomana, anthu amphatsoamenewo…Inu…Mphatso zimenezo zaperekedwa kwa inuosati kuti muzisewera nazo, osati kuti muziti, “Ulemerero kwaMulungu, ine ndimayankhula mu malirime! Aleluya!” Muli—muli—muli kudzitsitsa nokha. Izo zinaperekedwa kwa inu kutimuzigwira nazo ntchito. Ndipo gawo lanu mu mpingo lizibweramsonkhano waukulu usanayambe, chifukwa osaphunzitsidwaazikhala ali pakati pathu.131 Ndiye inu muzipita mu chipinda, ndipo inu muzikakhalammenemo, anthu inu palimodzi, chifukwa ndinu ogwira-ntchito limodzi mu Uthenga. Ndiye inu muzikhala mmenemo.“Ambuye, kodi chiripo chirichonse chimene Inu mukufunakuti ife tichidziwe usikuuno? Yankhulani kwa ife, o, Atateakumwamba,” mukupereka pemphero, mapembedzero; kuimbanyimbo. Molunjika pansi uzibwera Mzimu, nugwera pawinawake, nayankhula mu malirime. Wina naimirirapo nati,“PAKUTI ATERO AMBUYE.” Ndi chiani icho? Mvetserani.“Pitani mukamuuzeM’bale Jones kuti asamuke kumalo kumeneiye akukhalako, pakuti mawa madzulo kudzakhala mkuntho utiudzasese ku dziko limenelo; ndipo iwo udzaitenga nyumba yake.Atenge katundu wake ndipo achokeko!”132 Tsopano, izo—izo zikumveka bwino. Koma dikirani miniti.Payenera kukhala pali amuna atatu pamenepo omwe ali ndiMzimu wa kuzindikira. Mmodzi wa iwo akati, “Izo zinaliza Ambuye.” Mmodzi wina nkuti, “Izo zinali za Ambuye.”Awo ndi awiri motsutsana ndi atatu—mboni ziwiri kapenazitatu. Chabwino. Iwo azilembe izo pa chidutswa cha pepala.Ndizo zimene Mzimu wanena. Chabwino. Iwo abwerere pakupemphera, nkumamuthokoza Ambuye.133 Pakapita kanthawi, “PAKUTI ATERO AMBUYE (mlosiaimirira)—PAKUTI ATERO AMBUYE, usikuuno, kuchokera kuMzinda waku New York akhala ali mkazi; iye ali pa machila;iye abwera mu nyumbayi ali pa machila. Iye wamanga mpangowobiliwira kuzungulira mutu wake. Iye akufa ndi khansara.Chimene chinamupangitsa iye kuti akhale motere, Ambuyeakumutsutsa iye—nthawi ina iye anaba ndalama kuchokera kuMpingo Wake pamene iye anali wa usinkhu wa zaka sikisitini.Kamuuzeni M’bale Branham kuti amuuze iye zinthu zimenezi.PAKUTI ATERO AMBUYE, ngati iye akazikonza izo, iyeachiritsidwa.” Dikirani miniti. Izo zikumveka bwino kwambiri,koma dikirani miniti. Inu mulemba dzina lanu pa pepala ili,wozindikira? Kodi inu mulemba dzina lanu?

Page 38: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

464 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

134 “Izo zinali za Ambuye.” Wina nati, “Izo zinali za Ambuye.”Ndiye—ndiye inu muzilembe zimenezo, “PAKUTI ATEROAMBUYE, usikuuno pakhala mkazi yemwe ati abweremuno, chinthu chakuti, chakuti.” Iye amene ali ndi mzimuwakuzindikira, awiri kapena atatu a iwo alembepo dzina lawokwa izo. Mauthenga onse awa aperekedwa. Chabwino.135 Ndiye pakapita kanthawi iwo ayamba kumva belu likulira.Mpingo wayamba kusonkhana. Ndiye iwo abweretsa mauthengaawa, kuwaika iwo pomwepa pa desiki. Pano pomwe ndipamene izo zimayenera kuti zizikhala zitaikidwa. Ine ndirikwinakwake ndikuwerenga, kupemphera. Pakapita kanthawiine ndizitulukako nyimbo zitatha kuimbidwa. Mpingo wonse ulimu dongosolo, anthu akubwera, akukhala, akusinkhasinkha,akupemphera; ndicho chimene inu mukuyenera kuti muzichita.Osati kubwera ku tchalitchi ndi kumayankhulana wina ndimzake, muzibwera ku tchalitchi kuti mudzayankhulane ndiMulungu. Muzikakhala ndi chiyanjano chanu kunja uko.Mwaona? Ife tikuchita chiyanjano ndi Mulungu tsopano.Ndipo ife timabwera kuno kumayankhula, chirichonsemwakachetechete, molemekeza, Mzimu ukuyendayenda. Walimba kubwera ku limba pafupi maminiti faifi utumiki wanyimbo usanayambe, kuyambamokoma kwenikweni:

Pa mtanda Mpulumutsi anafa,Ponditsuka tchimo ndinalira,…

Kapena nyimbo ina yabwino yokoma, mwakachetechetekwenikweni. Izo zimabweretsa Kukhalapo kwa Mzimu Woyeramumsonkhano. Mwaona? Chabwino.136 Anthu atakhala mmenemo. Ena a iwo ali kwenikweni—akuyamba kulira ndi kumabwera ku guwa, nkumalapamsonkhano usanayambe nkomwe. MzimuWoyera uli pamenepo.Mwaona? Mpingo uli mu kusautsika. Akhristu akupemphera;iwo ali pa malo awo. Iwo sikuti angokhala apo akutafunachingamu, kumati, “Hei, Liddie, tandipatsa ine zopakammilomo zakozo; ine ndikufuna…Iwe ukudziwa. Iweukudziwa. Ine ndikusowa…Iwe ukudziwa, tsiku lina pameneine ndinali kumusi uko ndikugula, ine ndikukuuza iwe,ine ndinali pafupi kuti ndikuponde pa zala zako. Kodi inendinayamba ndaziwonapo zoterozo…Kodi iwe ukuganizachiani za izo?” O, chifundo! Ndiye nkuitcha iyo nyumba yaMulungu. Bwanji, ndi zopanda ulemu. Thupi laKhristu kubwerapalimodzi. Apo ife tinakhala.

Bambo atakhala chapafupi, “Ndikuti, inu mukudziwapamene ife tinapita uko, izi zakuti-n-zakuti ndi zakuti-n-zakuti-n-zakuti…” Izo ndi zabwino muli kunja, koma mkati muno ndimnyumba ya Mulungu.137 Muzibwera muno mwakupemphera; muzitenga malo anu.Ine ndikukamba tsopano, osati kwa mipingo yanuyo, abale.

Page 39: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 465

Ine sindikudziwa zomwe inu mumachita; ine ndikukamba kwakachisi uyu. Ine ndikuyankhula kwa khomo langa lakuserilomwe. Mwaona? Ndiko kulondola.138 Tsopano, pamene inu mubwera muno monga choncho, ndiyechinthu choyamba inu mukudziwa, m’busa amatuluka umo.Iye ali mwatsopano. Iye samasowa kuti azidzayankha izi, izo,ndi zinazo. Iye akubwera kumene kuchokera mu—mame autumiki wake. Iye wakhala ali pansi pa mphamvu ya MzimuWoyera. Iye akudzalowa kumene komwe malirime ochuluka amoto asonkhana palimodzi. Ali pafupi lawi tsopano (mwaona?),ili likuyendayenda apo. Iye akutulukira kuno, nadzatenga izi.“Uthenga wochokera kwa mpingo: ‘PAKUTI ATERO AMBUYE,M’bale Jones asamuke ku nyumba yake. Mawa madzulo pa 2koloko mkuntho udzasesa dziko laolo. Atenge zinthu zake ndipoachokeko.’” M’bale Jones akuzimwa zimenezo. Chabwino. Izozasungidwa. “PAKUTI ATERO AMBUYE, kukhala kuli mkazidzina lake Wakuti-n-wakuti ati abwere muno usikuuno, ndipoizo zinali—iye wachita zakuti-n-zakuti.” (Momwe ine ndanenerakumene, onani, monga choncho.) Chabwino, izo ziri pamenepa.Ndi zimenezo. Iwo ali nao kale malo awo tsopano mu mpingo.Chabwino.139 Ndiye iye akuutenga uthengawo. Ndipo chinthu choyambainu mukudziwa, iye akuyamba kulalikira. Palibe kanthukosokoneza; izo zachitika kale. Tsopano, ife tikupita patsogolo,ife tikulalikira uthenga.140 Ndipo patapita kanthawi pamene…Chinthu choyambainu mukudziwa pamene uthenga watha, mzere wa machiritsoukuyamba. Apa pakubwera mkazi. Winawake anayankhula mumalirime ndipo anati iye abwera. Mwaona? Aliyense wa ifeakudziwa chimene chiti chichitike. Aliyense wa ife akuzidziwaizo. Mukuona momwe chikhulupiriro chikuyambira kumangikandi malirime a moto awo ataima pa inu tsopano. Iwo ukuyambakusonkhanira palimodzi. Bwanji, iyo ndi ntchito yotsirizidwakale; ndi zomwezo.

Mkazi ameneyo…ine nditi, “Akazi a Akuti-ndi-akuti,mwachokera kuMzindawaNewYork,mulimuno…”Mwaona?

“O, izo nzolondola. Inumunadziwa bwanji izo?”“Uwo ndi uthenga wochokera kwa Ambuye kwa mpingo.

Pamene inu munali a usinkhu wa zaka sikisitini, kodi inusimunali pa malo akuti, akuti ndipo munachita—munatengandalama zina kuchokera ku mpingo, ndipo munaziba izo, ndipomunapita kwina, ndipomunakagula zovala zatsopano ndi izo?”

“O, uko nkulondola. Uko ndi kulondola.”“Izo ndi ndendende zomwe Mulungu watiuza ife usikuuno

kupyolera mwa M’bale Wakuti-n-wakuti, anayankhula ndimalirime; M’bale Wakuti-n-wakuti anatanthauzira; M’bale

Page 40: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

466 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

Wakuti-n-wakuti kuno ananena, mwa kuzindikira, anati izozinali zochokera kwaAmbuye. Ndipo izo nzoona.”

“Inde!”

“Ndiye, PAKUTI ATERO AMBUYE, pitani mukazikonzeizo, ndipo muthana nayo khansara yanuyo.”141 M’bale Jones akupita kwawo, akukatenga ngolo, akubwererauko, akutenga mipando yake, ndi kuchokako uko. Pa 2koloko mawa madzulo [M’bale Branham akupanga phokosokuti afotokozere—Mkonzi.] chikuchokapo chinthu chonsecho.Mwaona? Ndiye mpingo ukulemekeza…“Zikomo inu, AmbuyeYesu, chifukwa cha ubwino Wanu.” Tsopano, izo ndi zomwe ziri,kumangiriza, kwa mpingo.142 Tsopano, nanga bwanji ngati izo sizichitika iwo atanenakale izo. Ndiye inu muli ndi mzimu woipa pakati panu.Inu simukuchifuna chinthu choipa icho. Iwe ungafunirenjichinachake choipa pamene—miyamba yadzaza ndi zenizeni zaChipentekoste? Musati muzitenga choloweza mmalo chakalechochokera kwa mdierekezi. Pezani chinachake chenicheni.Mulungu ali nazo izo kwa inu. Ndiye inu musati muzikhala ndimisonkhano inanso, ndi kuika chirichonse pamenepa, mpakaMulungu atatsimikizira kale kuti inu mukulondola, chifukwandinu wothandizira kwa mpingo mu ntchito ya Uthenga.Tsopano, inu mukumvetsa zomwe izo ziri?143 Ndipo malirime, malirime osadziwika…Palibe munthuiye—amadziwa chimene iye akuchikamba. Iye amayankhula;koma phokoso lirilonse liri ndi tanthauzo. Izo ziri ndi tanthauzo[M’bale Branham akuwomba manja ake—Mkonzi.] “Guluku,guluku, guluku!” izo ziri—ndi—ndi chinenero kwinakwake.144 Pamene ine ndinali mu Afrika, ine sindinali kukhulupirirakonse izo, koma chirichonse chimene chinkapanga phokosochinali ndi mtundu wina wa tanthauzo kwa icho. Baibulo linatipalibe phokoso lopanda kufunikira, lopanda tanthauzo. Phokosolirilonse limene limapangidwa limakhala ndi tanthauzo linakwa chinachake. Mwakuti, ine ndimawamva anthu akuti…inendikuti, “Yesu Khristu, Mwana waMulungu.”145 Mmodzi wa iwo amati [M’bale Branham akupanga phokosola wotanthauzira wachi Afrika—Mkonzi.]. Wina amati [M’baleBranham akufotokozeranso—Mkonzi.]. Ndipo zimenezo zinali,“Yesu Khristu, Mwana wa Mulungu.” Mwaona? Izo zinali…Ndipo izo nkusamatanthauza kanthu kwa ine, koma kwaiwo icho chinali chinenero chimodzimodzi basi monga inendikuyankhulira kwa inu. Pamene wotanthauzira wa chi Zulu,chi Xhosa, chi Basuto, ndi chirichonse, chomwe chimadzamotsatira, chirichonse chimene chinali kunenedwa, aliyenseankachimva. Ndipo zinthu izi zimene inu mumawamva anthuawa akungoyankhula, ndi kumaganiza kuti ndi zochuluka za

Page 41: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 467

kubwebweta, uko sikuli; izo ziri nalo tanthauzo. Chotero ifetiyenera kuti tizizilemekeza izo, tiziziyika izomumalo ake.146 Tsopano, mwina pakhala palibe uthenga. Tsopano,msonkhano watha; kuitanira pa guwa kuli kupangidwa. Ndipopakapita kanthawi winawake (pakhala palibe uthenga kumbuyouko)—winawake akuimirira mwamsanga pamene iwo apezamwayi wotero. Mzimu Woyera…Tsopano, Baibulo linati,“Ngati palibe wotanthauzira, msiyeni iye akhale bata.” Ziribekanthu kuti akuvutika bwanji kuyesera kuti ayankhule, khalabata.147 Ukati, “Ine sindingakhoze kuchita izo.” Baibulo linati iweukhoza. Mwaona? Chotero kuti—izo ndi zokhazikika. Mukuona?Msiyeni iye akhale bata.148 Ndiye, pamene iwo, mwayi ukabwera pamene chirichonsechiri mu dongosolo, ndiye ngati Mzimu Woyera ulumphira paiye kuti apereke uthenga, ndiye upereke iwo. Ndizo ndendendezomwe inu muyenera kumazichita. Ndiye kutanthauzirakumabwera, nkuti, “Muli mkazi mkati muno dzina lake ndiSally Jones (ine ndikuyembekeza mkazi sali muno amene ali ndidzina limenelo, koma…)—Sally Jones. (Mwaona?) Mumuuzeiye kuti uno ndi usiku wotsiriza wa kuitanidwa kwake. Akonzezinthu ndi Mulungu chifukwa iye ali ndi nthawi yaifupikuti akhale kuno.” Tsopano, Sally Jones angathamangire kuguwa mwamsanga basi monga iye angakhoze kukafikira uko(mwaona?), chifukwa uko ndi kuitanidwa kwake kotsiriza.Mukuona? Ndiko kupereka uthenga, kapena kutsimikizira,kapena chinachake.149 Uwo ndi mpingo wa Chipentekoste ukugwira ntchito.Palibe mwayi woti mizimu yoipa ilowereremo, chifukwauli kale…Baibulo likupereka mwandendende, “Mulole izozikhale motsatizana, ndipo izo mwa atatu; ndipo muzilolaawiri kapena ochulukirapo aweruze.” Umenewo ndiwompingo. Koma kodi ife tafika nazo pati izo lero? Kudumphirammwamba, kupitiriza, kuseka ndi kumapitirira pamene winaakuyankhula mu malirime; wina kumayang’ana, kumayankhulaza chinachakenso ndi kumachulukana chozungulirapo;m’busa kumachita chinachake; kapena ena kumachulukanachozungulirapo. Komatu, izo sizabwino. Mwina m’busaakulalikira, ndipo winawake nkuimirira ndi kumamusokonezaiye mu…Mwina kumawerenga Baibulo ndipo winawake…Kumawerenga Baibulo, ndipo wina kumbuyo uko akuyankhulammalirime. O, ayi! Mukuona? Mlaliki ataima akulalikiramu guwa, winawake nkuima ndi kumamusokoneza iye,poyankhula mu malirime. Izo zonse nzabwino. Ine sindikutiuwo si Mzimu Woyera, koma inu mukuyenera kuti muzidziwamomwe muziugwiritsira ntchito Mzimu Woyera (mukuona?),kuwugwiritsa ntchito Iwo.

Page 42: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

468 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

Tsopano, ine—ine ndikuyankhula…Kodi inu muli nawomalo a limodzi lina? Ndiye, mawa ndi Lamlungu. Ndiye,ife tidza…Tiyeni tingo…Pano pali limodzi. Ine ndikuganizandilo lachisomo kwambiri. Ndipo tsopano, ngati inu nonsemutangopirira nane maminiti pang’ono okha motalikitsa,chonde. Ndiyeno, ndidza…ine ndikufuna inu—ine ndikufunainu kuti muchimvetse ichi. Ine ndinalisunga ili mwacholinga. Ilindi limodzi langa lotsiriza.

Tsopano, poyamba, ine ndikuti ndiwerenge zinthu ziwirizimene munthuyo wazifunsa. Izo ziri pa chidutswa chakalecha pepala, cholembedwa ndi malembedwe okongola. Ndiribelingaliro la yemwe ali, palibe dzina lalembedwa kwa—kwalirilonse la iwo.98. M’bale Branham, kodi ndi kulondola kuti atumiki

azipanga zikoka zazitali pa ndalama mu misonkhanoyawo, kumanena kuti Mulungu wawauza iwo kuti ochulukamwakuti mwa omvetsera akuyenera kupereka mochulukachotere? Ngati uku kuli kulondola, ine ndikufuna kutindidziwe. Kapena ngati ziri zolakwika, ine ndikufuna kutindidziwe. Izi zandisokoneza ine moyipa.

150 Tsopano, inu mukuona, mzanga, ine ndikuti ndikuuzeni inu,ine ndikuti ndikuuzeni inu chimene ine ndikuganiza. Mukuona?Tsopano, izo sizikutanthauza kuti nzolondola. Ine ndikuganizandi zoipa.151 Tsopano, ine ndikuganiza izi. Mulungu ananditumiza ine kuntchitoyi. Ine ndawonapo nthawi yomwe ine ndinkawonekangati ine ndikanati ndikhale mwinabe…Ndipo ine—inendimakhala ndilibe ndalama konse. Ndipo ine ndimati,“Ingodusitsani mbale ya chopereka.”

Ndipo amanejala amakhoza kubwera ndi kuti, “Taona, Billy,tiri madola zikwi zisanu mu ngongole usikuuno, Mnyamata.Kodi iwe uli nazo ndalama ku Jeffersonville zoti ukailipire iyo?”152 Ine nkuti, “Zonse ziri bwino. Mulungu ananditumizaine kuno, kapena ine sindikanati ndibwere. (Mukuona?)Ingodusitsani mbale ya chopereka.”

Ndipo msonkhano usanathe, wina nkuti, “Inu mukudziwa,Ambuye anachiyika pa mtima wanga kuti ndipereke madolazikwi zisanu ku izi.” Onani, mwaona? Choyamba, khalaniotsogozedwa pakuchita izo.153 Ine sindimakhulupirira kukokera, ndi kupempha,ndi kupemphetsa ndalama. Ine ndikuganiza ndi chinthucholakwika. Tsopano, m’bale, ngati inu mumachita izo, musatimundilole ine ndipweteketse kumverera kwanu.Mukuona? Inu—inu mukhoza kukhala nacho chilolezo kuchokera kwa Mulunguchochitira izo. Koma ine ndikuyankhula za mwiniwanga zokha.Ine sindimakhulupirira mu zimenezo.

Page 43: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 469

154 Tsopano, ine ndadziwapo ngakhale za azitumiki amapitandi kumati…Ine ndinaima pomwepo, osati kale litali…Tsopano, awa si Achipentekoste, awa ndi…Chabwino, ndimipingo (mukuona?), mipingo ina. Izo zinali ku msonkhanowaukulu wa msasa. Gertie, iwe unali nane, ambiri ena alipo.Ndipo iwo anatenga madzulo onse ku chipembedzo chotchuka—awiri kapena atatu a iwo palimodzi (ndizo zachizolowezi—mipingo yachizolowezi, monga mipingo yathu yamakono kunomu mzinda, ndi zina zotero) ku msonkhano waukulu—ndipoiwo anatenga madzulo onse, kuima pa nsanja ndi kumawopyezakuti—kuti Mulungu akanati awononge mbewu zawo, akanatiawapatse ana awo kupuwala, ndi zinthu monga choncho,ngati iwo akanati asapereke kwa msonkhano umenewo. Ndizondendende zoona, ndiri ndi Baibulo ili patsogolo panga.Ine ndinati, “Uko ndi kuchitira mwano kwa Mulungu ndikwa omutsatira Ake.” Ngati Mulungu akutumani inu, Iyeakusamalirani inu. Ngati Iye sanakutumeni inu, ndiye mulolechipembedzo chizikusamalirani inu apono. Koma—koma inu…NgatiMulungu akutumani inu, Iye akusamalirani inu.99. Nanga bwanji za sewero la Khrisimasi mu mpingo wa

Mzimu Woyera?155 Chabwino, ngati ziri zokhudza Khristu, izo zikhozakukhala zabwino. Koma ngati ziri zokhudza Santa Claus,ine sindimakhulupirira mwa iye. I—ine ndakula kale—inendakula nkuchoka kale kwa izo. Ine sindimakhulupirira mwaSanta Claus konse. Mukuona? Ndipo tinthu tina tating’ono taKhrisimasi tomwe iwo ali nato, ine ndikuganiza ndi zopusa.Ndipo…Koma ine ndikuganiza iwo amuchotsa Khristu yensemuKhrisimasi ndi kuikamo Santa Clausmmenemo.156 Ndipo Santa Claus ndi nthano yopeka. (Inesindikupweteketsa kumverera kwanu kulikonse, inendikuyembekeza, pokhudza ana.) Koma ine ndikuuzani inu.Kuno osati kale litali, pafupi zaka twente-faifi, sate zapitazo,pamene mtumiki kuno mu mzinda uwu, m’busa wa—wa mpingowinawake waukulu mu mzindawu, yemwe ine ndinkamudziwabwinobwino, mzanga wa pachifuwa wa ine, iye anadza kwa ine.Ndipo Charlie Bohannon (M’bale Mike, inu mukumukumbukiraCharlie Bohannon, mzanga wabwino kwa ine)…Anakhalapamenepo mu ofesi yake ndipo anati, “ine sindidzawauza konseana anga kapena zidzukulu zanga kuwauza bodza limenelokenanso.” Iye anati, “Mnyamata wanga yemwe wamng’onoanadza kwa ine iye atafika kale pafupi usinkhu wa zakathwelofu, ndi kumayankhula za Santa Claus…” Ndipo iyeanati, “Bwanji…Wokondedwa, ine ndiri ndi chinachake chotindikuuzeni inu,” Anati, “Amayi…” Inu mukudziwa, ndipoanapitirira kumamuuza iye zomwe iye anazichita.

Ndiye iye atabwerera, anati, “Ndiye, Adadi, kodi Yesu uyuali chinthu chomwecho?”

Page 44: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

470 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

157 Muzinena zoona. Santa Claus ndi zobweretsedwa ndiKatolika za munthu, Kriss Kringle kapena Nicholas Woyera,woyera wa Chikatolika wa chi German wokalamba wa zakazambiri zapitazo yemwe ankapita paliponse kumachita zabwinokwa ana. Ndipo iwo achipitiriza icho ngati mwambo. Koma YesuKhristu ndi Mwana wa Mulungu. Iye ndi weniweni, ndipo Iyealimoyo.

Tsopano, apa pali funso, limodzi lotsiriza, lomwe lirikwambiri…158 Tsopano taonani. Inu mukhoza kusagwirizana nane paizo. Koma ngati inu simugwirizana nane, kumbukirani,mulole izo zikhale zachibwanawe, mutero inu? Inendimakukondani inu, ndipo ine sindikufuna kuti—sindikufunakuti ndikupweteketseni inu. Ine ndangokhala, Ine ndikufunakuti ndikhale woonamtima. Ngati ine sindingathe…ngatiine ndimuuza mnyamata wanga bodza, ndiye ndine wabodza.Mukuona? Ine ndikufuna ndizimuuza iye zoona.159 Tsopano, ine ndikamuuza iye za Santa Claus, ine nkuti,“Eya, zedi, alipo Santa Claus. Mudzawaone Adadi pa usiku waKhrisimasi.” Mukuona? Eya.160 Inu mukudziwa, tsiku lina ine ndinali kumusi uko, ndipoine ndinayesera izo pa msungwana wamng’ono kuti ndingoona.Ine ndithudi ndinalipidwa mobwezeredwa dzana ilo. Ine ndinalimu nyumba. Ndipo iwo anali ataima apo, kumusi kuno kuQuaker Maid. Ndipo ine ndinapita uko kuti ndikagule zinthu.Ndipo chotero ife, mkazanga ndi ine, tinali mmenemo. Ndipouko kunali msungwana wamng’ono kwambiri, sanali wopitirirapafupi usinkhu wamiyezi eyitini, ndipo iye ataima apo, akupita,akuimba, “Dingle Bells, Dingle Bells…” Ndipo ine ndinati…Mu maimidwe ake aang’ono, inu mukudziwa, atakhala mmbuyomwa ngolo yaing’ono.

Ine ndinati, “Kodi iwe ukuyembekezera Santa Claus?”

Iye anati, “Ameneyo ndi adadi anga, Bambo.”

Ine ndinati, “Adalitsemtimawakowaung’ono,Wokondedwa.Iwe uli ndi nzeru.”

Tsopano, pano pali kokanirira kenikeni, abwenzi. Ndipomwa ichi…Ndiye ine nditseka. O, ndi—ndi Lemba lokoma,koma ndi lobaya kwa munthu aliyense yemwe wowoneka ngatiali. Ndipo ilo landikanirira ine kwa zaka ndi zaka; ndipo kokhamwa chisomo cha Mulungu chokha…Ndipo mkazi wangawofunika, wakhala kumbuyo komwe uko tsopano, pamene iyeanamva kuti ine ndinali nalo funso limenelo madzulo ano,iye anati, “Bill, iwe ukaliyankha chotani ilo?” Iye anati, “Inenthawizonse ndakhala ndikulidabwa ilo mwiniwanga.” Anati,“Ine sindimakhoza kulimvetsa ilo konse.”Ndipo anati…

Page 45: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 471

Ine ndinati, “Ubwere uko usikuuno, Wamtimawokoma.Ine ndikachita mwakukhoza kwanga pakuthandizidwa ndiMulungu.”

100. M’bale Branham, chonde tafotokozani Ahebri 6:4 mpaka 6.161 Iyo ndi nthawi imodzi yomwe kwenikweni…Mwaona,tsopano inu musowa kuti muyang’ane kuno pa chikhulupirirochathu, chisomo, chitetezero cha okhulupirira, kupirira kwaoyera, chipiriro, kani, cha oyera. Ahebrimutuwa 6, 4mpaka 6.

Tsopano, mwamsanga pamene izi…tikatsiriza izi, ndiye inendikuyembekeza kuti Mulungu andithandiza ine kuzipangitsaizo kumveka bwino bwino kwa inu. Ine ndikupepesa, i—ine ndirindi Uthenga wanga wa usikuuno; mwina ine ndilalikira chinthuchomwecho mmawawu pa—pa utumiki. Ndiye ine ndikhalandikupita.162 Tsopano, ili ndi lokanirira kwenikweni. Mukuona?Tsopano, inu muyenera kusamalitsa. Tsopano kumbukirani,ife timakhulupirira ndi kuphunzitsa pa mpingo uno, kuti sichirichonse chimabwera kuno ndi kumafuula, chirichonsechimene chimayankhula mu malirime, chirichonse chimenechimagwirana chanza ndi mlaliki, chiri nawo Moyo Wamuyaya.Koma ife timakhulupirira ngati iwe uli nawo Moyo Wamuyaya,ngati Mulungu wakupatsani inu Moyo Wamuyaya, inu mulinawo Iwo kwanthawizonse. Mukuona? Chifukwa onani. Ngatiukanati usakhale, Yesu apezeka ali mphunzitsi wabodza. MuYohane Woyera 5:24, Iye anati, “Iye amene amva Mawu Angandi kukhulupirira pa Iye amene anandituma Ine ali nawoMoyo Wosatha, ndipo sadzabwera konse ku chiweruzo, komawachoka ku imfa wapita ku Moyo.” Tsopano, tsutsanani nayeIye. “Onse amene Atate wandipatsa Ine…Palibe munthuangakhoze kubwera kwa Ine kupatula Atate atamukoka iye.(Ine ndikubwereza Lemba.) Onse amene adza…Palibe munthuangakhoze kubwera kwa Ine kupatula Atate Anga atamukokaiye poyamba. Ndipo onse omwe Atate Anga wandipatsa Ineadzabwera kwa Ine. (Mukuona?) Ndipo onse omwe abwera kwaIne, Ine ndidzawapatsa iwo Moyo Wosatha (Yohane Woyera6), ndipo ndidzamuukitsa iye pa masiku otsiriza.” Awo ndiwomawu Ake.163 Tsopano onani. Ngati ine ndikanakhoza kubwerera kuAefesomutuwa 1, Paulo akulalikira…Tsopano, Akorinto, winaaliyense anali ndi lirime ndi salmo. Inu mumazindikira mipingoina inalibe vuto limenelo. Iye sananene kanthu za iyo. Kodiiye anayamba watchulapo konse malirime paliponse mu mpingowa Aefeso, mpingo wa Roma? Ayi! Iwo anali nawo malirimendi chirichonse basi monga Akorinto analiri, koma iwo analiataziyika izo mu dongosolo. Akorinto sankakhoza basi kuziyikaizo mu dongosolo. Mukuona? Koma Paulo anapita uko ndipoanakawuyika mpingowomu dongosolo.

Page 46: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

472 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

Tsopano, iye…Ine ndikukhulupirira, monga Oral Robertsamanenera, “Mulungu ndi Mulungu wabwino.” Kodi inusimukukhulupirira zimenezo?164 Ndipo inu mukuti, “Chabwino, nanga bwanjiAchipentekoste ndi malirimewo ndiye, M’bale Branham?” Inendikuganiza iwo ali nawo Mzimu Woyera. Ndithudi iwo ali.Chabwino, bwanji? Taonani. Inu mukukhulupirira kuti Iye ndiMulungu wabwino? Tomasi anati nthawi ina, “Inu mukudziwa,Ambuye…”

Ena onse a iwo ankamukhulupirira Iye. Ankati, “O, ifetikudziwa Iye ndi weniweni!”

“O,” Tomasi anati, “ayi, ayi, ine sindikuzikhulupirira izo.Njira yokha yomwe ine nditi ndikhulupirire izo, ine ndiyenerakuti ndikhale nawo umboni wina. Ine ndisowa kuti ndilowetsezala zanga mu mbali Mwake ndi mu zipsyera za misomali mumanja Ake.”

Iye ndi Mulungu wabwino. Iye anati, “Bwera, Tomasi.Nazi apa.”

“O,” Tomasi anati, “tsopano ine ndikukhulupirira.”165 Iye anati, “Inde, Tomasi, iwe utandiwona Ine kaye, ndipoutandimverera Ine, ndi kuika dzanja Langa…manja ako mumbali Mwanga, iwe ukukhulupirirano. Koma kukula kwakenkotani kuli kwa mphoto yawo amene sanayambe awonandipo komabe akukhulupirira.” Iye ndi Mulungu wabwino. Iyeamakupatsa iwe chokhumba cha mtima wako, ndithudi. Tiyenitizingomukhulupirira Iye. Ndiko—ndiko—ndiko kumenya kwakumupha Satana. Pamene munthu amutengaMulungu paMawuAke, m’bale, izo zingamuphe Satana nthawi iliyonse. Ndikokumenya kolimbitsitsa kumene Satana angakhoze kukulandira,pamene munthu amutenga Mulungu pa Mawu Ake. Inde, bwanaMonga ine ndinati, “Munthu sadzakhala moyo (Yesu, usikuwina), koma ndiMawu onse otuluka kuchokera…”166 Tsopano, zindikirani izi. Tsopano ine ndikuti ndiyambire pandime yoyamba:

Chotero posiya zoyambirira za chiphunzitso chaKhristu, tiyeni ife tipitirire mpaka ku ungwiro;…(Tsopano, chinthu choyamba chimene ine ndikufunakuti inu muchidziwe: kodi Paulo akuyankhula ndindani apa? Aheberi. Iwo akuti, “Aheberi,” pamwamba,Bukhu la Aheberi. Ndi kulondola uko? Ayuda omweanali atamukana Yesu… Mungakhoze inu—inumukuzigwira izo tsopano? Iye akuyankhula kwa Ayuda,kumawasonyeza iwo mthunzi wa lamulo kukhalachoimira cha Khristu. Zinthu zakale zonse zoimiraza zatsopano. Tsopano penyani.)

Page 47: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 473

…posiya zoyambirira za chiphunzitso cha Khristu,tiyeni ife tipitirire mpaka ku ungwiro;…

167 Tsopano, iye wakhala akuyankhula kwa iwo za ziphunzitso.Tiyeni ife tipite ndi kumayankhula za zinthu zaungwiro.Tsopano, inu mumakhalitsidwa angwiro mwa Mulungu pameneinu mwasindikizidwa ndi Mzimu Woyera mpaka tsiku lachiwombolo chanu. “Iye amene ali wobadwa ndi Mulungu (lYohane) samachita tchimo; pakuti iye sangakhoze kuchimwa,pakuti Mbewu yaMulungu ikanali mwa iye.”168 Munthu yemwe ali wodzazidwa ndi Mzimu Woyera,osati woganizira kuti iye anadzazidwa, koma iye ameneali wobadwa ndi Mzimu wa Mulungu samachita tchimo,pakuti Mbewu ya Mulungu ili mwa iye, ndipo iye sangakhozekuchimwa. Mukuona? Kodi Baibulo limanena chomwecho?Chotero ndi izo apo. Inu muli…Osati zomwe inu mumachita,zomwe, ndi zomwe, osati zomwe dziko limaganiza za inu,ndi zomwe Mulungu amaganiza za inu. Mwaona, mukuona?Inu simungakhoze…Ine ndingakhoze bwanji kukhala ndichilolezo cholembedwa ndi meya wa mzinda, kuti ine ndikhozakumathamanga mailosi forte pa ora kudutsa mu mzinda, ndipompolisi aliyense nkundimanga ine? Ine sindingakhoze. Inendingakhoze kuchimwa bwanji pamene pali nsembe ya magazipamaso pa Mulungu mosalekeza, pamene Iye sangakhoze konsekumandiwona ine, pamene pali chotchinga pa—pa…patsogolopa ine ndi Mulungu, chishango cha Magazi; pakuti ndife akufa,ndipo moyo wathu wabisidwa mwa Khristu kupyolera mwaMulungu, osindikizidwa ndi Mzimu Woyera. Ungakhoze bwanjimdziko kuchita chirichonse cholakwika pamaso pa Mulungu.“Ngati ife tichimwa mwadala (Aheberi 10) ife titalandirakale chidziwitso cha Choonadi, sipamakhalanso nsembe kwatchimolo.” Mkati umu ndi zosatheka (mukuona?) kuti uchimwemwadala.169 Tsopano, tiyeni tipitirire nazo ndi kuziwerenga. Chabwino.

…ungwiro; osati kuikanso maziko a—a kulapa kuntchito zakufa, ndi…chikhulupiriro cha kwaMulungu,Za chiphunzitso cha maubatizo,…kuika kwa

manja, ndi za chiukitsiro cha akufa, ndi…chiweruzochamuyaya.Ndipo izi…ife tizichita, ngatiMulungu alola.(Tsopano apa ndi pamene iwo anafuna kuti ayambire,

kuchokera pa ndime ya 4.) Pakuti ndi kosathekakwa iwo…amene anawalitsidwapo, ndipo alawa zamphatso yakumwamba, ndipo anapangidwa kukhalaogawana nawo za Mzimu Woyera,Ndipo analawa nawo za mawu abwino a Mulungu, ndi

mphamvu za dziko likudza ilo,

Page 48: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

474 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

Ngati iwo adzagwa, kuti akakonzedwenso—kuwakonzanso iwo kachiwiri kuti alape; powona kutiiwo akudzipachikira kwa okha Mwana wa Mulungukatsopano, ndi kumuika iye ku manyazi apoyera.

170 Tsopano, tsopano, izo zikuwoneka mofanana, kuchokeramomwe inu mukuziwerengera izo apo, kuti munthu akhozakulandira Mzimu Woyera, ndiyeno nkubwerera mmbuyo ndikutayika. Koma ndi zosatheka kuti iye achite izo. Mukuona? Iyesangakhoze kuchita izo. Ngati iye angatero, Khristu ananama.Mukuona? Ndi zosatheka kwa iwo omwe anawalitsidwapo.Tsopano, penyani apa. Kodi iye akuyankhula kwa ndani? Iyeakuyankhula kwa Ayuda ammalire awo. Iye sanati konsemunthu ali wodzazidwa ndi MzimuWoyera; iye anati, “Ngati iyeanalawa Mawu a Mulungu.”171 Tsopano,mungondilora ine ndipereke izomwa fanizo, koterokuti inu muwone ndipo musaphonye izo tsopano. Tsopano, iyeakulembera kwa Ayuda awa. Ena a iwo ndi okhulupirira ammalire. Mukuona? Iye anati, “Tsopano, ife tizisiya ntchito izindipo tipita tikayankhule za ungwiro.” Anati, “Tsopano, ifetayankhula za maubatizo, ndi kuuka kwa akufa, ndi kusanjikakwa manja, ndi chirichonse; koma tiyeni tipitirire nazo tsopanokuti tikayankhule za ungwiro. Tsopano, ife tikuti tiyankhuleza pamene inu mubwera mu Mzimu Woyera. Tsopano, inumwakhalamukutsalira pamsonkhano kwa nthawi yaitali…”172 Ndipo inumwawawona anthu amenewo. Iwo amatsalira: iwosangalowe mkati kapena kuchokapo. Iwo amauyamikira MzimuWoyera. Iwo amabwera pafupi. Ndipo mwinamwake MzimuWoyera umachita chinachake ndi, amuna, iwo amaimirirandi kumafuula, ndi kumalumpha chokwera-ndi-chotsika pansichifukwa cha izo, koma iwo safuna konse kuti awulandireIwo iwoeni. Ayi, ayi! Mukuona? Ndipo iwo amati, “O, inde,izo nzabwino. O, ine sindikudziwa za izo tsopano.” Mwaona,mwaona, mukuona? Okhulupirira ammalire. Pafupi kumenempaka iwo akhoza kulawa Iwo, komabe iwo samaulandira Iwo.Mukuona? Tsopano, iwo amatsalira pozungulira monga chonchomotalika kwambiri mpaka pakapita kanthawi iwo amachokakokwathunthu. Ine ndikhoza kutchula maina a ochuluka omweanali ku kachisiyu, anachita chinthu chomwecho. Kugwa njirayonse kachiwiri, kuti adzikonze okha mwatsopano mwa kulapa,palibepo kulapa kwa iwo. Iwo anangowukwiyitsa Mzimu kutiutalikire kwa iwo. Iwo akhala ali pafupi kwambirimpaka…173 Apa, ngati inu mungatembenuze ndi ine (inu mulibe nthawi,ine ndikudziwa, tsopano) koma ngati inu mungatembenuze kuDetoronome mutu wa 1 ndi kuwerenga izo, inu mupeza chinthuchomwecho. Muzilembe izo apo tsopano, Detoronome mutu wa1. Tsopano, ndipo muyambire pa ndime ya 19 ndi kuwerengampaka pa 26. Detoronome… Inu mupezapo…Tsopano onani.Israeli yense…Zomwe anthu amenewo amachita, iwo amafika

Page 49: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 475

ku Kadeshi-barnea. O, ine ndikuwona chinachake! Kachisi uyu,dziko la Chipentekoste lino liri pa Kadeshi-barnea pakali pano.Ndiko kulondola ndendende, M’bale Neville. Ife tiri pa Kadeshi-barnea, mpando wa chiweruzo cha mdziko (unali mpandowachiweruzo).174 Ndipo azondi anapita uko. Yoswa ananena apa, “Tsopano,ine ndinatumiza azondi,” kapena Mose, kani, “ine ndinatumizaazondi, thwelofu, mmodzi wa, munthu mmodzi kuchokera mwalirilonse la mafuko anu. Ine ndinawatumiza iwo kuti akalizondedzikolo ndi kubweretsanso uthenga.”Ndi kulondola uko?

Ndipo pamene iwo anabwererako, uko kunali nainikuchokera pa thwelofu anati, “O, ilo ndi dziko labwino, komao, chifundo, ife sitingakhoze kulitenga ilo. O, mai! Aamori alikumeneko, ndipo ife tikuwoneka ngati ziwala pambali pa iwo.Iwo ndi amuna okhala ndi zida. Makoma awo ndi aakulu. O,ndizo…bwanji, ine ndikukhumba ife tikanafera kujamu Iguptommalo moti inu mutibweretse ife kuno.”175 Bwanji, ka Kalebu kachikulire ndi Yoswa analumphapamenepo ndipo anawatontholetsa iwo; anati, “Ndife okhozamoposa kuti tilitenge ilo.” Inde, bwana! Ndi ameneyo apo.Tsopano taonani. Ndi chiani chinachitika? Kalebu ndi Yoswaankadziwa kuti Mulungu anapereka lonjezo la ilo: “Inesindikusamala kaya ndi lalikulu bwanji ilo, kaya zotchingazondi zochuluka bwanji, kaya ndi zazitali bwanji, kaya ndizazikulu bwanji, izo ziribe kanthu kochita ndi izo. Mulunguananena chomwecho, ndipo ife tikhoza kulitenga ilo.” Ndipokodi inu mukudziwa kuti iwo anali anthu awiri okha, kuchokeramu mamilioni awiri ndi theka, omwe anawoloka konse kupitamu dzikolo? Chifukwa iwo anagwiritsa chikhulupiriro chawomu zomweMulungu anati kuti ndi Choonadi. Ameni!176 Kachisi, pakali pano, waima pa Kadeshi-barnea. Taonani,anthu amenewo anali pafupi kwambiri mpaka iwo analawakumene mphesa zochokera mdzikolo. Iwo anadya mphesazo.Pamene Kalebu ndi iwo anapita uko ndipo anakabweretsakomphesa, anyamata amenewo anakathyolako zina ndi kumadyaizo. “O, izo ndi zabwino, koma ife sitingakhoze kuzichita izo.”“Iwo amene analawa ntchito yabwino ya Mulungu, analawapoza Mzimu Woyera, anawona ubwino wa Iwo, analawa za Iwo,analawapo za Mawu a Mulungu…” Mukuona izo? Palibealiyense wa amuna amenewo, palibe mmodzi wa iwo anayambawalolezedwa kuti apite uko. Iwo anawonongeka mu dziko lawolomwelo, komwe kuno mu chipululu. Iwo sanapiteko konse,komabe iwo anali oyandikira mokwanira kuti alilawe Ilo, komaopanda chisomo chokwanira ndi chikhulupiriro kuti alitenge Ilo.Ndicho chimene izo ziri.177 Tsopano. Tsopano tamvetserani kwa munthu wokondedwauyo yemwe analemba kalata iyi. Tiyeni tingowerenga ndime

Page 50: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

476 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

yotsatirayo. Penyani miniti yokha. Mpenyeni Paulo. Tsopanotiyeni tiwerenge ya 7:

Pakuti dziko…limamwa mu mvula yomwe imadzamowirikiza pa ilo, ndi kumeretsa masamba chakudyakwa iwo omwe amalilimira, zimalandira madalitsoochokera kwa Mulungu:Koma izo zomwe zimabala minga ndi nthula

zimakanidwa ndipo ziri pafupi ndi kutembereredwa;zomwe mapeto ake ndiwo kuti ziwotchedwe.

178 Tsopano, mukuona zomwe iye akunena? Tsopano penyani.Panali funso ili apa; tsopano, ndiyeno ife titseka…Chinthu ichichimakhala ngati chindipha ine kwa zaka.179 Ine ndinapita ku msonkhano nthawi ina kumene anthu analikuyankhula mu malirime ku Mishawaka, Indiana. Tsopano,ine ndiri patsogolo pa khamu langa lomwe. Inu mwawamvapoanthu amenewo…mwandimvapo ine ndikunena mbiri ya moyowanga, ndi za munthu wachikuda yemwe anati, “Ndi uyu pano.Ndi uyu pano.” Tsopano, ine ndinakuuzani izo.180 Koma zina za izo: Ine ndinawawona amuna awiri. Iwoanali…Mmodzi ankakhoza kupereka uthenga, mmodziwinayo kumatanthauzira izo. Wina akapereka uthenga,ndipo winayo ankatanthauzira iwo. Ndipo m’bale, iwo analiakulondola. Basi izi…ine ndinaganiza, “Ubwino wanga! Inesindinayambe ndawonapo chirichonse chonga izo.” Ine ndinati,“Ine ndiri pakati pa angelo.” Ine ndinaganiza, ine sindinayambendawonapo chirichonse…Wina anali kuyankhula, ndipowinayo…181 Ndipo ine ndinakhala kumbuyo uko, ngati kamlalikikachikulire, inu mukudziwa. [Malo osajambulidwapa tepi—Mkonzi.]…amuna onsewo nthawiyina ndipondinagwirana nawo chanza. Ine ndinali ndisanawawonepoamuna oterowo mu moyo wanga. Iwo ankakhoza kuyankhulauthenga, ndipo winayo ankakhoza kuzitanthauzira izo.Ndipo mai, mai! Izo zinali zodabwitsa! Mmodzi ankakhozakuyankhula ndipo winayo nkutanthauzira. Onsewo…Ndipoiwo ankangosanduka oyera ngati choko pamene iwo ankaimitsamanja awo mmwamba. Ine ndinaganiza, “O mai, mai, kodiine ndakhala ndiri kuti moyo wanga wonsewu. Ichi ndichochinthucho!” Ine ndinati, “Mai, Achipentekoste ali kulondola.”Uko nkulondola ndendende.182 Ine ndinali ndisanawonepo zochuluka koma basi zomwezinali za cha komwe kuno, kumene…Mwinamwake akaziangapo ali ndi utumiki kwinakwake. Ndipo iwo amakhalaakukangana; ndipo wina kumamutcha mzakeyo, “chisacha akhungubwe,” ndipo, inu mukudziwa, basi mongachoncho, kukhala ngati kumakangana wina ndi mzake. Osatikuwanyozetsa akaziwo tsopano kapena chinachake ayi, koma

Page 51: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 477

basi…Izo—izo zinali mchikhalidwe chofooka. Ngati aliyensewa inu…Inu mukukumbukira, M’bale Graham. Inu munalimnyamata wamng’ono chabe pa nthawi imeneyo. Ndipo chotero,umo ndi momwe izo zinaliri.

Ndipo ine ndinamvetsera kwa izo, ndipo ine ndinaganiza,“O, mai, ine ndakumanizana ndi angelo.”183 Tsiku lina ndikubwera kuzungulira pa ngodya ya nyumbayo,cha mu tsiku lachiwiri, ine ndinakomana naye mmodzi waamunawo. Ine ndinati, “Inumuli bwanji, Bwana?”

Iye anati, “Iwe uli bwanji?” Iye anati, “Kodi…Dzina lakondiwe ndani?”

Ndipo ine ndinati, “Branham.”Iye anati, “Ukuchokera kuti iweyo? Kuno?”Ndipo ine ndinati, “Ayi, ndinewochokera ku Jeffersonville.”Iye anati, “Chabwino, izo nzabwino. Kodi ndiwe

Wachipentekoste?”Ine ndinati, “Ayi, bwana, ine sindiri.” Ine ndinati, “Ine

sindimavomereza basi njira ya Chipentekoste yolandiriraMzimuWoyera,” ine ndinati, “komabe,” ine ndinati, “ine ndiri kuno kutindiphunzire.”184 Iye anati, “Chabwino, izo nzabwino mwamphamvu.” Ndipondikuyankhula ndi iye, ndikuwugwira mzimu wake (mongamkazi pa chitsime), iye anali Mkhristu weniweni. M’bale,ine ndikutanthauza iye ankamvekera bwino ndithu. Iye analiwabwino. Tsopano, inu nonse…Ndi angati omwe mwakhalamulipo mu misonkhano yanga ndipo mwaziwonapo zinthuzimenezo zikuchitika? Inu mukuona? Ndipo bamboyo analiwabwino mwangwiro. Chotero ndiye, ine—ine ndinaganiza,“Apo! Mai, ndi zodabwitsa bwanji!”185 Pafupi usiku umenewo, madzulo nthawiyina, inendinakomana naye winayo. Ine ndinati, “Inu muli bwanji,Bwana?”

Iye anati, “Iwe uli bwanji? Dzina lako ndiwe ndani?” Ndipoine ndinamuuza iye. Ndipo iye anati, “Kodi…Kodi—ndiwe waChipentekoste?”

Ine ndinati, “Ayi, bwana, osati kwenikweni waChipentekoste, ine sindikuganiza.” Ine ndinati, “Inendangobwera kuno kuti ndidzaphunzire.”

Iye anati, ine ndinati, iye anati, “Iwe unayambawalandirapoMzimu Woyera?”

Ine ndinati, “I—ine sindikudziwa.” Ine ndinati, “Malinganandi zonse zomwe inu nonse muli nazo, ine ndikulingalira inendiribe.”

Ndipo iye anati, “Unayambawayankhulapomumalirime?”

Page 52: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

478 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

Ine ndinati, “Ayi, bwana!”

Iye anati, “Ndiye iwe sunayambewakhala nawo Iwo.”186 Ndipo ine ndinati, “Chabwino, ine—ine ndikulingalira ukonkulondola.” Ine ndinati, “Ine sindikudziwa. Ine ndangokhalandikulalikira pafupi zaka ziwiri, kucheperapo,” ndipo inendinati, “Ine sindikudziwa zochuluka kwambiri za Iwo.” Inendinati, “Mwinamwake ine sindikudziwa.” Ine ndinati, “Inesindikukhoza kuzimvetsa…” Chifukwa chimene, ine ndinalikuyesera kuti ndimugwirebe iye apo (mwaona?), kuti ndiugwireuwo. Ndipo pamene ine ndinatero, ngati ine ndinayambandakomanapo ndi wachinyengo, apo panali mmodzi wa iwo.Mkazi wake anali wa mutu-wakuda; ndipo iye anali akukhalandi mkazi wa mutu wa bulondi, anali nao ana awiri ndi iye;ndipo nkumayankhula mu malirime, kumawatanthauzira iwomwangwiro basi monga izo zikanakhoza kukhalira. Ndipo inendinati, “Tsopano, Ambuye, kodi ine ndalowa mu chiyani?”Kuchokera kwa angelo, ine sindimadziwa kuti ndinalowamu chiani. Ine ndinati, “I—ine—ndine wachikhazikitso; izoziyenera kukhala Baibulo. Izo ziyenera kukhala molondola.Pali chinachake chalakwika penapake, Ambuye. Izo zingakhalemotani?”187 Ine ndinapita ku msonkhano usiku umenewo, ndipoMzimu uwo umakhoza kugwa; ndipo m’bale, iwe umakhozakuwumverera iwo, kuti Iwo unali Mzimu Woyera. Inde, bwana!Ngati Iwo sunali, Iwo umachitira umboni ndi mzimu wangakuti Iwo unali Mzimu Woyera. Ndipo ine ndinangokhalamlaliki wamng’ono, ndipo sindinkadziwa momwe, mochulukaza kuuzindikira mzimu. Koma ine ndinali nditakhala apo.Ndipo ine ndikudziwa kuti Mulungu yemweyo ameneanandipulumutsa ineyo, uko kunali kumverera kofanana…Ndinamverera ngati ndinali kupita kudutsa pa denga, ukokunali kumverera kodabwitsa chotero mu nyumba imeneyo.Ndipo ine ndinaganiza…188 Pafupi mazana fifitini a iwo kumeneko. Ndipo inendinaganiza. “Mai, o mai!” Magulu awiri kapena atatu a iwoanali atakomana palimodzi. Ndipo ine ndinaganiza, “Nditi,mai! Zikukhala motani izo? Tsopano, Mzimu waukulu uwo muchipinda ichi ukugwamonga choncho; ndipo kuno, tayang’ananipa ichi chiri kupitirira umo, amuna awo akuyankhula mumalirime, kutanthauzira, kupereka uthenga mwangwiro—ndipo mmodzi wa iwo wachinyengo ndi winayo munthuweniweni wa Mulungu.” Ndipo ine ndinaganiza, “Tsopano,ndinewosokonezeka yense. Ine sindikudziwa choti ndichite.”189 Chabwino, mwamsanga zitachitika izo, mzanga wabwinokwa ine, M’bale Davis (inu mukumudziwa), anayamba kumatiine ndinali chipapeti. Ndicho chidole cha msungwana, inumukudziwa. Ndipo chotero, ine ndinali wosakwatira, ndipo

Page 53: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 479

chotero ine…Iye anayamba kumapitiriza ndi ine, ndiyenokumapitiriza, kumakhala ngati kumandinyoza ine.190 Ndipo ife tinkakhala ndi zapang’ono…Ndipo amayi anundi tonse ife tinkakhala ndi misonkhano yaing’ono ku maloosiyana. Kachisi sanali—sanali akuyenda nthawi imeneyo, ndipoife tinali kukhala ndi misonkhano yaing’ono mu malo osiyana.Ndipo potsiriza tsiku lina, kachisi atamangidwa kale, zakazambiri kenako, ine ndinapita uko ku Chigayo cha a Green kumphanga yanga kuti ndikapemphere, chifukwa M’bale Davisanali atanena zinthu zina zoipa pa ine mu—mu—mu pepala yake.Ine ndinkamukonda iye. Ine sindinkafuna kuti pachitike kanthukena, ndipo ine—ine ndinapita uko kuti ndikamupempherereiye. Ndipo ine ndinapita uko, ndipo ine ndinakalowa mumphanga. Ndipo ine ndinakhala mkati mmenemo pafupi masikuawiri. Ndipo ine ndinati, “Ambuye, mukhululukireni iye. Iye—iye sakutanthauza—sakutanthauza izo.” Ndipo ine ndinaganiza,“Inu mukudziwa…” Ine ndinangopezeka ndikuganiza zaLemba.191 Ndipo ine ndinatuluka. Ndipo uko kunali chipika (chipikachimenecho chikadali pamenepo, ndinali pa icho osati kalelitali) ukamatsika phirilo ndipo pali kanjira kakang’onokamene kamabwera mozungulira kuchokera ku khwawa. Ndipoine ndinangokhala pa chipikacho, ndikuyang’ana kudutsamapiri mmbuyo—kumbuyo uko, ndipo ndinaika Baibulo langaapo monga choncho. Ine ndinaganiza, “Inu mukudziwa…”Ine ndinali ndikuganiza za Lemba: “Wosulamkuwa, iyewandichitira ine zoipa zambiri, ndipo wanena zinthu.” Inumukudziwa…Ine ndinaganiza, “ine ndikukhulupirira inendingoziwerenga izo.” Ine ndinalitsegula Baibulo, ndipo inendinati, “Chabwino…” Ndinaipukuta nkhope yanga, ndipomphepo inawomba, ndipo iyo inalitsegula ilo ku Aheberi 6.“Chabwino,” ine ndinati, “apo si pamene izo ziri.” Ndipoine ndinaliyika Ilo mmbuyo monga chonchi. Ndipo mphepoinakupiza kachiwiri ndipo inalitsegula Ilo kachiwiri. Ndipo inendinati, “Tsopano, izo ndi zachilendo, mphepo kumalikupizailo mobwereza monga choncho.” Chotero ine ndinaganiza,“Chabwino, ine ndikukhulupirira ine ndiziwerenge izo.” Ndipolinati:

Pakuti ndi zosatheka kwa iwo ameneanawalitsidwirapo kale,…anapangidwa kukhalaogawana nawo za Mzimu Woyera, ndipo analawa…zaMawu a Mulungu, ndi zinthu za dziko likudzalo.Ine ndinaganiza, “Chabwino, ine sindikuwonapo kanthu

ndi izo.” Ndinaziwerenga izo mpaka mmusi, mutu wonsewo.Munalibe kalikonse umo. Ine ndinati, “Chabwino, ndizo—izozikukhazikitsa icho kwa izo.” Ndipo ine—ine ndinaziwonaizo monga chonchi, ndi mobwereza ilo linapitapo kachiwiri.Ndipo ine ndinalitenga Ilo, ndipo ine ndinaganiza, “Chabwino,

Page 54: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

480 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

kodi nchiani izo?” Ine ndinapitiriza kuziwerenga izo, ndikuziwerenga izo, ndi kuziwerenga izo. Ine ndinati, “Chabwino,ine sindikukhoza kuzimvetsa.”Ndiye ine ndinapitirira…Ndipoine ndinawerenga mpaka pansi:

…ziri zosatheka kwa iwo omwe anawalitsidwapokale,…Izo zinafikampaka pansi pamalo pamene iwo anati:Ndipo dziko lapansi…limamwa mu mvula yomwe

imadza mowirikiza pa ilo, kuti lizibala zomerachakudya kwa iwo omwe amazilimira, limalandiramadalitso ochokera kwa Mulungu:Koma izo zomwe zibala minga ndi nthula

zimakanidwa, ndi…kuyandikira ku themberero;zomwe chiweruzo chake ndi kuti ziwotchedwe.

192 Ine ndinati, “Ndikudabwa chomwe izo zikutanthauza?”Ine basi…Tsopano, ine sindinali kuganiza za kanthupamwamba apo. Kumangoganiza izo. Ndipo nthawi yomweyopamene ine ndinali nditakhala pamenepo, ine ndinkaganizaAmbuye akanati andipatse ine masomphenya okhudza M’baleDavis ndi iwo kumusi uko. Ndipo ine ndinali nditakhalaapo; ine ndinayang’ana, ndipo ine ndinawona chinachakechikutembenuzika modutsa kumitengoko patsogolo pa ine.Ndipo ilo linali dziko likutembenuzika. Ndipo ine ndinawona ilolonse linali litalimidwa, linkangowoneka ngati kuti linali lonselitatipulidwa konse. Ndipo Mwamuna anapita uko ali ndi—c—chinthu chachikulu kwambiri patsogolo pa Iye chodzazandi mbewu, ndipo Iye anali akufesa mbewu njira yonsekudutsa pa dziko lapansi pamene Iye anali kupita. Ndipo Iyeanapita kuzungulira kobisika kwa dziko lapansi, ndipo Iyeanachoka ku nkhope yanga. Ndipo mwamsanga pamene Iyeanachoka ku nkhope yanga, apa panadza bambo wooneka-mwaukathyali, atavala zovala zakuda, akupita chozunguliramonga chonchi, akuti [M’bale Branham akupanga phokoso kutiafotokoze—Mkonzi.] akuponya mbewu zoipa [M’bale Branhamakubwereza phokosolo—Mkonzi.] Ndipo ine ndinkaziyang’anaizo, ndipo pamene dziko linkapitirira kutembenuzika…193 Patapita kanthawi tirigu anatulukira. Ndipo pamene tiriguanatulukira, kuchokera umo kunabwera mitungwi, nthula, ndiminga, ndi udzu wonunkha, ndi chirichonse chikumera, thengolamkaka, ndi chirichonse chikumera mu tirigumo. Ndipo izozonse zinali kumerera palimodzi. Ndipo apo panadza chilalachenicheni, choipa, ndipo tirigu wamng’onoyo anali atatukulamutu wake monga choncho, ndipo mtungwi waung’onowo,ndi nthula, minga, izo zinali zitatukula mitu yawo. Udzuuliwonse kumangoti [M’bale Branham akupanga phokoso lawefuwefu—Mkonzi.] kumapuma monga choncho. Iwe umakhozabasi kumazimva izo. Ndipo izo zinali kuitanitsamvula,mvula.

Page 55: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 481

194 Ndipo patapita kanthawi, motsatira kunadza mtambowaukulu kwambiri, ndipo madzi anangokhuthukira pansi.Ndipo pamene iwo anagwera pamenepo, tirigu uja analumphirammwamba ndi kuyamba kufuula, “Ulemerero, Aleluya, AmbuyeAlemekezeke!” Mmwamba unalumphira udzu waung’onowonunkha ndi kumafuula, “Ulemerero, Ambuye Alemekezeke,Aleluya!” Minga ndi zonse izo, zikuvina mozungulirammunda wonsewo zikufuula, “Ulemerero, Aleluya, Ambuyealemekezeke!”

Chabwino, ine ndinati, “Ine sindikukhoza kuzimvetsa izo.”195 Masomphenya anandichokera ine; ndiye ine ndinagwerammbuyo pa zija kachiwiri: “Nthula zomwe zayandikira kutizikanidwe” Ndiye ine ndinazimvetsa izo. Yesu anati, “Mvulaimagwera pa olungama ndi osalungama.” Munthu akhozakukhala mu msonkhano, akhoza kuyankhula ndi malirime,akhoza kufuula ndi kumachita chimodzimodzi monga onseamene ali ndi Mzimu Woyera weniweni ndipo nkusakhalabeali mu Ufumu wa Mulungu. Ndi kulondola ndendende.Kodi Yesu sanati, “Ambiri adzaima mu tsiku limenelo nati,‘Ambuye, kodi ine sindinatulutse ziwanda mu Dzina Lanu;kodi ine sindinalosere (kulalikira) mu Dzina Lanu; kodiine sindinachite ntchito zambiri zazikulu mu Dzina Lanu?’”Yesu anati, “Chokani kwa Ine, inu ochita kusaweruzika, inesindinakudziweni nkomwe inu.”Nanga bwanji zimenezo?196 Pano pali ndendende chomwe izo zikutanthauza apa.Mwaona? Iwo analawa mvula yabwino yochokera Kumwamba.Koma pakuyamba pomwe, iwo anali olakwika. Pakuyambapomwe zolinga zawo sizinali zolondola; zokhumba zawo sizinalizolondola. Ndiko, inu simungakhoze kudziwa. Inu mukudziwa,pa kukolola iye anati, “Kodi ine ndipite uko ndi kukazizulazonsezo?”197 Iye anati, “Zisiyeni izo zikulire palimodzi, ndipo pa tsikulimenelo minga izi ndi nthula zidzawotchedwa palimodzi,ndipo tirigu adzapita ku nkhokwe.” Tsopano, iwe ungadziwebwanji kuti minga ndi iti, kapena nthula ndi iti, kapenatirigu ndi uti? “Ndi zipatso zawo inu mudzawadziwa iwo.” Inumukuona, M’bale, Mlongo, mtengo wabwino sungakhoze kubalachipatso choipa. Ziribe kanthu, penapake potsatira msewuwu,izo zidzakugwirani inu. Kotero, inu muli kufunafuna ubatizowa Mzimu Woyera…Ndine wokondwa yense yemwe analembailoyo. Mukuona?198 Tsopano, okhulupirira ammalire awo kumbuyo uko, iwoanali limodzi nawo. Iwo anali atadulidwa ndi mdulidwe wao.Iwo anapita mpaka ku dziko lomwe Mulungu analilonjeza, kumalire komwe a ilo. Anthu ambiri amayenda mpaka ku malireamenewo. Iye amayenda mpaka ku ubatizo wa Mzimu Woyerawomwe ndi kuwukana iwo. Iye samafuna kuti awulephere iwo.

Page 56: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

482 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

Iye amayenda kumene mpaka ku Lemba lomwe la ubatizo muDzina la Yesu Khristu, ndi kutembenuzira nsana wake, ndikukana kuti alephere kuziwona izo.

199 Mulibe Lemba limodzi mu Baibulo lonse pamene winaaliyense anayamba wabatizidwapo mu dzina la Atate, Mwana,Mzimu Woyera, palibe Lemba limodzi. Mpingo wa Katolikaunayambitsa izo, zinatuluka mwa Lutera, mpaka kwa Wesile,ndipo azikoka izo kudutsa mpaka kuno. Kulondola ndendende.Koma dongosolo la Mwamalemba ndi Dzina la AmbuyeYesu Khristu. Umenewo ndiwo ubatizo wautumwi. Iwesungakhoze kuchita izo ndi kumakhalabe mu chipembedzo.Ndiko kulondola.

200 Tsopano, inu mukuona zinthu izo? Ubatizo wa MzimuWoyera, mphatso za Mzimu, zinthu zomwe Mulunguamazibweretsapo…Chipatso cha Mzimu ndicho chikondi,chimwemwe, kuvutika-motalika (o, inu mukuti, “Koma M’baleBranham, Mulungu adalitsike, ndine wovutika-motalika.” Izozikuwoneka ngati choncho. Ine ndinapita ku Ohio kuno osatikale litali, ndipo winawake anandifunsa ine, analembera kalatakunoko ndipo anandifunsa ine ngati ine ndimawabatiza anthumu Dzina la Yesu Khristu. Ine sindinanene konse mawu. Iwoanazipeza izo mulimonse, ndipo azitumiki sikisitini ogwirizanaanachokako. Ndiko kuvutika-motalika sichoncho uko!)—kuvutika-motalika, ubwino, kufatsa, kudzichepetsa, kupirira,ndi MzimuWoyera. Mwaona?

201 O, M’bale, Mlongo, ndife—ife tiri pa Kadeshi-barnea. Inumukulawa tsopano. Usiku watha Mzimu Woyera unagwera paife, unabwera mwa ife, kulowa monga mphepo yankokomo.Iyo inadzakhala pa ambiri a inu. Lero atumiki akhalaakuyendera makomo kuno ndi uko, kumakasanjika manja ndikumawapempherera iwo omwe akufunafuna Mzimu Woyera.Musati inu mutenge cholowezammalo. Musati muzitengamtundu wina wa phokoso. Musati inu muzitenga mtunduwina wa kugirigisha. Inu mudikire pamenepo mpaka Mulunguatakuwumbani inu ndipo atakupangani inu cholengedwachatsopano, atakupangani inu munthu watsopano. Inumukuulawa Iwo tsopano, kungoulawa Iwo, koma muloleNkhunda ikutsogolereni inu mpaka ku tebulo, ndi—ndipoMwanawankhosa ndi Nkhunda zikhale pansi limodzi, ndikumadya kwanthawizonse pa Mawu a Mulungu. Pakuti Iwoadzaima pamene padzakhala kulibe miyamba kapena dzikolapansi;Mawu aMulungu adzakhala alipobe. Izo ndi zoona.

202 Chonde musati muziganiza kuti ndine wotengeka. Ngati inendakhala ndiri, ine sindimatanthauza kutero. Ngati ine…inendikuyembekeza ine ndawayankha mafunso awa; ine ndatero,mwa kupambana kwa kudziwa kwanga.

Page 57: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 483

203 Ndipo chotero, mu Aheberi 6, ngati inu muti muwone, Pauloakuyankhula kwa Ahebri omwe ankati, “Chabwino, ife tipitananu inu motalika chonchi.” Iwo azibwera. Inu mukuona? Nati,“Tsopano, inumuli…” Iwo amene abwera apa ndipo alawa.204 Ine ndinangopezeka ndikuyang’ana mmbuyo muchipindamu. Kuti ndikusonyezeni inu umboni wa MulunguWamoyo. Ine ndikuyembekeza sindikumupanga munthuuyu kuwonekera. Ine ndinabwera muno ndikuchokera kumsonkhano osati kale litali, ndipo ndinabwera kuno, ndipondinalengeza kwa inu kuti mzanga wabwino, bwanawe waine, mzanga wosaka naye, bambo yemwe wakhala wabwinokwa ine, munthu yemwe anafikako ku mpingo wanga, ndipoanakhala ali m’bale wanga; ine ndinkamutcha iye Busty. Dzinalake ndi Everett Rodgers; ankakhala ku Milltown. Ndi angatiakukumbukira ine nditabwera kuno ndi kudzalengeza izo? Iyeanali atagona muno mu chipatala; madokotala anamuchitaiye opareshoni, anamutsegula iye, ndipo anali wodzaza ndikhansara iwo anangomusoka iye. Anati, “Iye azilara pakalipano; mu masabata angapo iye akhala atapita; izo zikhala zonsezomwe ziti zidzakhalepo kwa izo. Iye akhala atatsirizika, ndizozonse.”205 Inu mukukumbukira momwe ine ndinaimira kuno pansanja, ndinkamupempherera iye? Ndinapita kumusi uko ndipondinapita mu chipinda, chinachake chinali chikundidya mumtima wanga. Ine ndinayenda kulowa mpaka mu chipinda,ndipo mwamsanga pamene ine ndinamutulutsa aliyense kunjachotero ine ndikanakhoza…M’bale Everett anali atagona apo.Ndipo inu mukumbukira izi. Ine ndinalowa mkatimo; inendinati, “M’bale—M’bale Busty.” (Ine ndinkamutcha iye Busty.)206 Kale litali pamene ife tinali ndi misonkhano ya ku msitulamdima kumusi uko, Amethodisti onse awo kumeneko paphirilo (Gertie, mmodzi wa iwo), anazemberako, ankasuzumiramu msitu wa mpesa kuti awone zomwe ine ndikanati ndinene,ndi monga choncho, kuwopa kuti mpingo wa Methodistiukanati uwachotse iwo. Ndiyeno, ine ndinapita ndipo ndinalindi masomphenya kumeneko, ndipo ine ndinawona nyamaitawunjikidwa mu chitini. Ine ndinagwira mulu wa nsombandipo ndinazimangirira izo pa, ndinaziyika—ndinaziyika izo pazomangira izi, ndipo ine ndinazimanga zingwezo. Ndipo pameneine ndinayang’ana…Ndipo izo zonse zinali mu masomphenya;ine ndinasiya—ndinalisiya gulu la anthu ataima pansi pamsituwo usiku umenewo ndipo ndinapita pamwamba pa phirikwa M’bale Wright. Ndipo iwo samakhoza kundipeza nkomweinemmawawotsatira. Ine ndinati, “Musati winawa inu…”207 Pamene ine ndinali nditaima apo ndikulalikira, apa panadzaKuwala kuja; Lawi la Moto lija linapachikika apa pomwepatsogolo pa ine ndipo linati, “Choka kuno ndipo upite ku tchire;ine ndikayankhula kwa iwe.” Izo zinali pa tsiku lomwelo, tsiku

Page 58: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

484 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

lotsatira pamene iwo anandipeza ine pa phiri apo. Ndipo inendinali ndiri pamwamba apo; ine ndinabisa galimoto yangamu udzu, ndipo ndinali ndiri pa phirilo ndikupemphera usikuwonse ndi tsiku lonse lotsatira. Ena a iwo anabwera uko,anaipeza galimotoyo ndipo anabwera pamwambapo uko…Ilolinali tsiku limene M’bale Graham Snelling, kuno, analandiraMzimuWoyera ndi kuitana kuti alowemu utumiki.208 Pamwamba apo ku mbali ya phiri pamene ine ndinalinditagona apo, ndipo Iye—Iye anandiuza ine zinthu zosiyana zotindizichita ndi kuyankhulana kumene ife tinali nako limodzi.Iye anapereka masomphenya oziwona nsomba izi zitamangidwaapo, anati, “Uwu ndiwompingowakowakuMilltown.”

Ndipo anai kapena asanu za izo zinagwapo; ndipo inendinati, “Ndi ndani uyo?”

Anati, “Mmodzi wa iwo ndi Guy Spencer ndi mkazi wake.Mmodzi winayo ndi Spencer wina uko, ndi awo.” Ndipo Iyeanawatchula ena osiyana, omwe akanati adzagweko.209 Ine ndinawauza iwo; ine ndinati, “Asati aliyense wainu adye.” Akazi anga ndi ine sitinali…Apo panali ifetisanakwatirane; ndipo iye anapita kwawo kuti akakhale utaliwa usiku wonse ndi Mlongo Spencer, mkazi wodabwitsa.Mwamuna wodabwitsa, Guy Spencer ndi bambo wabwino basiyemwe anaimapo mu chikopa cha nsapato. Ndipo iye—ndipoiye anapita kumusi uko, ndipo Opal anati, “Tsopano, taona…”Kwa Meda, iye anati, “Tsopano, Meda, ine ndikukhulupiriraM’bale Bill.” Iye anati, “Koma pamene Opal akhala ndi njala,iye amayenera kukhala ndi nyama ndi mazira.” Kotero iyeanapita uko, ndipo anakakazinga nyama yake ndi mazira, ndipoanakhala pansi kuti azidya izo, ndi kuyamba kunena mdalitso,ndipo anatsamira pa tebulo, akulira, sanakhoze kuzigwira izo.Ndiye iwo anabwera akusaka.210 Ndipo pamwamba pa phiri paja tsiku limenelo, Iyeanandiuza ine ndendende zomwe zikanati zidzachitike. Iyeanati, “Awa achoka, kenako awa achoka.” Koma Iye anali ndigulu lalikulu la nyama ya nchitini. Iye anati, “Uyisunge iyi kutiidzagwiritsidwe ntchito mtsogolo kwa anthu aku Milltown.”Ndipo usikuwina pamene ine ndinamumvaM’bale Creech…Iyeanali muno usiku watha. Ine sindiri…M’bale Creech, kodi inumuli muno usikuuno? Pamene M’bale Creech anabwera kwa ine,anandiyimbira ine, ndipo Mlongo Creech, akulira; bambo akeanali atagona pamenepo. Anati, “M’bale Bill, musati mumuuzeiye. Iye akufa.” Anati, “Iye wadyedwa ndi khansara; madokotalaanamutsegula iye, ndipo iye wangodzaza ndi khansara mongaiye akanakhoza kukhalira.” Ndipo Will Hall (ndipo nonseinu mukumukumbukira iye), pamene dokotala yemweyoanamutsegula iye ndipo iye anali atadzaza ndi khansara…Ine ndinayamba kupita kukasaka agologolo mmawa umenewo,

Page 59: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 485

ndipo ine ndinawaona maapulo aja atapachikika mu chipinda.(Inu mukuikumbukira nkhani iyo ya izo?) Ndipo uko bamboyoakadali moyo lero. Izo zakhala ziri zaka zapitazo. Iye ndi M’baleBusty anali abwenzi.211 Ndipo ine ndinapita uko ku chipatala, chipatala chatsopano(ine ndaiwala chomwe iwo amachitcha icho, kumeneko mu NewAlbany)—chipatala chatsopano. Ndipo ine ndinapita uko kutindikamuwone Busty; ndipo pamene ine ndinalowa mu chipinda,ine ndinati, “M’bale Busty.”

Iye anati, “M’bale Bill.” Anandigwira dzanja langa ndidzanja lokalamba lalikulu ilo; msilikali wakale wa NkhondoYoyamba ya Dziko Lonse, osati nkunena izo iye alipo, koma ndimtima wabwino basi wonga uwo womwe unayamba wagundapansi pa malaya akale a buluu. Iye analigwira dzanja langa.Ine ndakhalapo mu nyumba yake; ndadyapo mu nyumba yake;ndagonapo mu nyumba yake, basi ngati ndinali m’bale wake.Ana ake ndi onse, ndife basi—monga abale amagazi basi.Munthuwabwino.212 Ndipo iye…Koma iye sanabwere nao konse Ambuyemwakuya. Iye…ine ndinamubatiza iye mu Dzina la YesuKhristu. Koma tsiku limenelo pamene mlaliki wa Chimethodistiuja anati, “Aliyense yemwe anabatizidwa mu Dzina la YesuKhristu, chokani pansi pa hema wanga.” Izo zinali zabwino.George Wright ndi iwo anatulukamo. Madzulo amenewo inendinapita uko kuti ndikawabatize mu Dzina la Yesu Khristuku Totten Ford. Gulu lake lonse linalowa mmadzi ndipolinabatizidwa mu Dzina la Yesu Khristu. Chotero ine ndinalikungopitirira. Izo zinali zabwino. Mulungu akakhala ndi inu,ndani angakhale mokutsutsani inu? Ine sindikudziwa nkomwekomwemunthuyo anapita, chomwe chinachitika kwa iye.213 Komabe, ine ndinakalowa mu chipatala. Uko kunaliBusty atagona pamenepo ali wodzaza ndi khansara,madokotala sakanakhoza ngakhale, sanachite kanthu komakungomumanganso iye palimodzi. Busty ananena kwa ine;iye anati, “M’bale Bill, izi ziri kwa cholinga. Chinachakechachitika.”

Ine ndinati, “Inde, Busty.” Ndinayamba kuumverera Mzimuumenewo monga choncho nkokomo wamphepo yomwe inendakhala ndikuikamba, inumukudziwa, ikubwerammenemo.

Iye anati…Pamene ine ndimalowa muno, panali utawalezapa ngodya iyo, utaima mu ngodya imeneyo. Utawaleza ndipangano; pangano la Mulungu. Mulungu anapanga pangano ndiine pa phiri lija tsiku lija. Ndinaika manja anga pa M’bale Bustyndipo ndinamupempherera iye.

Madokotala akuti, “Iye azilalapo. Iye azingotsika pansi.Palibe kanthu koti nkuchita…Iye akhala atapita mu masikuangapo okha.”Ndipo Busty Rodgers…Awo akhala ali masabata

Page 60: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

486 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

ndi masabata ndi masabata apitawo, ndipo Busty Rodgers,wakhala mmbuyo momwe muno mu mpingowu usikuuno,wathanzi ndi wojintcha monga ine ndinayamba ndamuwonapoiye akuwoneka mmoyo wanga. Taimirira, M’bale Busty. Ndi uyoapo. Tiyeni timupatseMulungumatamando, aliyense.

Anasonkana mu chipinda,Akupemphera m’Dzina Lake.Anabatizidwa ndi Mzimu Woyera,Mphamvu ya utumiki inadza.Chomwe anawachitira apo,Akuchitirani chomwecho.Ndinewokondwa kuti, “Ndinemmodzi wawo.”

Mmodzi wawo, mmodzi wawo;Ndinewokondwa kuti, “Ndinemmodzi wawo.”(Aleluya!)

Mmodzi wawo, mmodzi wawo;Ndinewokondwa kuti, “Ndinemmodzi wawo.”

Anthuwa samadzinenera,Kudzitama ndi za mdziko,Onse alandira Pentekoste,Abatizidwa m’Dzina la Yesu.Akuwauza onse kutali,Mphamvu yake ndi yomweyo.Ndinewokondwa kuti, “Ndinemmodzi wawo.”

Mmodzi wawo, mmodzi wawo;Ndine wokondwa kuti “ndine mmodzi wawo,”(Aleluya!)

Mmodzi wawo, mmodzi wawo;Ndinewokondwa kuti, “Ndinemmodzi wawo.”

Bwera m’bale, funa dalitso’liLikutsuka mtima mwako,Liyambitsa mabelu a chimwemwe,Liyatsa moyo wako.O, ukuyaka mu mtima mwanga,Ulemerero ku Dzina Lake.Ndinewokondwa kuti, “Ndinemmodzi wawo.”(Tiyeni tiyimbe iyo!)

O, mmodzi wawo, mmodzi wawo;Ndinewokondwa kuti, “Ndinemmodzi wawo.”(Aleluya!)

Mmodzi wawo, mmodzi wawo;Ndinewokondwa kuti, “Ndinemmodzi wawo.”(Ndi angati ali mmodzi wawo, kwezanidzanja lanu? O, mai! O, momwe ine ndiririwokondwa kuti ndine mmodzi wawo.)

Page 61: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 487

Mmodzi wawo, mmodzi wawo;Ndinewokondwa kuti, “Ndinemmodzi wawo.”(Aleluya!)

Mmodzi wawo, mmodzi wawo;Ndinewokondwa kuti, “Ndinemmodzi wawo.”Anali mchipinda chapamwamba,Akupemphera mu Dzina Lake.Nabatizidwa ndi Mzimu Woyera,Mphamvu ya utumiki inadza.Zomwe anawachitira apo,Akuchitirani zomwezo.Ndinewokondwa kuti, “Ndinemmodzi wawo.”Mmodzi wawo, mmodzi wawo;Ndinewokondwa kuti, “Ndinemmodzi wawo.”(Aleluya!)

Mmodzi wawo, mmodzi wawo;Ndinewokondwa kuti, “Ndinemmodzi wawo.”

Tsopano, pamene ife tikuimba kolasi imeneyo kachiwiri, inendikufuna aliyense wa inu kuti atembenuke, ndi kugwiranamanja ndi winawake pafupi ndi inu, ndi kuti, “Kodi ndinummodzi wawo?” Mukuona? Chabwino.

O, mmodzi wawo (ine ndikudziwa inumuli, M’bale…?…ine ndikudziwa inumuli, M’bale…?…) [M’bale Branhamakugwirana chanza ndi iwo apafupi ndiiye—Mkonzi.]…mmodzi wawo.

O, mmodzi wawo, mmodzi wawo;Ndinewokondwa kuti, “Ndinemmodzi wawo.”

214 O, kodi sindinu okondwa ndinu mmodzi wawo. Ndiangati akufuna kuti akhale mmodziyo, kwezani dzanja lanu?Chabwino. Tsopano, ine ndikuti ndikuimbireni inu iyi:

Ndiye bwera m’bale, funa dalitso’liLikutsuka mtima mwako,Liyimbitsa mabelu a chimwemwe,Liyatsa moyo wako.O, ukuyaka mu mtima mwanga,Ulemerero ku Dzina Lake.Ndinewokondwa kuti, “Ndinemmodzi wawo.”O, mmodzi wawo, mmodzi wawo;Ndinewokondwa kuti, “Ndinemmodzi wawo.”(Aleluya!)

Mmodzi wawo, mmodzi wawo,Ndinewokondwa kuti, “Ndinemmodzi wawo.”

215 Mukukumbukira zomwe msungwana wamng’ono ananenaPetro, “Kodi sindiwe mmodzi wa iwo?” Ndine wokondwakwambiri, sichoncho inu? Inu mukudziwa, Petro ananena patsiku la Pentekoste, “Ichi ndi Chija!” Tsopano, ine ndanenapo

Page 62: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

488 KHALIDWE DONGOSOLO NDI CHIPHUNZITSO CHA MPINGO

nthawizonse, “Ngati ichi si Chija. Ndine wokondwa kuti inendiri ndi ichi, ndikuyembekeza Chijacho kuti chibwere.” Ndikokulondola. Ine ndikukondwa ndi ichi.

Ndine mmodzi wawo, mmodzi wawo;Ndinewokondwa kuti, “Ndinemmodzi wawo.”O, mmodzi wawo, mmodzi wawo;Ndinewokondwa kuti, “Ndinemmodzi wawo.”

216 O, kodi izi sizodabwitsa, kukhala limodzi mu malo aMmwambamwamba mwa Khristu Yesu, kuyanjana limodzi ndiMzimu, kuyanjana pa Mawu, kumayankhula za zinthu zabwinoziri nkudza. Ndi zabwino kwambiri. Ndine wokondwa kwambiripodziwa zimenezo, sichoncho inu? Kodi sindinu okondwa ndinuMkhristu? Kodi sindinu okondwa machimo anu ali pansi paMagazi? Iye akhala akubwera limodzi la masiku awa, ndipoife tidzakhala tikupita ndi Iye. Ndiye taganizani, ukalambawonse udzagwa kuchoka pa ife; matenda onse, kusautsika konse,moyo wonse wachivundi udzasintha. O, mai! Ine ndikhozakungoganiza za abale okondedwa achikulire omwe anaima pano.Ine ndikukumbukira…Ndi angati akumukumbukira RabbiLawson? Mai, pafupi nonse inu. Ine ndikukhoza kumuwona iyeatapachika ndodo yakale ija apa pomwe. Ndipo ine ndimakhalandiri kumbuyo uko. Iye amakhoza kumaimba nyimbo yaing’onoiyi…(Miniti yokha Teddy,M’bale.) Ine ndiyesera, ndiwone ngatindingakhoze kupeza kuimba kwa iyo. Ine sindikudziwa.

Likundiyembekeza ine mawa lokondwa,Pamene zipata za ngale zidzakankhikankutsegula kwambiri,

Ndipo pamene ndidzawoloka chotchinga chachisoni ichi,

Ndidzakapuma ku mbali inayo.

Tsiku lina kupyola momwe chivundichingadziwire,

Tsiku lina, Mulungu yekha akudziwa zoti ndikuti ndi liti,

Magudumu a moyo wachivundi onse adzaimanji,

Ndiye ine ndidzapita kukakhala ku phiri laZioni.

217 Magudumu aang’ono awa omwe akugudubuzika mkatimwa ife—kuwona, kulawa, kukhudza, kununkhiza, ndi kumva,zokhudzira zazing’ono izi ndi magudumu omwe akugudubuzikamu moyo wachivundi uno, tsiku lina zidzaima nji. Ndiye ine,inemwini, ndi inu, tidzapita kukakhala pa phiri la Zioni. O,ine ndikuzikonda izo, sichoncho inu? Podziwa kuti tiri nachochitsimikizo chodala icho. Chabwino. Ndi angati akuidziwanyimbo yathu yakale yobatizira? Tsopano, ife tisintha iyo. Tiyenititenge nyimbo yathu yobalalikira:

Page 63: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

MAFUNSO NDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERA 489

Tenga Dzina la Yesu ndi iwe,Mwana wosauka ndi watsoka;Lidzakusangalatsa ndi kukupatsa iwechitonthozo,

Tenga ilo kulikonse upita.Tengani Dzina la Yesu limodzi nanu. Ingochitani izo, pamene

inu mukupita. Chabwino, tonse palimodzi tsopano. Musatimuiwale, 8 kolokommawamakadi a pemphero azidzaperekedwamu msonkhano. Msonkhano udzayamba ili hafu pasiti naini. Inendidzakhala ndikulalikira pa 10:00. Msonkhano wa pempherokwa odwala udzayamba pafupi 11 koloko.

Mawa madzulo, mawa usiku udzakhala uthenga waulalikiku kachisi. Ndipo mawa usiku, nonse inu omwe mwalapamachimo anu ndipo simunabatizidwe konse, kudzakhala…dziwe lomwe lidzakhala lotsegulidwa; ife tidzakhalatikuwabatiza anthumuDzina la Ambuye YesuKhristu.

Aliyense limodzi tsopano, pamene ife tikuimba pamwambapa mawu athu. M’bale Busty, inu simukudziwa momweine ndiriri wokondwa ndi wothokoza kwa Mulungu. Inumukudziwa, iye anapita kwa dokotala. Ndipo iwo akundiuza inekuti adokotala anayang’ana pa iye, ndipo sanali kudziwa basizoti aganize. Iye sanali kukhulupirira kuti uyo anali mwamunayemweyo. O, si chinsinsi zomwe Mulungu angakhoze kuchita.Kodi si kulondola uko? Chabwino.

Tenga Dzina (Iyimbeni iyo momveka!) la Yesu,Mwana wosaukawe;Lidzakusangalatsa iwe,Litenge kulikonseko.Dzinalo (Lofunika!), O ndi lokoma!Chiyembekezo cha dziko;Dzina lofunika (O, lofunika!), ndi lokoma!Chisangalalo cha Kumwamba.

Chabwino. Ine ndikutembenuzira msonkhano tsopano kwaabusa. Iwo akhala ali ndi mawu ena, kapena ayankhula kutiwinawake atibalalitse ife, chirichonse chimene chiri pa mtimawao.

Page 64: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

Khalidwe Dongosolo ndi Chiphunzitso cha Mpingo, Bukhu Loyamba(Conduct, Order And Doctrine Of The Church, Volume One)

Mauthenga awa a M’bale William Marrion Branham olalikidwa ku BranhamTabernacle mu Jeffersonville, Indiana, U.S.A., anatengedwa kuchokera pamatepi ojambulidwa ndi maginito ndipo anadindidwa mosachotsera mawuena mu Chingelezi. Ndipo kumasulira kwa Chichewa uku kunadindidwa ndikugawidwa ndi Voice of God Recordings.

CHICHEWA

©2009 VGR, ALL RIGHTS RESERVED

VOICE OF GOD RECORDINGS, MALAWI OFFICE

P.O. BOX 51453, LIMBE, MALAWI

VOICE OF GOD RECORDINGS

P.O. BOX 950, JEFFERSONVILLE, INDIANA 47131 U.S.A.www.branham.org

Page 65: MAFUNSONDI MAYANKHO PA MZIMU WOYERAdownload.branham.org/pdf/CHA/CHA59-1219 Questions... · ulipo. Ndipo pamene mphamvu ya mpingo uwu ikwera, iwo udzawabweretsa abale ake; mphamvu

Chidziwitso kwa ofuna kusindikiza

Maufulu onse ndi osungidwa. Bukhu ili mukhoza ku printa kunyumba kwanu ngati mutafuna kuti mugwiritse ntchito inuyo kapena kuti mukawapatse ena, ulere, ngati chida chofalitsira Uthenga wa Yesu Khristu. Bukhu ili simungathe kuligulitsa, kulichulukitsa kuti akhalepo ambiri, kuikidwa pa intaneti, kukaliika pakuti ena azitengapo, kumasuliridwa mu zinenero zina, kapena kugwiritsidwa ntchito ngati njira yopezera ndalama popanda chilolezo chochita kulembedwa ndi a Voice Of God Recordings®.

Ngati mukufuna kuti mumve zambiri kapena ngati mukufuna zipangizo zina zimene tiri nazo, chonde mulembere ku:

Voice of God RecoRdinGsP.o. Box 950, JeffeRsonVille, indiana 47131 U.s.a.

www.branham.org